< 2 Timoteyo 2 >

1 Tsono iwe, mwana wanga, limbika mʼchisomo chimene chili mwa Khristu Yesu.
Fini n big, ya pagd a pal yen ya ŋalbalgin yen yesu kilisu niini.
2 Ndipo zinthu zimene unamva ine ndikuziyankhula pamaso pa mboni zambiri, uziphunzitse kwa anthu odalirika amene akaphunzitsenso ena.
A tunda yal k a bang n kan k kasielb bocial tuo a po, bogdli ya nub k a dan bi po k ba fid ki wan bitab.
3 Umve nane zowawa, monga msilikali wa Khristu Yesu.
ŋan tuo ki ga fala yen nni, nan yesu kilisu ya nannangu yen.
4 Palibe msilikali amene ali pa ntchito amagwiranso ntchito za anthu wamba, iye amafuna kukondweretsa bwana wolamulira.
Yua n kua t sojed k bua wan mang o canba pal kan jɔd o yeyienu boam bona po.
5 Chimodzimodzinso, munthu amene ali pa mpikisano waliwiro, salandira mphotho ya wopambana pokhapokha atatsiriza monga mwa malamulo a mpikisanowo.
Nasanlo k o ga e panpan kaa cɔnln ban blo ya kuana.
6 Mlimi wolimbika ndi amene amayembekezereka kukhala woyambirira kulandira gawo la zokolola.
Ya kpakuolo n ko paa n tie yua n ba cil ki mang o pal taagu po.
7 Lingalira zimene ndikunenazi, pakuti Ambuye adzakuzindikiritsa zonsezi.
Maal ŋamma min mara yal yen yom dan ba nan gbad l bona kul.
8 Kumbukira Yesu Khristu wochokera ku mtundu wa Davide kuti anauka kwa akufa. Uwu ndiye uthenga wanga wabwino
Fin n tiad yesu kilisu po, yua fi bi kpienb sigan, dafid yabil, yal naan yen min muandi ya labal.
9 umene ndikuwuvutikira choterewu mpaka kumangidwa ndi maunyolo ngati wakuba. Koma mawu a Mulungu sanamangidwe ndi maunyolo.
Lan labal poe kin cangin, hal ki ban lolin nan o kukpal yen. O tienu maam, lan wan ki luol.
10 Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios g166)
N gan li maaba kul yen li junl, kilisu yab ya po k o tienu gagd, lan fid bimɔn la ya fabu n yesu kilisu, yen ya kpagidi n ki pia gben yen yal yeg yenl. (aiōnios g166)
11 Mawu oyenera kuwadalira ndi awa: Ngati ife tinafa naye pamodzi, tidzakhalanso moyo pamodzi naye.
Klma li maama tie moamoɔn ne: li ya tua k t kpe yen o, yen wan, ti ba fuo yen o.
12 Ngati tinapirira, tidzalamuliranso naye pamodzi. Ngati ife timukana, Iye adzatikananso.
Li ya tua ki ti tugn yen o t ba pia o palu. Ama ti ya yieo omoɔ ba yie ti.
13 Ngati ndife osakhulupirika, Iye adzakhalabe wokhulupirika popeza sangathe kudzikana.
Ti yaa tieg yeno, wan wan baa ye n tiegman klma o kan fid ki yie o ba.
14 Uziwakumbutsa anthu a Mulungu zinthu izi. Uwachenjeze pamaso pa Mulungu kuti asamakangane pa za mawu. Zimenezi nʼzopanda phindu ndipo zimangowononga amene akumvawo.
Lane ki li bual min ya tiada yog kul. O tienu ki bua n niam: la pugd pu. Li yaa tie lan bid yab n song yaa ka.
15 Uyesetse kukhala wovomerezeka pamaso pa Mulungu monga wantchito wopanda chifukwa chochitira manyazi amene amalalikira mawu achoonadi molondola.
Pag aba ki sed o tienu nug nan ya nulo n bobn, k kua li tuonl kaa pia wansan k ŋa li tuonl, klma o wangi o tienu maam yen e mumɔn.
16 Upewe nkhani zopanda pake, zosalemekeza Mulungu, chifukwa anthu oyankhula zotere amanka napotokerapotokera.
ŋa ti miyoyod yen yamb n k tie li dandal yab. yab ta bi ba k tenb, b fagd yogu kul yen o tienu.
17 Chiphunzitso chawo chidzafalikira ngati chilonda. Mwa anthuwa muli Humenayo ndi Fileto.
Li nub maam tie nan li bofuodl yen ki li ŋman k ban gben t gbanand. Li tie nan d yimane yen filet yene.
18 Iwowa apatuka pa choonadi. Iwo amaphunzitsa kuti kuuka kwa akufa kunachitika kale, motero amawononga chikhulupiriro cha anthu ena.
Bi den fagd e mon ki mali kin yiedm tienped o, yeni, bi ji ye ki ŋand bocianl li dandanln.
19 Komabe maziko olimba, amene Mulungu anawayika ngokhazikika, ndipo mawu olembedwapo ndi awa: “Yehova amadziwa amene ndi ake,” ndiponso, “Aliyense amene amavomereza dzina la Ambuye ayenera kusiya zoyipa.”
Li yogunu goga, o tienu tan pupal se yen no maam yal tie o po bam: yomdan baan yaab n tie o yaab, yua n taa yomdan yel kul ba fagidi yen o. yam i dan ban yab tie o nub “yua n ye ki o tie ti yom i dan, wan fagd ti bid.”
20 Mʼnyumba yayikulu simukhala ziwiya zagolide ndi zasiliva zokha, koma mumakhalanso zamtengo ndi zadothi. Zina zimakhala za ntchito yapamwamba, zina za ntchito wamba.
O dieciangun, wula yen a ligi babaa bi be ka ye, li yɔgli yen ti dad ya boba. Cincin na yal tie b yumandaciab yi yale. A tien a mɔn na tagn kul.
21 Munthu akadziyeretsa nʼkusiya ntchito za wambazi, adzakhala chiwiya cha ntchito yapamwamba, woyeretsedwa, ndi waphindu kwa Ambuye wake, wokonzeka kugwira ntchito iliyonse yabwino.
Li ŋan, nulo ya cua oba min mad yal kul po. o baa tie ya bobl n bobn a tuonŋanma po, k gud pli pli, ki mon o danopo, ki pia n yaam a tuonŋanna kul po.
22 Thawa zilakolako zoyipa zachinyamata. Funafuna chilungamo, chikhulupiriro, chikondi ndi mtendere pamodzi ndi amene akuyitanira pa dzina la Ambuye ndi mtima osadetsedwa.
Fagd yen ya yeyienu n ba bid o nupano. Sɔn a palyukiba l dandanl, n buam, yen n yanduam yen ya dab n ban o tienu.
23 Ukane matsutsano oyipa ndi opusa, chifukwa amayambitsa mikangano.
Yie ti yajaga bid yen yayajaga n ki pia tanpul; a ban kili cuon yen a konkona.
24 Ndiponso mtumiki wa Ambuye asamakangane ndi anthu, koma azikhala wachifundo kwa aliyense, wodziwa kuphunzitsa, osati wokalipakalipa.
Ama, la wan ti yomdan o tuinsonlo wan ya pia konkona. li bɔl ki wan ya pia n buam yua kul po. Ki ba fid tund, ki go ga amaaba.
25 Otsutsana naye awalangize mofatsa, mwina Mulungu adzawapatsa mwayi woti asinthike ndi kuzindikira choonadi.
O ba ŋagd yen li pisonl yab n ki ban o tienu. ŋaa ban o tienu ya kan lebd bi yeyienu ban baa emonn?
26 Motero nzeru zawo zidzabweramo, ndipo adzathawa msampha wa mdierekezi, amene anawagwira ukapolo kuti azichita zofuna zake.
bi ba guan ki ba bi yeyien ŋannu ki ŋan stan jalm yal n kub ti yonbdan ki bi suan o buam.

< 2 Timoteyo 2 >