< 1 Yohane 2 >

1 Inu Ana anga okondedwa, ndikukulemberani zimenezi kuti musachimwe. Koma wina akachimwa, tili nayo Nkhoswe yotinenera kwa Atate, Yesu Khristu, Wolungamayo.
Ana ane alowa, kumukilisilya i makani aya kitalanyu iti muleke kituma i milandu, kukete mukuili nuili palung'wi nu Tata, uYesu Kilisto niiza ingi munya tai ane.
2 Iyeyo ndiye nsembe yopepesera machimo athu, ndipo osati athu okha, komanso machimo onse a dziko lapansi.
Nuanso mukinyinkang'ni witu ku mulandu itu, hangi shanga ku milandu itu ing'wene, kuiti ga ku unkumbigulu wihi,
3 Ife timatsimikiza kuti tikumudziwa ngati tikusunga malamulo ake.
Ku ili kalingaa kina kumulingile nuanso, anga kusunje i malagiilyo akwe.
4 Munthu akamanena kuti, “Ine ndimadziwa Mulungu,” koma samvera malamulo a Mulunguyo, ndi wabodza ameneyo ndipo mwa iye mulibe choonadi.
Nuanso nuiligityaa, “Numulingile Itunda.” kuiti shanga uambile i malagiilyo akwe, ige muteele, ni tai imutile mukati akwe.
5 Koma munthu aliyense akamvera mawu ake, ndiye kuti chikondi cha Mulungu chafikadi penipeni mwa iyeyo. Pamenepo timatsimikizadi kuti tili mwa Iye.
Kuiti wihi nuiambaa u lukani nulakwe, itai mu muntu nuanso u ulowa nuang'wa Itunda ukondeeigwe, Mu ili kulingile kina kukoli mu kati akwe.
6 Aliyense amene amati amakhala mwa Mulungu, ayenera kukhala moyo umene Yesu ankakhala.
Ng'wenso nuiligityaa wikiee mukati ang'wa Itunda utakiwe mukola kulongoleka anga iti uYesu Kilisto nai ulongolekile.
7 Okondedwa, sindikukulemberani lamulo latsopano koma lakale lomwe lija, limene munali nalo kuyambira pachiyambi. Lamulo la kalelo ndi mawu amene munawamva kale.
Alowa, shanga numukilisiiye unyenye ilagiilyo igeni, ila ilagiilyo nila kali naiza makondilye kutula ni lyenso puma ng'wandyo, Ilagiilyo nila kali ingi ikani niiza nai muligulye,
8 Komabe ndi lamulo latsopano limene ndikukulemberani. Choonadi chake chikuoneka mwa Yesu ndiponso mwa inu, chifukwa mdima ukutha ndipo kuwunika kwenikweni kwayamba kale kuwala.
Ga ni iti kumukilisilya unyenye ilagiilyo igeni, niiza inge tai mung'wa Kilisto nu kitalanyu, kunsoko i kiti kikukilaa nu welu nua tai ukoli ukondile ukelya.
9 Aliyense amene amati ali mʼkuwunika, koma nʼkumadana ndi mʼbale wake ali mu mdima.
Nuanso nuiligityaa ukoli mu welu hangi umubipiwe u muluna nuakwe ukoli mu kiti ga nitungili.
10 Aliyense amene amakonda mʼbale wake amakhalanso mʼkuwunika, ndipo mwa iye mulibe chokhumudwitsa.
Nuanso numuloilwe u muluna nuakwe wikiee mu welu hangi kutili ikani lihi nilihumile kumutasha.
11 Koma aliyense wodana ndi mʼbale wake ali mu mdima ndipo akuyenda mu mdima. Iyeyo sakudziwa kumene akupita, chifukwa mdima wamudetsa mʼmaso mwake.
Kuiti nuanso numubipiwe u muluna nuakwe ukoli mu kiti; nuanso shanga ulingile pi ulongoe, kunsoko ikiti kimapokuuye imiho akwe
12 Inu ana okondedwa, ndikukulemberani popeza kuti machimo anu akhululukidwa chifukwa cha dzina la Yesu.
Kumukilisilya unyenye, ana alowa, Kunsoko mulekewe i milandu anyu kunsoko a lina nilakwe.
13 Inu abambo, ndikukulemberani popeza kuti munamudziwa Iye amene analipo kuyambira pachiyambi. Inu anyamata, ndikukulemberani popeza kuti munagonjetsa woyipayo.
Kumukilisilya unyenye a tata, kunsoko mumulingile nuanso nuailee puma ung'wandyo, kumukilisilya unyenye, ahumba, kunsoko mamuhumilee uyo u mulugu. Kumukilisilya unyenye, ang'yinya ni aniino, kunsoko mumulingile uTata.
14 Ana okondedwa, ndikukulemberani chifukwa mumawadziwa Atate. Abambo, ndikukulemberani chifukwa munamudziwa Iye amene analipo kuyambira pachiyambi. Inu anyamata, ndikukulemberani chifukwa ndinu amphamvu. Mawu a Mulungu amakhala mwa inu ndipo mumamugonjetsa woyipayo.
Kumukilisilya unyenye, ia tata, kunsoko mumulingile nuanso nuailee puma u ng'wandyo. Kumukilisilya unyenye, ahumba, kunsoko mukoli ikomu, nu lukani nulang'wa Itunda likiee mukati anyu, hangi mamuhumaa uyo u mulugu.
15 Musamakonde dziko lapansi kapena chilichonse cha dziko lapansi. Ngati munthu wina aliyense akonda dziko lapansi, mwa iyeyo mulibe chikondi chokonda Atate.
Leki kumilowi ihi ang'wi makani akwe niiza ili mi ihi. Ga ni iti uyo nukumilowa ihi, ulowa nua kumulowa uTata uutili mukati akwe.
16 Pakuti zonse za mʼdziko lapansi, zilakolako za thupi, zinthu zimene maso amakhumbira ndiponso kuyandikira zinthu za moyo uno, zonsezi sizichokera kwa Atate, koma ku dziko lapansi.
Iti gwa kila kintu ni kimoli mi ihi - i nsula a muili, nsula a miho, nu lugoha nu la upanga- shanga ipuminkanilye nu Tata kuiti ipembeeye mi ihi.
17 Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn g165)
Ihi ni nsula niakwe ikilaa, Ila nuanso nuitumaa u ulowa nuang'wa Itunda nuanso nikie ikali na kali. (aiōn g165)
18 Ana anga, ino ndi nthawi yotsiriza, ndipo monga munamva kale kuti anthu okana Khristu akubwera, ngakhale tsopano okana Khristu ambiri afika kale. Zimenezi zikutisonyeza kuti ino ndi nthawi yotsiriza.
Ang'yinya ni aniino, ingi matungo a mpelo niiza migulye kina u mukingila Kilisto upembilye, ga nitungili ia kingila Kilisto azilee, ku hali iyi kulingile kina inge matungo a mpelo.
19 Anthu amenewa anachoka pakati pathu, komatu sanali a mʼgulu lathu. Pakuti akanakhala a mʼgulu lathu, akanakhalabe nafe, koma kuchoka kwawo kunatisonyeza kuti sanali a mʼgulu lathu.
Ai endile yao kupuma kitaitu, iti gwa shanga aizaa a kitaitu. Anga iti ai atule a kitaitu ai azeelongoleka kutula palung'wi nu sese. Kuiti matungo nai alongoe yao, nikanso ai kilagiie shanga ai izaa a kitaitu
20 Koma inu muli ndi kudzoza kochokera kwa Woyerayo, ndipo nonsenu mukudziwa choonadi.
Kuiti muikiwe i makuta nu uyo ni ng'welu, nu nyenye mihi mumilingile itai.
21 Sindikukulemberani chifukwa choti simudziwa choonadi ayi, koma chifukwa choti mumadziwa choonadicho, ndipo mukudziwanso kuti bodza silichokera pa choonadi.
Shanga ai numukilisiiye unyenye kunsoko shanga mumilingile itai, ila kunsoko mumilingile hangi kutili u uteele nua tai iyo.
22 Wabodzayo ndani? Ndi munthu aliyense amene amanena kuti Yesu si Mpulumutsi. Munthu woteroyo ndi wokana Khristu, ndiponso amakana Atate, ndi Mwana.
Nyenyu ni muteele, ila ingi mg'wenso nuikingila kina uYesu ingi Kilisto? U muntu uyu ingi mukingila Kilisto, pang'wanso nuku mukingila uTata nu Ng'wana.
23 Aliyense wokana Mwana alibenso Atate. Wovomereza Mwana alinso ndi Atate.
Kutili nui mukingila uNg'wana watule nu Tata. Wihi nui mulapilaa u Ng'wana ukete uTata ga.
24 Onetsetsani kuti zimene munazimva kuyambira pachiyambi zikhalebe mwa inu. Ngati zikhala mwa inu, inunso mudzakhala mwa Mwana ndiponso mwa Atate.
Anga ize kunsoko anyu, iko nai mukigulye puma ng'andyo leka kilongoleke kutula mukati anyu. Anga ize iko nai mukigule puma ng'wandyo kiki kie mukati anyu, ga, mukikie mukati a Ng'wana nu Tata.
25 Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios g166)
Ni ili ingi ilago nai ukinkiiye usese; Upanga nua kali na kali. (aiōnios g166)
26 Ine ndikukulemberani zimenezi kuti ndikuwuzeni za amene akufuna kukusocheretsani.
Numukilisiiye aya unyenye kutula awo naza azeemutongeela unyenye mu ulimili.
27 Koma za inu, kudzoza kumene munalandira kwa Khristu kuli mwa inu, ndipo sipafunika wina aliyense kuti akuphunzitseni. Koma kudzozako kumakuphunzitsani zinthu zonse, ndipo popeza kudzoza kwakeko nʼkoona osati konama, monga munaphunzira, khalani mwa Iyeyo.
Hangi kunsoko anyu, imakuta ayo nai mumasingiiye kupuma kung'waakwe ikiee mukati anyu, hangi shanga mukusiga muntu wihi kumumanyisa. ila anga i makuta akwe akumumanyisa kutula makani ihi ni ingi tai ni shanga uteele, hangi ga ni anga makondyaa kumanyisigwa, ikii mukati akwe.
28 Tsopano ana okondedwa, khalani mwa Yesu, kuti pamene adzaonekera, ife tidzakhale otsimikizika mu mtima ndi wopanda manyazi pamaso pake akamadzabwera.
Ni itungili, ang'yinya alowa ikii mukati akwe, iti itungo nuikapumila, kuhume kutula nu ugimya hangi shanga kihumya minyala ntongeela akwe mu upembyi nuakwe.
29 Popeza mukudziwa kuti Khristu ndi wolungama, choncho mukudziwanso kuti aliyense amene amachita chilungamo ndi mwana wa Mulungu.
Anga ize mulingile kina nuanso ingi tai ane, mulingile kina kila ung'wi nuitumaa itai ane utugilwe nu ng'wenso

< 1 Yohane 2 >