< 2 Petro 1 >

1 Ndine Simoni Petro, mtumiki ndi mtumwi wa Yesu Khristu. Kwa anthu amene analandira chikhulupiriro cha mtengowapatali chomwe ifenso tinalandira chifukwa cha chilungamo cha Mulungu ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu.
Simioni Petro, Mutung'waa wang'wa Yesu kilisto, Ku awo nai asingiiye u uhuiili wuwo wuwoo nua nsailo anga nai kuusingiiye usese, uhuiili nu ukoli mukati a tai ane niang'wa Itunda nu muguni witu uYesu Kilisto.
2 Chisomo ndi mtendere zochuluka zikhale nanu pomudziwa Mulungu ndi Yesu Ambuye athu.
Ukende utule kitalanyu; Ulyuuku wongeeligwe kukiila uhugu nuang'wa Itunda nu Mukulu witu Yesu.
3 Mulungu mwa mphamvu zake anatipatsa zonse zofunika kukhala moyo opembedza, potidziwitsa za Iyeyo amene anatiyitana ku ulemerero wake ndi ubwino wake.
Kukiila uhugu nuang'wa Itunda kalijaa imakani akwe ihi kunsoko a ipolya nua wikali, Puma kung'wa Itunda nai ukitangile kusoko a uziza nui ikulyo ni lakwe.
4 Mwa ulemerero ndi ubwino wakewo, anatipatsa malonjezo opambana kwambiri ndi a mtengowapatali. Amenewa ndi malonjezo amene amakuthandizani kulandira nawo moyo wa Mulungu, titapulumuka ku chiwonongeko chimene chili mʼdziko lapansi chifukwa cha zilakolako zoyipa.
Ku nzila iyi ai ukuhumilye nsula a ilago ikulu ni la nsailo. Ai witumile ili iti kuunonia ki asali a upumoo nuang'wa Itunda, ku iti ni kulongolekile kuuleka u ubii nua ihi iyi.
5 Choncho, chitani khama kuwonjezera moyo wabwino pa chikhulupiriro chanu, ndipo pa moyo wabwino muwonjezerepo nzeru.
Kunsoko iyi, kagupi kituma kongeelya u uziza ku nzila a uhuiili nuanyu, kunsoko a uziza, uhugu.
6 Pa nzeru muwonjezerepo kudziretsa, pa kudziretsa muwonjezerepo chipiriro, ndipo pa chipiriro muwonjezerepo khalidwe lolemekeza Mulungu.
Kukiila uhugu, ngele ni kukiila ngele usupyo, ni kukiila usupyo, welu.
7 Pa khalidwe lolemekeza Mulungu muwonjezerepo chifundo cha ubale, pa chifundo cha ubale muwonjezerepo chikondi.
Kukiila welu ulowa nua muluna nu kukiila ulowa nua muluna, ulowa.
8 Ngati zonsezi zikhala mwa inu nʼkumachuluka, zidzakuthandizani kuti musakhale aulesi ndi osapindula ndi chidziwitso chanu cha Ambuye athu Yesu Khristu.
Anga ize imakani aya amoli mukati anyu, aze alongolekile kukula mukati anyu, iti gwa unyenye shanga mukutula miagumba ang'wi antu nishanga itugaa inkali mu uhugu nuang'wa Mukulu witu uYesu Kilisto.
9 Koma ngati wina alibe zimenezi, ndi wakhungu sangathe kuona patali, ndipo wayiwala kuti anayeretsedwa machimo ake akale.
Kuiti wihi ni mugila i makani aya, wihengaa makani a pakupi uduu; nuanso ingi mupoku, wiwaa uweligwa nua milandu akwe na akali.
10 Nʼchifukwa chake abale anga, funitsitsani kuti mayitanidwe ndi masankhidwe anu akhale otsimikizika. Pakuti ngati muchita zinthu izi, simudzagwa konse.
Ku lulo, aluna ane, kagupi kituma iti kilingasiilya nu usagulwa nua witangwi ku nzila anyu. anga ize mukituma aya, shaga mukikwatya.
11 Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios g166)
Iti gwa mukiligiilya widu nua mulango nua kingiila mu utemi nua kali na kali nua Mukulu witu hangi muguni uYesu kilisto. (aiōnios g166)
12 Tsono ine ndidzakukumbutsani nthawi zonse za zinthu zimenezi, ngakhale kuti mumazidziwa ndipo kuti munakhazikika mʼchoonadi chimene muli nacho tsopano.
Kululo unene nikatula nkondile kumukimbusha i makani aya itungo, anga ize mulingile, ni tungili matulaa miakomu mu tai.
13 Ndikuganiza kuti nʼkoyenera ndikanali mu msasa uno, kuti ndikutsitsimutseni ndi kukukumbutsani,
Nsigile kutula nkoli iziza kumuusha nu kumukimbukiilya migulya a makani aya, ze ntuile moli mu kitala iki.
14 chifukwa ndikudziwa kuti posachedwapa ndikuchoka mu msasa uno, monga Ambuye athu Yesu Khristu anandidziwitsiratu.
Ku ndogoelyo iyi ningile kutula shanga itungo ilipu nikakiheja ikitala ni kane, anga uMukulu uYesu kilisto nai undagiie.
15 Ndipo ndidzayesetsa kuti nditachoka, mudzakumbukire nthawi zonse.
Nikakagupa kutula nu ukagupi kunsoko anyu iti mukimbukiilye imakani aya ze yakilaa unene kuhega.
16 Ife sitinatsate nkhani zongopeka titakuwuzani za mphamvu zake ndi zakubweranso kwa Ambuye athu Yesu Khristu, koma tinaona ndi maso athu za ukulu wake.
Kunsoko usese shanga ai kutyatile u uganulwa nai wingiigwe ku logo pang'wanso naikumuganuie migulya a ngulu nu kikumuula ku Mukulu witu uYesu kilisto, ila usese ai katulaa akuiili ni ikulyo ni lakwe.
17 Pakuti Iye analandira ulemu ndi ulemerero kuchokera kwa Mulungu Atate atamufikira mawu ochokera ku ulemerero wa ukulu akuti, “Uyu ndi mwana wanga amene Ine ndimukonda, amene ndimakondwera naye kwambiri.”
Nuanso ai usingiiye ikulyo nu ukulu puma kung'wa Itunda Tata pang'wanso ululi nai ligigwe kupuma mi ikulyo ikulu luzeligitya. “Uyu ng'wenso ng'wana nu ane, mulowa wane niiza ndoeigwe nu ng'wenso”
18 Ifeyo tinamva mawuwa akuchokera kumwamba pamene tinali naye pamodzi pa phiri lopatulika lija.
Ai kuligulye ulu lupuumie kilunde pang'wanso naikukoli nu ng'wenso mu lugulu ulo nu lwelu.
19 Tsono ifenso tili ndi mawu a uneneri amene ndi odalirika kwambiri ndipo inu mudzachita bwino mukawasamalira mawuwa, monga kuwunika kumene kukuwala mu mdima, mpaka tsiku lidzayambe kucha, pamene nthanda idzayambe kuwala mʼmitima mwanu.
Kukete ikani ili nila unyakidagu nai likamiinkiie, niiza ku lyenso mitumaa iza kulitumikila. anga lumuli nu leilye mu kiti kupikiila kelya ni nzota nia dau ni yigeeleka mu nkolo nianyu.
20 Kuposa zonse, inu muyenera kuzindikira kuti palibe mawu a uneneri amene amatanthauzidwa pa okha.
Lingi aya kina, kutili unyakidagu nuikilisigwa kunsoko a kiloeelya ku munyakidagu mukola.
21 Pakuti mawu a uneneri sanadze mwa kufuna kwa anthu, koma anthu anayankhula zochokera kwa Mulungu, Mzimu Woyera atawayankhulitsa.
Kunsoko kutili unyakidagu nuiuzile ku ulowa nua ng'wana adamu, Kwaala ng'wana adamu ai upewe ngulu nu Ng'wau ng'welu nai utambue puma kung'wa Itunda.

< 2 Petro 1 >