< 1 Mbiri 25 >

1 Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
I oddělil David a knížata vojska k službě syny Azafovy a Hémanovy a Jedutunovy, kteříž by prorokovali při harfách, při loutnách a při cimbálích. Byl pak počet jejich, totiž mužů těch, jenž práci vedli v přisluhování svém,
2 Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
Z synů Azafových: Zakur, Jozef, Netaniáš a Asarela, synové Azafovi, pod spravou Azafavou byli, kterýž prorokoval k rozkazu královu.
3 Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
Z Jedutuna synů Jedutunových bylo šest: Godoliáš, Zeri, Izaiáš, Chasabiáš, Mattitiáš a Simei, pod spravou otce jejich Jedutuna, kterýž prorokoval při harfě k slavení a chválení Hospodina.
4 Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
Z Hémana synové Hémanovi: Bukkiáš, Mataniáš, Uziel, Sebuel, Jerimot, Chananiáš, Chanani, Eliata, Giddalti, Romantiezer, Jazbekasa, Malloti, Hotir a Machaziot.
5 Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
Všickni ti synové Hémanovi, proroka králova v slovích Božských, k vyvyšování moci. A dal Bůh Hémanovi synů čtrnácte a dcery tři.
6 Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
Všickni ti byli pod spravou otce svého, při zpívání v domě Hospodinově na cymbálích, loutnách a harfách, k službě v domě Božím vedlé poručení králova Azafovi, Jedutunovi a Hémanovi.
7 Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
Byl pak počet jich s bratřími jejich, těmi, kteříž byli vycvičení v zpěvích Hospodinových, všech mistrů dvě stě osmdesát osm.
8 Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
Tedy metali losy, houf držících stráž naproti druhému, jakž malý, tak veliký, mistr i učedlník.
9 Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
I padl první los v čeledi Azaf na Jozefa, na Godoliáše s bratřími a syny jeho druhý, jichž bylo dvanáct.
10 Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
Třetí na Zakura, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
11 Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
Ètvrtý na Izara, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
12 Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
Pátý na Netaniáše, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
13 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
Šestý na Bukkiáše, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
14 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
Sedmý na Jesarele, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
15 Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
Osmý na Izaiáše, synům jeho a bratřím jeho dvanácti.
16 Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
Devátý na Mataniáše, synům a bratřím jeho dvanácti.
17 Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
Desátý na Simei, synům a bratřím jeho dvanácti.
18 Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
Jedenáctý na Azarele, synům a bratřím jeho dvanácti.
19 Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
Dvanáctý na Chasabiáše, synům a bratřím jeho dvanácti.
20 Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
Třináctý na Subaele, synům a bratřím jeho dvanácti.
21 Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
Ètrnáctý na Mattitiáše, synům a bratřím jeho dvanácti.
22 Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
Patnáctý na Jerimota, synům a bratřím jeho dvanácti.
23 Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
Šestnáctý na Chananiáše, synům a bratřím jeho dvanácti.
24 Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
Sedmnáctý na Jazbekasa, synům a bratřím jeho dvanácti.
25 Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
Osmnáctý na Chanani, synům a bratřím jeho dvanácti.
26 Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
Devatenáctý na Malloti, synům a bratřím jeho dvanácti.
27 Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
Dvadcátý na Eliatu, synům a bratřím jeho dvanácti.
28 Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
Jedenmecítmý na Hotira, synům a bratřím jeho dvanácti.
29 Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
Dvamecítmý na Giddalta, synům a bratřím jeho dvanácti.
30 Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
Třímecítmý na Machaziota, synům a bratřím jeho dvanácti.
31 Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.
Ètyřmecítmý na Romantiezera, synům a bratřím jeho dvanácti.

< 1 Mbiri 25 >