< Gesami Hea:su 2 >
1 Abuliba: le soge bagade fi dunu ilia gegemusa: ilegesala: ? Abuliba: le, ilia da udigili gegemusa: sia: dabela: ?
Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu?
2 Ilia hina bagade dunu ilia gegemusa: dawa: , amola ilia ouligisu dunu ilia Hina Godema higasa amola Hina Bagade E ilegele lai Ema higasa.
Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.
3 Ilia amane sia: sa, “Be ninia da ilia hamoma: ne sia: i agoema afafamu da defea, amola ilia ouligi yolesimu da defea.”
Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”
4 Hina Gode da Hi Hebene fafai fisu da: iya fila heda: le ousa, amola ilia sia: dasu amo nabalu ousa.
Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo.
5 Amolalu, E da ougi gasa bagadewane sisasu sia: olelesa. E da Ea gasa ilima olelebeba: le, ilia beda: sa.
Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
6 Gode da amane sia: sa, “Saione (amo da Na hadigi sema goumi) amo da: iya, Na da Na Hina Bagade amogai asunasi.
“Ine ndakhazikitsa mfumu yanga pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
7 Na da Hina Gode Ea sia: dilima sia: mu. E da nama amane sia: i, “Di da Nagofe. Wali da Na Dia Ada hamoi.
Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako.
8 Adole ba: ma, amola Na soge fi huluane Dima imunu osobo bagade huluane da Dia: ganumu.
Tandipempha, ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako; malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
9 Dia da ili ouli fesonoi amoga fane fili fasimu, amola Dia da huluane osoboga hahamoi yaeya amo gagoudane fofonobone fasisu amo defele ili gagoudane fasimu.”
Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
10 Dilia osobo bagade hina bagade dunu! Na sisasu sia: olelesu noga: le nabima!
Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
11 Hina Gode Ema beda: iwane fa: no bobogema.
Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
12 Ema beda: ga yaguguiwane muguni bugila sa: ima. Amai hame hamosea, Ea ougi hou da hedolowane heda: mu galebe, amola dilia da hedolowane bogomu. Nowa da Ema gaga: ma: ne ahoasea da Ea hahawane dogolegesu hou ba: mu.
Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye; kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu, pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa. Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.