< Malasu 1 >

1 Goe buga ganodini malasu amo Soloumone (Da: ibidi ea mano) Isala: ili hina bagade da dedei.
Iyi ndi miyambi ya Solomoni mwana wa Davide, mfumu ya Israeli:
2 Goe da malasu amo ea di bagade fidimuyo amola dia noga: le hou moloi ba: ma: ne amola hou ida: iwanedafa olelesa. Amola noga: le amo sia: dawa: ma: ne ea bai da gududafa.
Ndi yothandiza kuti munthu adziwe nzeru ndi malangizo; kuti amvetse mawu a matanthauzo ozama;
3 Amola ilia da dima noga: le hou moloi ahoanoma: ne olelesa amola defele hamoma: ne olelesa.
kuti alandire malangizo othandiza kuti achite zinthu mwanzeru, akhale wangwiro, wachilungamo ndiponso wosakondera.
4 Amola ilia di dawa: loma: ne hamosa amola dunu dawa: su bagade olelesa eno dunu goi olelema: ne.
Ndi yothandiza munthu wamba kuti aphunzire nzeru za kuchenjera, achinyamata kudziwa zinthu bwino ndi kulingalira.
5 Amo sia: dedei da bagade dawa: su dunu ilima dawa: loma: ne, olelesu amola moloidafa hou imunu.
Munthu wanzeru amvetse bwino miyamboyi kuti awonjezere kuphunzira kwake, ndi munthu womvetsa zinthu bwino apatepo luso,
6 Amasea, ilia da malasu wamolegei bai amo noga: le dawa: ma: ne amola malasu da moloi dunu ea hou heda: ma: ne eno hou doaga: sea, dawa: ma: ne olelesa.
kuti azimvetsa miyambi ndi mafanizo, mawu a anthu anzeru ndi mikuluwiko.
7 Di da bagade dawa: su hou lamu hanai galea, hidadea Godema nodone dawa: ma. Gagaoui dunu ilia da dawa: su bagade lama: ne hame asigisa, amola moloidafa hou dawa: mu higasa.
Kuopa Yehova ndiye chiyambi cha nzeru. Zitsiru zimanyoza nzeru ndi malangizo.
8 Nagofe! Dia noga: le nabima, dia ada amola ame elea sia: sea.
Mwana wanga, mvera malangizo a abambo ako ndipo usakane mawu okuwongolera a amayi ako.
9 Elea olelebe amo ea dia hou da gado heda: mu amola dia hamobe liligi da nina: hamoi habuga o galogoaga gisa: gisu amo ba: le defele ba: mu.
Ali ngati sangamutu yokongola ya maluwa pamutu pako ndiponso ali ngati mkanda mʼkhosi mwako.
10 Nagofe dia! Wadela: le hamosu dunu ilia dima adoba: sea, di amoma maedafa madelama.
Mwana wanga, ngati anthu oyipa afuna kukukopa usamawamvere.
11 Ilia sia: sa, “Misa! Ninia hedemusa: noga: i dunu medole legemusa: hogola masunu.
Akadzati, “Tiye kuno; tikabisale kuti tiphe anthu, tikabisalire anthu osalakwa;
12 Amaiba: le ninia asili, hahawane esalebe dunu ba: sea, hedolowane medole legemu. (Sheol h7585)
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol h7585)
13 Amasea ninia ilia liligi lale ninia diasuga gaguli masunu amola ninia da liligi gagui dunu agoai esalumu.
Motero tidzapeza zinthu zosiyanasiyana zamtengowapatali ndi kudzaza nyumba zathu ndi zolanda;
14 Misa! Ninima madelama! Amola ninia wamolai liligi gilisili gagumu.”
Bwera, chita nafe maere, ndipo tidzagawana chuma chathu tonse.”
15 Nagofe! Agoai dunu ilima mae gilisima amola di gasigama.
Mwana wanga, usayende nawo pamodzi, usatsagane nawo mʼnjira zawozo.
16 Ilia da gasa bagadewane eso huluane eno dunu medole legemusa: momagei esala.
Iwowatu amangofuna zoyipa zokhazokha, amathamangira kukhetsa magazi.
17 Amola di da sio di hanai amo sio sa: ima: ne sani amoga gaguma: ne e ba: lalea hame ligisisa.
Nʼkopanda phindu kutchera msampha mbalame zikuona!
18 Be dunu nowa e amane hamosea, e da hina: bogoma: ne sani amoga hina: sa: ima: ne logo hogosa.
Koma anthu amenewa amangobisalira miyoyo yawo yomwe; amangodzitchera okha msampha!
19 Wamolasu e da ea wamolasu hamobeba: le da bogosu ba: mu. Nowa da nimi gasa fi hou bagade hamosea da bogosu ba: mu.
Awa ndiwo mathero a anthu opeza chuma mwankhanza; chumacho chimapha mwiniwake.
20 Nabima! Bagade Dawa: su Hou da welala amola logoga amola gilisisu bidi lama: ne diasu sogega welala.
Nzeru ikufuwula mu msewu, ikuyankhula mokweza mawu mʼmisika;
21 Gasa gala welala amola fi sogebi logo holeiga amola dunu huluane gilisibi amola misini gilisisu sogebi.
ikufuwula pa mphambano ya misewu, ikuyankhula pa zipata za mzinda kuti,
22 Gagaoui dunu habowali dili da gagaoui esaloma: bela: ? Habowali dilia da Bagade Dawa: su Hou amoma higale oufesega: ma: bela: ? Amola habogala dawa: lama: bela: ?
“Kodi inu anthu osachangamukanu, mudzakondwera ndi kusachangamuka mpaka liti? Nanga anthu onyogodola adzakondabe kunyogodola mpaka liti? Kapena opusa adzadana ndi nzeru mpaka liti?
23 Na da dilima gagabole sia: sea, dilia noga: le nabima! Na da hahawane sia: olelesa amola na dawa: dilima olelemu.
Tamverani mawu anga a chidzudzulo. Ine ndikukuwuzani maganizo anga ndi kukudziwitsani mawu anga.
24 Na da dilima welalu amola dili misa: ne sia: nanu, be dilia da hame nabi amola dilia da na sia: be hame dawa: digi.
Popeza ndinakuyitanani koma inu munakana kumvera. Ndinayesa kukuthandizani koma panalibe amene anasamala.
25 Dili da na fada: i sia: i higa: i amola na olelei amola dili da amane hamomusa: hame hanai amola na gagabosu hame nabi.
Uphungu wanga munawunyoza. Kudzudzula kwanga simunakusamale.
26 Amaiba: le, dilia da da: i dioi doaga: sea na da diliba: le oufesega: mu amola na da dili gadele oumu dilima beda: ga da: i dioi doaga: sea.
Ndiye inenso ndidzakusekani mukadzakhala mʼmavuto; ndidzakunyogodolani chikadzakugwerani chimene mumachiopacho.
27 Adi liligi, mulu mabe amo defele se fo mabe defele dilima da: i dioi amola se nabasu doaga: sea,
Chiwonongeko chikadzakugwerani ngati namondwe, tsoka likadzakufikirani ngati kamvuluvulu, mavuto ndi masautso akadzakugwerani.
28 dilia da hahawane bagade dawa: su esalusu hogomu amola wemu. Be na da hame nabimu. Dilia da na hogoi helemu. Be amomane dilia da na hame ba: mu.
“Tsono mudzandiyitana koma sindidzayankha; mudzandifunafuna, koma simudzandipeza.
29 Dili da musa: Bagade Dawa: su Hou hogomusa: hame hamosu amola dili da Gode Ea moloidafa hou nabimu higasu.
Popeza iwo anadana ndi chidziwitso ndipo sanasankhe kuopa Yehova,
30 Dili da na sia: amo hame nabasu amola na olelesea amoga hame dawa: su.
popeza iwo sanasamale malangizo anga ndipo ananyoza chidzudzulo changa.
31 Amaiba: le dili da dilia higa: i amo ea bidi lamu. Amola dili hou amo hamoiba: le, dilia da olomu.
Tsono adzadya zipatso zoyenera mayendedwe awo ndi kukhuta ndi ntchito zimene anachita kwa ena.
32 Hame dawa: su dunu ilia bogosu bai da ilia Bagade Dawa: su Hou amo higasa. Amola gagaoui dunu ilia da ilia gagaoui hou amoga ilila: wadela: sa.
Pakuti anthu osachangamuka amaphedwa chifukwa cha kusochera kwawo, ndipo zitsiru zimadziwononga zokha chifukwa cha mphwayi zawo.
33 Nowa da nama nabasu hou hamosea amo da gaga: su ba: mu, amola e da udigili beda: su hou bai hame ba: mu.
Koma aliyense wondimvera adzakhala mwa bata; adzakhala mosatekeseka posaopa chilichonse.”

< Malasu 1 >