Aionian Verses
Egefelali amola idiwi huluane da ema ea dogo denesima: ne doaga: i, be e da dogo denesimu amola olofomu hamedei ba: i. E amane sia: i, “Na da mae yolesili, da: i dione amola dinana bogomu.” Amaiba: le, ea da: i dioi e da mae yolesili da: i diolalu. (Sheol )
Ngakhale kuti ana ake onse aamuna ndi aakazi anasonkhana kudzamutonthoza, iye anakana kutonthozedwa. Iye anati, “Ayi. Ndidzalira mpaka ndidzapite kwa mwana wanga ku manda.” Choncho Israeli anapitirirabe kulira mwana wake. (Sheol )
Be Ya: igobe da amane sia: i, “Na gofe da dili sigi masunu hamedei. Ea ola da bogoi amola hisu da esala. E da logoga se nabasa: besa: le, hamedafa masunu. Na da dunu da: i hamoi dagoi. Di da amo se nabasu nama iasea, na bogomu.” (Sheol )
Koma Yakobo anati, “Mwana wanga sapita nanu kumeneko; mkulu wake anamwalira ndipo watsala yekha. Ngati choyipa chitamuchitikira pa ulendo mukupitawu, ndiye kuti ndi mmene ndakalambiramu inu mudzandipha ndi chisoni chotere.” (Sheol )
Na da ufi mano afae fawane esala. Be amo dilia oule ahoasea, e da se nabasea, na da: i hamoiba: le, se bagade dili nama i amo nababeba: le, bogomu.’ (Sheol )
Tsopano mukanditengeranso uyu, nakaphedwa mu njira ndiye kuti mudzandikankhira ku manda ndi chisoni.’ (Sheol )
Amaiba: le, ada! Na amo goi fisili adama bu asili, e da goi hame oule misi amo ba: sea, bogomu. Ea esalusu amola amo goi ea esalusu da gilisili lala: gi agoane diala. E da: idafa hamoiba: le, ninia da amo se nabasu ema iasea, e da bogomu. (Sheol )
(parallel missing)
Genesis 44:31
(parallel missing)
ndipo akakaona kuti mnyamatayu palibe, basi akafa. Ife tidzakhala ngati takankhira abambo athu ku manda ndi chisoni. (Sheol )
Be Hina Gode da hou musa: hame ba: i hamosea, amola osobo ea lafi da dagale, dunu amola ilia liligi huluane amo mogo salasea, amola ilia esaleawane udigili bogoi sogega gudu dasea, amo dunu da Hina Gode da ilima higale yolesi dagoi dilia da dawa: mu.” (Sheol )
Koma Yehova akachita china chake chachilendo, nthaka nitsekula pakamwa pake ndi kuwameza iwo pamodzi ndi zonse zimene ali nazo, iwowa nʼkulowa mʼmanda ali moyo, pamenepo mudzazindikira kuti anthu amenewa ananyoza Yehova.” (Sheol )
Amaiba: le, ilia amola ilia liligi huluane da mae bogole, bogoi sogega gudu sa: i. Ilia gudu sa: i dagoloba, osobo ea lafi da bu ga: si. Ilia da bu hamedafa ba: i. (Sheol )
Analowa mʼmanda amoyo pamodzi ndi zonse zimene anali nazo. Nthaka inawatsekera ndi kuwawononga ndipo sanaonekenso. (Sheol )
Na ougi da lalu agoane heda: mu. Liligi huluane osobo bagadega diala da amoga nene dagomu. Amo lalu da bogoi sogega doaga: le, goumi ea bai huluane nene dagomu. (Sheol )
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol )
Hina Gode da fane legesa amola bu wa: lesisu dawa: E da dunu bogoi sogega asunasisa, amola amo bu sinidigima: ne oule maha. (Sheol )
“Yehova amabweretsa imfa ndipo amaperekanso moyo, amatsitsira ku manda ndipo amawatulutsakonso. (Sheol )
Na bogomu da gadenenewane ba: i. Bogoi uli dogoi da sani agoane dili dialu. (Sheol )
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
Dia hamomu amo di dawa: Amo dunu medole legema: ma. (Sheol )
Iwe uchite kwa iye molingana ndi nzeru zako, koma usalole kuti afe ndi ukalamba ndi kupita ku manda mwamtendere. (Sheol )
Be di da ema dawama: ne se dabe ima. Dia hamomu amo di dawa: Amo dunu medole legema: ne sia: ma.” (Sheol )
Koma tsopano usamuyese ngati munthu wosalakwa. Iwe ndiwe munthu wanzeru. Udzadziwa choti uchite naye. Ngakhale ndi wokalamba, aphedwe ndithu.” (Sheol )
Job 7:9 (Yobu 7:9)
(parallel missing)
Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol )
Mu mobi da ba: lalu, hedolowane gilasi dagoi ba: sa. Amo defele, ninia osobo bagade dunu da bogosea, hame buhagisa. Nini dawa: su dunu, ilia da nini hedolo gogolesa. (Sheol )
(parallel missing)
Di da mu digili ba: mu gogolesa. Be Gode da mu amola liligi huluane baligisa. Gode da bogoi dunu ilia soge dawa: be. Be di da amo hame dawa: (Sheol )
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol )
Di da na bogoi dunu ilia sogebi amoga wamolegemu, na da hanai gala. Na da wamolegei dialea, Dia ougi da gumisia fawane, Dia na bu dawa: ma: ne eso ilegema. (Sheol )
“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda ndi kundiphimba kuti ndisaoneke mpaka mkwiyo wanu utapita! Achikhala munandiyikira nthawi, kuti pambuyo pake mundikumbukirenso. (Sheol )
Nama hobea misunu dafawane hamoma: beyale hou dawa: be da bogosu soge fawane dawa: sa. Amogawi na gasi ganodini dialumu. (Sheol )
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol )
Na da bogoi dunu ilia sogega gudu dasea, hobea misunu hou hahawane hamoma: beyale dawa: su da na gilisili hame masunu.” (Sheol )
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol )
Ilia olofole agoane esalu, se mae nabawane bogosa. (Sheol )
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol )
Eso da gia: sea, mugene ofo da alalolesisa. Amo defele, wadela: i hamosu dunu da dunu esalebe sogega bu mae ba: ma: ne alalolesisa. (Sheol )
Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana ndi momwemonso mmene manda amachotsera omwe achimwa. (Sheol )
Gode da bogoi dunu ilia soge ba: lala. Ea siga mae ba: ma: ne, amo soge da hame alaloi. (Sheol )
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol )
Osobo bagade fi bogosu sogebi amo ganodini ilia da Di hame dawa: sa. Amogawi, Dima nodomu da hamedei. (Sheol )
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol )
Dunu huluane amo da wadela: le hamosa amola Godema higabe dunu huluane da bogosu ba: mu. (Sheol )
Oyipa amabwerera ku manda, mitundu yonse imene imayiwala Mulungu. (Sheol )
Bai Dia da bogosu logo ea gasa amoga na gaga: i dagoi. Amola Di da na dogolegeiba: le, Dia da na bogosu soge ganodini dasama: ne hame yolesimu. (Sheol )
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
Na bogomu da gadenenewane ba: i. Bogoi uli dogoi da sani agoane dili dialu. (Sheol )
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol )
Di da na bogosa: besa: le gaga: i dagoi. Na da bogosu hagudu amoga ahoanu galu, be Di da na bu esaloma: ne hamoi. (Sheol )
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol )
Hina Gode! Na da Dima wele sia: sa! Na da mae gogosiasu hamoma: ma! Be wadela: i hamosu dunu ilia gogosiasu ba: mu da defea. Ilia da ouiya: lewane bogosu sogebi amo gudu sa: imu da defea. (Sheol )
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol )
Ilia da sibi agoane, hobeamu gogoleiba: le, bogosu ba: mu. Fedege agoane, Bogosu da ilia sibi ouligisu dunu agoai ba: mu. Bogosu soge ganodini ilia fifi lasu amoga sedadewane dialea, ilia da: i hodo da dasamu. Amola moloidafa hamosu dunu ilia da amo wadela: i hamosu dunu hasalimu. (Sheol )
Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol )
Be Gode da na gaga: mu. Amola bogosu ea gasa amoga E da na gaga: mu. (Sheol )
Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol )
Nama ha lai dunu ilia da ilia bogosu eso mae doaga: le, bogomu da defea. Ilia da esaleawane, bogoi sogega gudu sa: imu da defea. Wadela: i hou da ilia diasu gaguli gagai amola ilia dogo amo ganodini dialebe ba: sa. (Sheol )
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol )
Dia nama asigi hou amo da mae yolele gebewane diala! Di da uli dogoi amo ganodini na dasa: besa: le, na noga: le gaga: i. (Sheol )
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol )
Bidi hamosu bagohame da nama misiba: le, na da bogomu gadenei. (Sheol )
Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda. (Sheol )
Nowa da mae bogole fifi ahoanoma: bela: ? Dunudafa ninia da, nini bogoi uli dogoi amoga dasa: besa: le habodane gaga: ma: bela: ? (Sheol )
Kodi ndi munthu uti angakhale ndi moyo ndi kusaona imfa? Kapena kudzipulumutsa yekha ku mphamvu ya manda? (Sela) (Sheol )
Na da baligiliwane da: i dioi amola beda: i galu. Bai na bogole, bogoi uli dogoiga gudu sa: imu gadenene ba: i. (Sheol )
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol )
Na da muagado heda: i ganiaba, Di da amogawi esalebe ba: la: loba. Na da bogosu sogebia asiaba, Di da amogawi esalebe ba: la: loba. (Sheol )
Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko; ndikakagona ku malo a anthu akufa, Inu muli komweko. (Sheol )
Lalu ifa da gaga: ne habele dudunumiai ba: mu. Amo defele, amo dunu ilia gasa da bogoi ulidogoi bega: afagogoi ba: mu. (Sheol )
Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza, ndi momwenso mafupa athu amwazikira pa khomo la manda.” (Sheol )
Amaiba: le ninia asili, hahawane esalebe dunu ba: sea, hedolowane medole legemu. (Sheol )
tiwameze amoyo ngati manda, ndi athunthu ngati anthu otsikira mʼdzenje. (Sheol )
Agoai uda da di sigi osobo bagadega bogosu amoga oule ahoa. Amola logo ea ahoabe amo da bogosu amoga doaga: musa: ahoa. (Sheol )
Mapazi ake amatsikira ku imfa; akamayenda ndiye kuti akupita ku manda. (Sheol )
Amola di da amo uda ea diasuga ahoasea, di da bogosu logo amoga ahoa. Amo ahoasu da hedolodafa bogosu amoga doaga: sa. (Sheol )
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol )
Dunu ilia ea sia: nabasea, ilia hame dawa: ea diasu amo da bogoi uli dogoi agoaiwane. Amola dunu ilia amoga ahoa. Amola dunu ilia da musa: ea diasuga asi da wali bogosu soge amoga sa: i dagoi. (Sheol )
Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko, ndi kuti alendo ake alowa kale mʼmanda akuya. (Sheol )
Hina Gode da liligi huluanedafa dawa: E da bogosu soge amo ganodini diala liligi huluane dawa: Amaiba: le, dunu da ea asigi dawa: su amo Hina Godema habodane wamolegema: bela: ? (Sheol )
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol )
Noga: i dawa: su dunu da logo amo da esalalalusu amoga heda: sa, amoga ahoa. Be logo da bogosu amoga gudu daha, amo logoga ilia da hame ahoa. (Sheol )
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol )
Be amo dawa: ma: ne fasu da ea esalusu gaga: mu. (Sheol )
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol )
Bogosu soge da hamedafa nabamu. Amaiwane, osobo bagade dunu da liligi hanai gala. Amola sadimu hame dawa: (Sheol )
Manda sakhuta, nawonso maso a munthu sakhuta. (Sheol )
Amo liligi biyaduyale gala da, (age) Bogoi uli dogoi da hame sadimu. (ageyadu) Aligime uda da hame sadimu. (osoda) Hafoga: i osobo gibu hameba: le da hame sadimu. (biyadu) Amola lalu haba: domu gogolei amo da hame sadimu. (Sheol )
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol )
Dia hawa: hamosea, gasa fili hamoma! Bai di bogoi sogebi doaga: sea, hawa: hamomu amola asigiga dawa: mu amola bagade dawa: su hou huluane bu hamedafa ba: mu. Amola di da bogoi soge amogawi masunu. (Sheol )
Ntchito iliyonse imene ukuyigwira, uyigwire ndi mphamvu zako zonse, pakuti ku manda kumene ukupita kulibe kugwira ntchito, kulibe malingaliro, chidziwitso ndiponso nzeru. (Sheol )
Dia nama fawane sasagema. Amola dia loboga eno mae sogoba: le, na fawane sogoba: ma. Be gia: i bagade mudasu hou amo da bogosu ea gasa defele gala. Amo hou da lalu agoane heloa: gala: le, lalu gegemoi defele nenana. (Sheol )
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol )
Fedege agoane, bogoi sogebi da dili manusa: , ha: i bagade gala. E da ea lafi bagadewane daga: sa. E da Yelusaleme ouligisu dunu amola sia: bagade dunudafa huluane gilisili da: gisa. (Sheol )
Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta ndipo kwayasama kwambiri kukamwa kwake; mʼmandamo mudzagweranso anthu otchuka a mu Yerusalemu pamodzi ndi anthu wamba ochuluka; adzagweramo ali wowowo, nʼkuledzera kwawoko. (Sheol )
“Dia Hina Gode da dima dawa: digima: ne olelesu ima: ne, Ema adole ba: ma. E da bogoi soge haguduga o muagado Hebene amoga dima dawa: digima: ne olelesu imunusa: dawa: (Sheol )
“Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako, chikhale chozama ngati manda kapena chachitali ngati mlengalenga.” (Sheol )
Bogoi sogebi ouligisu dunu ilia da Ba: bilone hina bagade aowamusa: momagesa. Musa: esalu osobo bagade ouligisu dunu ilia a: silibu da nedigisa. Ilia da fisu fisili, wa: legadosa. (Sheol )
Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol )
Musa: dunu da dima nodomusa: , sani baidama dusu, be wali di da guiguda: bogoi sogebi amoga misi doaga: i. Di da ifidi gilisisu amoga diaha amola dia da daba: amoga dedeboi dagoi. (Sheol )
Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol )
Be amo hame hamone, di da bogoi sogebi osodogone amoga gisalugala: i dagoi ba: sa. (Sheol )
Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol )
Dilia da hidale, dilia da bogosu hou amola bogoi dunu ilia esalebe soge amoga gousa: su hamoi dagoi sia: sa. Wadela: lesisu da osobo bagadega doaga: sea, dilima hame doaga: ma: ne, dilia giadofale dawa: sa. Bai ogogosu sia: amola ogogosu hou da dili gaga: mu, dilia dawa: (Sheol )
Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol )
Gousa: su hou amo dilia da bogosu hou amola bogosu soge amoga hamoi, amo da yolesi dagoi ba: mu. Amola gugunufinisisu se nabasu da dilima doaga: sea, dilia da amoga hasanasi dagoi ba: mu. (Sheol )
Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol )
“Na da na esalebe eso amoga, bogoi sogebi amoga masusa: dawa: i galu. Na da na esalebe defei, defele esalumu hame dawa: i. (Sheol )
Ine ndinaganiza kuti ndidzapita ku dziko la akufa pamene moyo ukukoma. (Sheol )
Dunu ilia da bogoi sogebi amoga Dima nodomusa: hame dawa: Bogoi dunu da Dia mae fisili moloidafa hou amo dafawaneyale dawa: ma: ne hame dawa: (Sheol )
Pakuti akumanda sangathe kukutamandani, akufa sangayimbe nyimbo yokutamandani. Iwo amene akutsikira ku dzenje sangakukhulupirireni. (Sheol )
Dilia da gabusiga: manoma legelalu, ogogosu ‘gode’ amo Moulege amoma nodone sia: ne gadomusa: ahoa. Dilia da ‘gode’ liligi eno ilima sia: ne gadomusa: amo hogoma: ne, dilia da sia: ne iasu dunu soge sedagaga asuna ahoa. Amola amo hogomusa: dilia da osobo bagade baligili, bogosu sogebi amoga ahoa. (Sheol )
Mumapita kukapembedza fano la Moleki mutatenga mafuta ndi zonunkhira zochuluka. Munachita kutumiza akazembe anu kutali; inu ngakhale munapita ku manda kwenikweniko! (Sheol )
Ouligisudafa Hina Gode da amane sia: sa, “Amo esoha ifa da bogoi sogebi amoga ahoasea, Na da didigia: su dawa: digisu hamoma: ne, hano hagudu amo e dedeboma: mu. Na hano huluane mae masa: ne, gagulaligimu. Amo ifa da bogobeba: le, Na da Lebanone Goumi amoga gasima: ne hamomu, amola iwila ifa huluane bioma: mu. (Sheol )
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pa nthawi imene mkungudzawo unatsikira ku manda, ndinawuza nyanja kuti iwulire maliro pakuwuphimba. Ndinawumitsa mitsinje ndipo madzi ambiri anaphwa. Ndinabweretsa mdima pa Lebanoni chifukwa cha mtengowo ndipo mitengo yonse ya mʼdzikomo inawuma. (Sheol )
Na da amo ifa bogoi sogebi amoga asunasisia, ea dafasu ga: da fifi asi gala huluane fofogomu. Idini soge ifa huluane amola Lebanone ifa (amo da hano noga: le i, amola noga: idafa) amo huluane da hagudu sa: i dagoi - ilia huluane da ea dafai ba: sea, hahawane ba: mu. (Sheol )
Mitundu ya anthu inagwedezeka pakumva mkokomo wa kugwa kwake, pamene ndinawutsitsira ku manda pamodzi ndi iwo amene anafa. Pamenepo ku dziko la akufa mitengo yonse ya ku Edeni pamodzi ndi ya ku Lebanoni yosankhidwa bwino inasangalatsidwa chifukwa cha zimenezi. (Sheol )
Ilia da amo dolo ifa gilisili bogoi sogebiga, eno ifa musa: amoga sa: i amoma gilisimusa: sa: imu. Amola huluane da ea ougiha esalu, amo da fifi asi gala amoga esaloma: ne afagogolesi ba: mu. (Sheol )
Amene ankakhala mu mthunzi wake, amene ankayanjana nawo, iwonso anapita nawo pamodzi ku manda, kukakhala pamodzi ndi amene anaphedwa ndi lupanga pakati pa mitundu ya anthu. (Sheol )
Gasa bagade gegesu dunu, amola dunu da Idibidi fi amoma gale gegene bogoi, ilia da Idibidi bogoi dunu ilia bogoi sogega doaga: sea, ili nodone lale sala. Ilia da amane wele sia: sa, ‘Gode Ea hou hame dawa: dunu da gegesu ganodini medole legei, goegudu misini, dialumu!’ (Sheol )
Mʼkati mwa manda atsogoleri amphamvu pamodzi ndi ogwirizana nawo azidzakambirana za Igupto nʼkumati, ‘Afika kuno anthu osachita mdulidwe aja! Ndi awa agona apawa, ophedwa pa nkhondo.’ (Sheol )
Musa: gasa bagade noga: i dunu da bogosea, dunu eno da amo nodone uli dogosu. Ilia da amo dunu ilia gegesu gobihei ilia dialuma ha ligisili, amola ilia gegesu gaga: su liligi ilia da: i hodo da: iya ligisili, uli dogosu. Amo musa: noga: i dunu da gasa bagadeba: le, esalebe dunu da beda: gia: i. (Sheol )
Iwo sanayikidwe mwaulemu ngati ankhondo amphamvu amakedzana, amene anatsikira ku dziko la anthu akufa ndi zida zawo zomwe za nkhondo. Malupanga awo anawayika ku mitu yawo, ndipo zishango zawo anaphimba mafupa awo. Kale anthu amphamvu amenewa ankaopsa dziko la anthu amoyo. (Sheol )
Na da amo fi dunu da bogoi soge amoga mae sa: ima: ne amola bogosu ea gasaga mae fama: ne, hamedafa gaga: mu. Bogosu! Dia olo gia: su amo oule misa! Bogoi soge! Dia wadela: su oule misa! Na da amo dunu fi ilima bu hame asigimu. (Sheol )
“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda; ndidzawawombola ku imfa. Kodi iwe imfa, miliri yako ili kuti? Kodi iwe manda, kuwononga kwako kuli kuti? “Sindidzachitanso chifundo, (Sheol )
Ilia da uli dogone, gudu sa: ili, bogoi sogega doaga: sea, Na da ili hogole ba: mu. Ilia da muagado heda: sea, Na da ili ba: mu. (Sheol )
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko. (Sheol )
E amane sia: i, “Hina Gode! Na da se bagadedafa nababeba: le, Dima wele sia: ne gadoi. Amola Dia na sia: ne gadobe amo nabalu, dabe i. Na da soge wadela: i ganodini esalu, amo da dunu bogogia: su soge diala, amola na Dia fidima: ne di. Amola na dibi amo di nabi dagoi. (Sheol )
Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol )
Bagade gagui hou da ogogosu agoane. Uwasu dunu da gasa fili, helefisu hame dawa: Ilia da bogosu defele-sadisu hame dawa: Amaiba: le, ilisu gagumusa: , fifi asi gala hasalili, mae fisili, eno amola eno agoane hasalimusa: ahoa. (Sheol )
Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo; ndi wodzitama ndiponso wosakhazikika. Pakuti ngodzikonda ngati manda, ngosakhutitsidwa ngati imfa, wadzisonkhanitsira mitundu yonse ya anthu ndipo wagwira ukapolo anthu a mitundu yonse. (Sheol )
Be wali Na da dilima sia: sa, ‘Nowa dunu da ea na: iyadoma ougi galea, e da fofada: mu. Nowa da ea na: iyado ea hou fonobosea, e da fofada: su dunuma doaga: mu. Nowa da ea na: iyadoma ‘Di da gagaoui!’ sia: sea, e da Helo lalu ba: mu agoai galebe.’ (Geenna )
Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wokwiyira mʼbale wake adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene wonena mʼbale wake kuti, ‘Ndiwe wopanda phindu,’ adzapezeka wolakwa ku bwalo la milandu lalikulu. Ndipo aliyense amene anganene mnzake ‘wopandapake’ adzatengeredwa ku bwalo la milandu. Ndiponso aliyense amene angamunene mnzake kuti, ‘Chitsiru iwe,’ adzaponyedwa ku gehena. (Geenna )
Dia sidafa da dia hou wadela: sea, amo si di duga: le fasima. Dia da: i hodo huluane Helo sogega doaga: sa: besa: le, dia da: i hodo liligi fonobahadi afae fawane fisimu da defea. (Geenna )
Ngati diso lako lakumanja likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
Dia lobodafa da dia hou wadela: sea, amo lobo di damuni fasima. Dia da: i hodo huluane Helo sogega dasa: besa: le, liligi fonobahadi afae fawane fisimu da defea. (Geenna )
Ndipo ngati dzanja lako lamanja likuchimwitsa, ulidule ndi kulitaya. Pakuti nʼkwabwino kwa iwe kutaya chiwalo chimodzi cha thupi lako, kusiyana ndi kuti thupi lonse liponyedwe mʼgehena. (Geenna )
Dilia da: i hodo bogoma: ne medosu dunu ilima mae beda: ma. Be Gode da a: silibu amola da: i hodo gilisili Helo sogega wadela: mu dawa: beba: le, Godema beda: mu da defea. (Geenna )
Musamaope amene amapha thupi koma sangathe kuchotsa moyo. Koma muziopa Iye amene akhoza kupha mzimu ndi kuwononga thupi mu gehena. (Geenna )
Gabena: iame fi! Dilia da muagado heda: ma: bela: ? Hame mabu! Dilia da Helo sogega gudu sa: imu. Sodame dunu ilia da dilia waha ba: i liligi ba: loba, Sodame da mae ulagili dialala: loba. (Hadēs )
Ndipo iwe Kaperenawo, kodi udzakwezedwa kufika kumwamba? Ayi, udzatsitsidwa mpaka pansi kufika ku Hade. Ngati zodabwitsa zimene zinachitika mwa iwe, zikanachitika mu Sodomu, bwenzi iye alipo kufikira lero. (Hadēs )
Nowa da Dunu Egefema lasogole sia: sea, bu fofada: sea, ea hou da gogolema: ne olofoi dagoi ba: mu. Be Gode Ea A: silibu Hadigidafa gala Ema lasogole sia: sea, gogolema: ne olofosu da hame ba: mu. Wali osobo bagade eso amola fa: no misunu eso huluane ganodini, gogolema: ne olofosu hamedafa ba: mu. (aiōn )
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn )
Hawa: aya: gaga: nomei sogega bugi, da Gode Ea sia: nabasu dunu eno agoane. E da se nababeba: le amola osobo bagade hou amola muni hanai hou bagade dawa: beba: le, Gode Ea Sia: ea dogo ganodini diala da amoga bagade gigisiba: le, e da dulu hame legesa. (aiōn )
Zimene zinafesedwa pakati pa minga, ndi munthu amene amamva mawu koma nkhawa za moyo uno ndi chinyengo cha chuma zimalepheretsa mawuwo kuti abale chipatso. (aiōn )
Wadela: i gisi bugisu dunu da Sa: ida: ne. Faimu Eso da soge wadela: mu eso. Faisu dunu da a: igele dunu. (aiōn )
Ndipo amene anafesa namsongole ndi Satana. Kukolola ndiko kutha kwa dzikoli ndipo otuta ndi angelo. (aiōn )
Gisi da gilisili laluga ulagibi, agoaiwane hou ninia da soge wadela: mu eso doaga: sea ba: mu. (aiōn )
“Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. (aiōn )
Amo hou da soge wadela: mu eso amoga ba: mu. A: igele dunu da misini, dunu fi ganodini ida: iwane dunu yolesili, wadela: i dunu lidili, (aiōn )
Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. (aiōn )
Na da dima sia: sa! Dia dio dawa: loma: ne da ‘igi’. Amo igi da: iya Na da Na Fa: no Bobogesu Fi gasawane gagumu. Amasea, Ha: idisi da Na fi ilima hame osa: la heda: mu. (Hadēs )
Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs )
Dia lobo ea hou o dia emo ea hou hamobeba: le, di da wadela: le hamosea, di da eso huluane mae haba: dole nenanebe lalu ganodini, dia lobo adunawane amola emo adunawane ahoasa: besa: le, dia emo o lobo damuni fasima. Di da Fifi Ahoanusu ganodini lobo o emo afaewane masunu da defea. (aiōnios )
Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios )
Dia siga ba: beba: le dafamu galea, defea, dia si duga: le fasima. Di da si afadafa fawane Fifi Ahoanusu amo ganodini masunu da defea. Be si adunawane gala amo Helo laluga ha: digi dagoi ba: mu da defea hame. (Geenna )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna )
Eso afaega, dunu afae da Yesuma misini, amane sia: i, “Olelesu! Na da eso huluane Fifi Ahoanusu ba: ma: ne, adi ida: iwane hou hamoma: bela: ?” (aiōnios )
Taonani mnyamata wina anabwera kwa Yesu namufunsa kuti, “Aphunzitsi, ndi chinthu chiti chabwino chimene ndiyenera kuchita kuti ndipeze moyo wosatha?” (aiōnios )
Sia: eno diala. Nowa dunu da Nama asigiba: le, ea diasu, ola, eya, aba, eda, eme, mano o soge fisi galea, e da amo liligi 100 agoane lamu, amola eso huluane mae bogole, Fifi Ahoanusu lamu. (aiōnios )
Ndipo aliyense amene wasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena bambo kapena mayi kapena mkazi, kapena ana, kapena minda chifukwa cha Ine adzalandira madalitso ochuluka ndi kulandiranso moyo wosatha. (aiōnios )
E da figi ifa logo bega: ba: beba: le, ha: i manu faimusa: , figi ifa baia doaga: i. Be dulu hame ba: i, lubi fawane ba: i. Amaiba: le, Yesu da amo figi ifa amoma amane sia: i, “Di da hobea dulu bu hamedafa legemu.” Amalalu, figi ifa da hedolodafa bioi dagoi ba: i. (aiōn )
Ataona mtengo wamkuyu mʼmbali mwa msewu, anapitapo koma sanapeze kanthu koma masamba okhaokha. Pamenepo anati kwa mtengowo, “Usadzabalenso chipatso!” Nthawi yomweyo mtengowo unafota. (aiōn )
Dilia Sema olelesu dunu amola Fa: lisi dunu da se iasu bagade ba: mu! Dabua fawane molole ogogosu dunu! Dilia lalegagui dunu afadafa hamomusa: , hano wayabo bagadega amola osobo bagadega lala. Dunu afadafa dilia hou lalegaguli, ea Helo sa: imu logo dilia fodobeba: le, ea wadela: i hou da dilia wadela: i hou baligisa. (Geenna )
“Tsoka kwa inu, aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi, achiphamaso! Mumayenda maulendo ambiri pa mtunda ndi pa nyanja kuti mutembenuze munthu mmodzi, ndipo akatembenuka, mumamusandutsa kukhala mwana wa gehena kawiri kuposa inu. (Geenna )
Wadela: i sania fi! Dilia da Helo se iasu sogega mae doaga: ma: ne, hobeamu logo hamedafa ba: mu. (Geenna )
“Njoka inu! Ana amamba! Mudzachithawa bwanji chilango cha gehena? (Geenna )
Yesu da Olife Goumia esaloba, Ea ado ba: su dunu da wamowane Ema misini, amane adole ba: i, “Dia waha olelei da habogala doaga: ma: bela: ? Dia bu misunu eso amola soge wadela: mu eso da gadenene doaga: lalu, ninia adi dawa: digima: ne olelesu ba: ma: bela: ?” (aiōn )
Pamene Yesu anakhala pansi pa phiri la Olivi, ophunzira ake anabwera kwa Iye mwamseri nati, “Tiwuzeni, kodi izi zidzachitika liti, ndipo chizindikiro cha kubwera kwanu ndi zizindikiro za kutha kwa dziko zidzakhala chiyani?” (aiōn )
Amasea dunu Ea lobo fofadidili esala, ilima E da amane sia: mu, ‘Dilia Gode Ea gagabusu aligima: ne lai dunu! Masa! Eso huluane nenanumu lalu, Sa: ida: ne amola ea a: igele dunu se iasu ima: ne Gode hamoi, amoga masa! (aiōnios )
“Pamenepo adzanena kwa akumanzere kwake kuti, ‘Chokani kwa Ine, inu otembereredwa, pitani ku moto wosatha wokonzedwera mdierekezi ndi angelo ake. (aiōnios )
Amalalu, ilia da eso huluane mae dagole se iasu ba: lalumu. Be hou ida: iwane dunu da eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu lamu.” (aiōnios )
“Amenewa adzapita ku chilango chosatha pamene olungama ku moyo wosatha.” (aiōnios )
Ilia da Na dilima olelei liligi huluane nabawane hamoma: ne, amo ilima olelema. Dilia ba: ma! Na da dili mae yolelewane ouligilalea, soge wadela: mu eso da doaga: mu.” Sia: Ama Dagoi (aiōn )
ndi kuwaphunzitsa amvere zonse zimene ndinakulamulirani. Ndipo onani, Ine ndidzakhala pamodzi ndi inu kufikira kutha kwa dziko lapansi pano.” (aiōn )
Be nowa dunu da Gode Ea A: silibu Hadigidafa Gala amoma lasogole sia: sea, e da gogolema: ne olofosu hamedafa ba: mu. Ea wadela: i hou da mae fisili eso huluane dialalalumu.” (aiōn , aiōnios )
koma aliyense amene achitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa pakuti wachita tchimo losatha.” (aiōn , aiōnios )
Be osobo bagade hou dawa: beba: le, muni amola liligi hanaiba: le, amo sia: da goe dunu ea dogo ganodini gigisiba: le, e da ha: i manu fage hame legesa. (aiōn )
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn )
Amaiba: le, dia lobo ea hamobe amo dia hou wadela: sa: besa: le, defea, dia lobo damuni fasima. Di da lobo afaewane Fifi Ahoanusu lamu da defea. Be lobo adunawane Helo sogega lalu mae haba: dole nenanebe amoga sa: imu da defea hame galebe. (Geenna )
Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna )
Dia emo ea hamobe da dia hou wadela: musa: dawa: sea, defea, dia emo damuni fasima. Di gasuga: igiwane Fifi Ahoanusu lamu da defea. Be di emo aduna ida: iwane gala Helo sogega sa: imu da defea hame galebe. (Geenna )
Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna )
Dia si da dia hou wadela: mu ba: sea, amo duga: le fasima. Di da si afaewane Gode Ea Hinadafa Hou heda: mu da defea. Be di si adunawane Helo sogega sa: imu da defea hame galebe. (Geenna )
Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna )
Yesu da bu logoga ahoanoba, dunu afae da hehenane, Ema doaga: le, muguni bugili, Ema amane adole ba: i, “Olelesu ida: iwane! Na da eso huluane Fifi Ahoanusu ba: ma: ne, adi hamoma: bela: ?” (aiōnios )
Yesu atanyamuka, munthu wina anamuthamangira nagwa mogwada pamaso pake. Iye anafunsa kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
e da osobo bagade esoga wali diasu, yolali, aba, eme, mano amola soge100agoane bu lamu. Eno dunu da ema higabeba: le, e da osobo bagadega se nabimu, be fa: no mabe esoga eso huluane Fifi Ahoanusu ba: mu. (aiōn , aiōnios )
adzalephera kulandira 100 (nyumba, abale, alongo, amayi, ana ndi minda, pamodzi ndi mazunzo) mʼbado uno ndi moyo wosatha nthawi ya mʼtsogolo. (aiōn , aiōnios )
Amaiba: le, Yesu da amo figi ifama amane sia: i, “Dia ha: i manu amo dunu ilia da hobea hamedafa manu!” Ea ado ba: su dunu ilia da amo sia: nabi dagoi. (aiōn )
Ndipo Iye anati kwa mtengo, “Palibe amene adzadyenso chipatso kuchokera kwa iwe.” Ndipo ophunzira ake anamva Iye akunena izi. (aiōn )
E da eso huluane mae fisili, Ya: igobe egaga fi, ilima Hinawane esalumu. Ea Hinadafa Hou da hamedafa dagomu.” (aiōn )
ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” (aiōn )
E da A: ibalaha: me amola ea fi huluane ilima Ea asigi amola gogolema: ne olofosu hou olelei. Amo hou E da mae fisili, eso huluane hamonanumu.” (aiōn )
Kwa Abrahamu ndi zidzukulu zake ku nthawi zonse monga ananena kwa makolo athu.” (aiōn )
E da hemonega, Ea balofede dunu ilia lafidili amane ilegele sia: i, (aiōn )
(Monga mmene ananenera kudzera mwa aneneri oyera), (aiōn )
Yesu da ili “Abisi” (wadela: i a: silibu se iasu diasu) amoga mae asunasima: ne, Fio liligi huluane da Yesuma ha: giwane adole ba: i. (Abyssos )
Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. (Abyssos )
Gabena: iame fi! Dilia Hebene diasuga heda: musa: dawa: bela? Dilia da Helo sogega gudu sa: imu.” (Hadēs )
Kodi iwe Kaperenawo, adzakukweza mpaka kumwamba? Ayi, adzakutsitsa mpaka ku Malo a anthu akufa. (Hadēs )
Eso afaega, sema olelesu dunu da Yesu dafama: ne, wa: legadole, Ema amane sia: i, “Olelesu! Na da Fifi Ahoanusu lama: ne, adi hamoma: bela?” (aiōnios )
Nthawi ina katswiri wa malamulo anayimirira kuti ayese Yesu. Iye anati, “Aphunzitsi, ndichite chiyani kuti ndikhale ndi moyo wosatha?” (aiōnios )
Be afadafa fawane beda: ma! Dunu afadafa esala. E da dunu ea da: i hodo medole legele, ea a: silibu Helo sogega galadigimu dawa: Dafawane! Amo dunuma beda: ma! (Geenna )
Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna )
Amalalu, ogogosu muni ouligisu dunu da dawa: iwane hamoiba: le, ea hina da ema nodone sia: i. Bai osobo bagade dunu ilia muni ouligisu hou da hadigi lai dunu ilia muni ouligisu hou baligisa. (aiōn )
“Bwana anayamikira kapitawo wosakhulupirikayo popeza anachita mochenjera. Pakuti anthu a dziko lino lapansi ndi ochenjera kwambiri akamachita zinthu ndi anthu ofanana nawo kuposa anthu a kuwunika. (aiōn )
Amaiba: le na dilima sia: sa. Muni da osobo bagade liligi fawane. Be osobo bagade dunu da dilima asigima: ne, muni ouligisu hou noga: le hamoma. Agoane hamosea, hobea amo hou da dagoiwane ba: beba: le, Gode da dilima misa: ne sia: beba: le, dilia da Hebene sogega doaga: sea, ilia dima hahawane yosia: mu. (aiōnios )
Ine ndikukuwuzani inu, gwiritsani ntchito chuma cha dziko lapansi kuti mudzipezere nokha abwenzi, kuti pamene chatha mudzalandiridwe mʼmalo okhala amuyaya. (aiōnios )
Bagade gagui dunu da Ha: idisi amo ganodini se nabawane esalu. E da ea si ba: le gadole, A:ibalaha: me sedagawane lelebe ba: i. La: salase da A: ibalaha: mela dafulili lelebe ba: i. (Hadēs )
Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. (Hadēs )
Isala: ili ouligisu dunu afae da Yesuma amane adole ba: i, “Olelesu ida: iwane gala! Na da eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu lama: ne, adi hamoma: bela: ?” (aiōnios )
Oweruza wina wake anamufunsa Iye kuti, “Aphunzitsi abwino, ndichite chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?” (aiōnios )
e da osobo bagadega esalea, amo liligi fisi baligiliwane bu lamu, amola fa: no fifi misunu amo esoga, e da mae bogole, Eso Huluane Fifi Ahoanusu lamu.” (aiōn , aiōnios )
adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
Yesu E bu adole i, “Waha esala dunu amola uda ilia da uda lasu hou dawa: (aiōn )
Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. (aiōn )
Be nowa dunu amola uda ilia da bogole, bu wa: legadole, Eso Huluane Mae Bogole Fifi Ahoanusu lamusa: , Gode da defelewane ba: sea, amo dunu da uda hame lamu, amola amo uda da dunuma hame fimu. (aiōn )
Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa. (aiōn )
Dunu huluane amo da Dunu Egefe Ea hou dafawaneyale dawa: sea, eso huluane Fifi Ahoanusu lama: ne, amo hou da doaga: mu. (aiōnios )
kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Bai Gode da osobo bagade fifi asi gala hodole, ilima asigili, Egefe ilima i. Ea sia: dafawaneyale dawa: sea, lalegagusia, eso huluane mae bogole Fifi Ahoanumu. (aiōnios )
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Nowa da Gode Egefe dafawaneyale dawa: sea, e da eso huluane Fifi Ahoanusu lai dagoi. Be nowa da Gode Egefe Ea sia: hame nabawane hame hamosea, e da eso huluane Fifi Ahoanusu mae lale, Gode Ea ougi se iasu ba: mu agoai galebe!” (aiōnios )
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios )
Be nowa da Na hano dili iasu nasea, e da hobea gumiba: le, bu hano hame hanamu. Be hano ea dogo ganodini heda: lebeba: le, nawa: li agoane dalebeba: le, eso huluane mae bogole, Fifi Ahoanusu hou ema imunu.” (aiōn , aiōnios )
koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
Nowa dunu da yoi liligi faisia, e da bidi lale, ea fai liligi da eso huluane Fifi Ahoanusu ba: mu. Amaiba: le, bugi dunu amola faisu dunu, da gilisili hahawane ganumu. (aiōnios )
Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios )
Na da dilima dafawane sia: sa. Nowa da Na sia: nabasea amola Na Asunasisu Dunu amo Ea hou dafawaneyale dawa: sea, amo dunu da eso huluane Fifi Ahoanusu lai dagoi. E da se imunusa: fofada: su mae hamone, bogosu sogebi yolesili, degele, eso huluane Fifi Ahoanusu sogebi amoga doaga: i dagoi. (aiōnios )
“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo. (aiōnios )
Dilia da Fifi Ahoanusu lamusa: Gode Sia: Dedei idilala. Be amo sia: da Na hou fawane olelesa. (aiōnios )
Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. (aiōnios )
Hedolo wadela: mu ha: i manu amo lama: ne, mae hawa: hamoma. Be ha: i manu mae dasale, Fifi Ahoanusu imunu liligi, amo lama: ne hawa: hamoma. Gode, Adadafa, da Dunu Egefe ilegei dagoiba: le: , Dunu Egefe da amo ha: i manu dilima imunu.” (aiōnios )
Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios )
Bai Na Ada da agoane hanai gala. Nowa dunu da Gode Eagofedafa Ea hou dafawaneyale dawa: sea, lalegagusia, huluane da Fifi Ahoanusu lamu., amola soge wadela: mu eso amoga Na da amo dunu wa: legadolesimu.” (aiōnios )
Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios )
Na da dilima dafawane sia: sa! Nowa da dafawaneyale dawa: sea, e da Fifi Ahoanusu lai dagoi. (aiōnios )
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios )
Na da Agi Esalebe agoane muagadonini guiguda: sa: i. Nowa da amo agi nasea, e da mae bogole, eso huluane esalalalumu. Agi Na da ema imunu liligi da Na hu. Amo da osobo bagade fi dunu ilia esaloma: ne, Na da iaha.” (aiōn )
Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn )
Be nowa da Na hu nasea amola Na maga: me nasea, e da eso huluane Fifi Ahoanusu lai dagoi. Amola Na da soge wadela: mu eso amoga amo dunu esaloma: ne wa: legadolesimu. (aiōnios )
Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios )
Amaiba: le, noga: le dawa: ma! Na sia: i liligi da agidafa muagado misi. Dilia aowalali fi dunu da ma: na mai dagoi be huluane da fa: no bogoi. Nowa da Na sia: i agi agoane nasea, e da mae bogole eso huluane Fifi Ahoanumu.” (aiōn )
Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn )
Saimone Bida da bu adole i, “Hina! Ninia nowa dunuma masa: bela: ? Disu da eso huluane Fifi Ahoanusu Sia: gagui gala. (aiōnios )
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios )
Udigili hawa: hamosu dunu da sosogo fi ganodini eso huluane esalumu hamedei. Be amo sosogo fi dunu mano lalelegei, amo da ea fidafa amo ganodini mae fisili, esalumu. (aiōn )
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn )
Na dilima dafawane sia: sa. Nowa da Na olelesu nabawane hamosea, e da bogosu hamedafa ba: mu.” (aiōn )
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn )
Ilia da Ema amane sia: i, “Defea! Wali ninia hananewane dawa: Di da Fio liligi gala. A: ibalaha: me da bogoi dagoi, amola balofede dunu huluane, ilia bogoi. Be Di da nowa dunu da Dia olelesu nabasea hame bogomu amo ogogolewane olelesa. (aiōn )
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn )
Osobo bagade degabo hahamosu esoha amola fa: no, si dofoi dunu ea si bu hahamoi amo hou da hamedafa ba: su. (aiōn )
Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn )
Na da ilima eso huluane Fifi Ahoanusu iabeba: le, ilia da mae bogole fifi ahoanumu. Ilia da Na lobo ganodini gaguiba: le, enoga bu samogemu da hamedei galebe. (aiōn , aiōnios )
Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. (aiōn , aiōnios )
Nowa esala dunu da Na sia: dafawaneyale dawa: sea, e da mae bogole esalalalumu. Amo sia: di dafawaneyale dawa: bela: ?” (aiōn )
Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn )
Nowa dunu da ea esalusu gagumusa: hanai galea, e da ea esalusu fisimu. Be nowa dunu ea osobo bagade esalusu amoma hame asigisia, e da ea esalusu bu lale, Fifi Ahoanusu ba: mu. (aiōnios )
Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios )
Dunu huluane bu adole i, “Ninia sema ganodini, Mesaia da mae bogole, eso huluane esalalalumu, amo dedei diala. Amaiba: le, osobo bagade dunu ilia Dunu Egefe gaguia gadomu, Di abuliba: le sia: dalula: ? Dunu Egefe da nowa dunula: ?” (aiōn )
Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn )
Na Ada Ea sia: da eso huluane Fifi Ahoanusu iaha, amo Na dawa: Amaiba: le, Na Ada da musa: Nama adoi liligi, amo fawane Na da olelesa!” (aiōnios )
Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios )
Bida e bu sia: i, “Na emo Di da hamedafa dodofemu.” Be Yesu E bu adole i, “Dia emo Na hame dodofesea, di da Na fi ganodini esalumu hamedei.” (aiōn )
Petro anati, “Ayi, Inu simudzandisambitsa konse mapazi anga.” Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine sindisambitsa mapazi ako, ulibe gawo mwa Ine.” (aiōn )
Na da Edama adole ba: muba: le, E da Fidisu eno Na defele, dilima imunuyo. E da eso huluane mae yolesili, dili fidilalumu. (aiōn )
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn )
Bai E da fifi asi gala dunu huluane ilima Hinadafa esaloma: ne, Di da Ema gasa i dagoi. E da dunu huluane amo Di da Ema i, ilima Fifi Ahoanusu ima: ne, amo gasa Ema i. (aiōnios )
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios )
Fifi Ahoanusu ea bai da Disu da Godedafa esala amo dawa: mu, amola Di da Yesu Gelesu asunasi dagoi. (aiōnios )
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios )
Dia da na a: silibu bogoi sogebi amoga hame yolesimu. Na da Di mae yolesili hawa: hamosu dunu esala. Amaiba: le, Di da na da: i hodo dasama: ne, bogoi uli dogoiga hame yolesimu (Hadēs )
Chifukwa simudzasiya moyo wanga kumalo a anthu akufa, ku manda, kapena kulekerera Woyerayo kuti awole. (Hadēs )
Da: ibidi da Gode Ea fa: no hamomu hou ba: beba: le, e da Mesaia Ea bu uhini wa: legadomu olelei amane, “Gode da bogosu sogebi amo ganodini amo dunu hame yolesi. Ea da: i hodo da bogoi uli dogoi ganodini dasai hame ba: i.” (Hadēs )
Davide ataoneratu zimene zinali mʼtsogolo anayankhula za kuuka kwa Khristu, kuti Iye sanasiyidwe mʼmanda, ndipo thupi lake silinawole. (Hadēs )
Bai E da wali Hebene soge amo ganodini esala! Be balofede dunu da hemonega amo Gode da liligi huluane gaheabolo hamomu sia: i. Amo eso doaga: sea, Yesu Gelesu da bu misunu. (aiōn )
Iye ayenera kukhalabe kumwamba mpaka nthawi ya kukonzanso zinthu zonse monga Mulungu analonjeza kale kudzera mwa aneneri ake oyera mtima. (aiōn )
Be Bolo amola Banaba: se, ela mae beda: ne gasa bagadewane sia: i, “Dilia Yu dunu da hidadea Gode Ea sia: nabi dagoi. Bai Gode da amo ilegei dagoi. Be dilia amo sia: hihiba: le, dilia eso huluane Fifi Ahoanusu lamu dilia defele hame dawa: beba: le, defea, ninia dili fisili asili, Dienadaile dunuma olelemu. (aiōnios )
Ndipo Paulo ndi Barnaba anawayankha molimba mtima kuti, “Ife tinayenera kuyankhula Mawu a Mulungu kwa inu poyamba. Popeza inu mwawakana ndi kudziyesa nokha osayenera moyo wosatha, ife tsopano tikupita kwa anthu a mitundu ina. (aiōnios )
Amo sia: nababeba: le, Dienadaile dunu da hahawane bagade ba: beba: le, Gode Ea Sia: amoma nodoi. Amola nowa dunu da eso huluane Fifi Ahoanusu lama: ne Gode da ilegei dagoi, amo dunu da Yesu Ea hou lalegagui. (aiōnios )
Anthu a mitundu ina atamva izi, anakondwa ndipo analemekeza Mawu Ambuye; ndipo onse amene anawasankha kuti alandire moyo osatha anakhulupirira. (aiōnios )
Hina Gode da amo sia: sa. E da musa: hemonega olelei dagoi.’” (aiōn )
zinaululidwa kuyambira kalekale.’ (aiōn )
Degabo, Gode da osobo bagade hahamoi amola fa: no eso huluane, amo esoga dunu huluane da Gode Ea hou, dunu ilia siga hame ba: su hou, amo huluane dawa: su. Gode Ea hahamoi liligi ba: beba: le, Gode da hadigidafa amola E da eso huluane esalalala, amo ilia dawa: i galu. Amaiba: le, amo dunu ilia hame nabasu hou abalomu da hamedei. (aïdios )
Pakuti kuyambira pamene dziko lapansi linalengedwa, zinthu zosaoneka za Mulungu, mphamvu zake zosatha ndi chikhalidwe cha umulungu, zakhala zikuoneka bwinobwino. Akhala akuzindikira poona zimene Mulungu analenga, kotero kuti anthu sangathe kuwiringula. (aïdios )
Gode Ea moloidafa hou yolesili, ilia ogogosu hou lalegagusa. Osobo Bagade Hahamoi Dunu Ema nodone sia: ne gadosu hou amola hawa: hamosu hou yolesili, ilia bu Gode Ea hahamoi liligi amoma sia: ne gadosa amola hawa: hamosa, Be Osobo Bagade Hahamoi Gode Ema mae yolesili eso huluane nodone sia: ne gadolalumu da defea. Ama. (aiōn )
Iwo anasinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza ndipo anapembedza ndi kutumikira zinthu zolengedwa mʼmalo mwa Mlengi amene ali woyenera kutamandidwa mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Dunu mogili ilia da eso huluane hawa: moloidafa hamonana. Ilia hadigi hou, Godema nodosu hou amola eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu hogoi helesa. Gode da ilima eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu imunu. (aiōnios )
Iye adzapereka moyo wosatha kwa amene amafunafuna ulemerero, ulemu ndi moyo pochita ntchito zabwino mopirira. (aiōnios )
Amaiba: le, musa: bogosu da doaga: beba: le, wadela: i hou da osobo bagade dunuma ouligisuwane dialu. Amo defele wali hou moloidafa da doaga: beba: le, Gode Ea hahawane moloidafa asigi hou da ilima ouligisuwane diala. Ninia amo hou lalegagusia, Hina Gode Yesu Gelesu da fidibiba: le, ninia da Eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu ba: mu. (aiōnios )
Choncho monga momwe tchimo linkalamulira anthu ndi kubweretsa imfa pa iwo, chomwecho kunali koyenera kuti chisomo chilamulire pobweretsa chilungamo kwa anthu, ndi kuwafikitsa ku moyo wosatha mwa Yesu Khristu Ambuye athu. (aiōnios )
Be wali dilia wadela: i hou se iasu diasu logo da doasibiba: le, dilia da Gode Ea udigili hawa: hamosu dunu esala. Dilia bidi waha labe da eso huluane dilia hou afadenene bu asigilasa, amola hobea Eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu ba: mu. (aiōnios )
Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Bai wadela: i hou hamosu ea bidi da bogosu fawane! Be Gode Ea hahawane dogolegele iasu da Hina Gode Yesu Gelesu amoma madelagiba: le, eso huluane mae bogole Fifi Ahoanumu. (aiōnios )
Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios )
Ilia da musa: Hibulu siba fi dunu bagade amo ilia mano esala. Yesu Gelesu da osobo bagade dunu ea da: i hodo lale, ilia fi amo ganodini lalelegei. Gode da liligi huluane amoma ouligisuwane esalebeba: le, Ema eso huluane nodonanumu da defea. Ama. (aiōn )
Awo ndi makolo athu. Kuchokera kwa iwo mʼthupi ndi kumene kunachokera makolo a Khristu Yesu amene ndi Mulungu wolamulira zinthu zonse, alemekezeke mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
Eno da amane adole ba: mu da defea hame, “Nowa da bogoi soge amoga gudu sa: ima: bela: ?” (Bai Gelesu Ea bu bogole, wa: legadolesimu da hamedei.) (Abyssos )
“kapena ‘Ndani adzatsikira ku dziko la anthu akufa?’” (ndiko, kukamutenga Khristu kwa akufa). (Abyssos )
Gode da dunu huluanedafa ilima Ea udigili gogolema: ne olofosu hou olelema: ne, E da dunu huluane hame nabasu se iasu udigili hawa: hamosu dunu agoane hamoi dagoi. (eleēsē )
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse. (eleēsē )
Bai E da liligi huluanedafa hahamoi dagoi. E hahawane ba: ma: ne, liligi huluanedafa diala. Ninia Godema mae yolesili nodonanumu da defea. Ama. (aiōn )
Pakuti zinthu zonse nʼzochokera kwa Iye, nʼzolengedwa ndi Iye ndipo zimabweretsa ulemerero kwa Iye. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya! Ameni. (aiōn )
Dilia osobo bagade dunu ilia hou defele mae hamoma! Be Gode da dilia asigi dawa: su bu afadenene moloidafa hamomusa: hanaiba: le, amo E hamoma: ne, dilia logo fodoma. Amasea, dilia da Gode Ea hanai asigi dawa: su dawa: mu. Dilia da hou moloidafa amola hou amo Gode da hahawane ba: sa, amo noga: le dawa: mu. (aiōn )
Musafanizidwenso ndi makhalidwe a dziko lino koma musandulike pokonzanso maganizo anu. Ndipo mudzadziwa ndi kuzindikira chifuniro chabwino cha Mulungu chomwe ndi chokondweretsa ndi changwiro. (aiōn )
Gode da Hadigidafa! Ninia Ema nodomu da defea! Gode Ea Sia: Ida: iwane Gala, na da agoane olelesa. Amo da Yesu Gelesu Ea hou dafawanedafa hou musa: ode bagohame wamolegei agoane, be wali ninia ba: sa. Wali, balofede dunu ilia da amo dafawane hou dedeiba: le, sia: da hadigiga misi dagoi. Amola Gode da hamoma: ne sia: beba: le, dunu huluane ilia dafawaneyale dawa: beba: le nabasu hou hamoma: ne, dunu eno da osobo bagade fifi asi gala huluanema olelesa. Amo hou defele, dilia huluane dafawaneyale dawa: su hou amo ganodini gasawane leloma: ne, Gode da defele esala. (aiōnios )
Tsopano kwa Iye amene ali ndi mphamvu yokhazikitsa monga mwa uthenga wanga wabwino ndikulalikidwa kwa Yesu Khristu, monga mwa vumbulutso lachinsinsi chobisika kwa nthawi yayitali, (aiōnios )
Romans 16:26 (Aroma 16:26)
(parallel missing)
koma tsopano chavumbulutsidwa ndi kudziwika kudzera mʼMalemba a uneneri mwa lamulo la Mulungu wosatha, kuti mitundu yonse ikhulupirire ndi kumvera Iye, (aiōnios )
Gode Hi fawane da Gode Esala. Hi fawane da dawa: su huluane gagusa. Yesu Gelesu Ea hawa: hamobeba: le, ninia eso huluane mae yolesili Godema hadigi ima: ne, nodonanumu da defea. Ama. Sia: Ama Dagoi (aiōn )
kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni. (aiōn )
Amaiba: le, bagade dawa: su dunu, sugulu hamoi dunu amola sia: fofada: su bagade dawa: su dunu da wali hamedei agoane ba: sa. Gode Ea hamobeba: le, osobo bagade dunu bagade dawa: su hou da gagaoui hou agoai ba: sa. (aiōn )
Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi? (aiōn )
Be dunu ilia a: silibu hou da asigilai, ilima na da bagade dawa: su sia: olelesa. Be amo dawa: su sia: da osobo bagade dunu amola osobo bagade hina dunu amo ilia dawa: su hou defele hame. Amo osobo bagade dawa: su hou da mugululi hame ba: mu. (aiōn )
Komabe ife timayankhula uthenga wa nzeru kwa okhwima, koma osati ndi nzeru ya mʼbado uno kapena ya olamula a mʼbado uno, amene mphamvu yawo ikutha. (aiōn )
Na olelesu liligi da Gode Ea wamolegei dawa: su liligi. Amo da osobo bagade dunu mae ba: ma: ne wamolegei. Be osobo bagade hame hamoi esoga, Gode da amo dawa: su hou amoga hobea ninia hadigima: ne dawa: i galu. (aiōn )
Ayi, ife timayankhula za nzeru yobisika ya Mulungu, nzeru imene inabisidwa ndipo imene Mulungu anatikonzera mu ulemerero wathu isanayambe nthawi. (aiōn )
Osobo bagade hina dunu huluane ilia amo dawa: su hou hame dawa: i. Amo dawa: su hou ilia dawa: i ganiaba ilia da hadigi Hina Gode Yesu Gelesu bulufalegeiga hame medole legela: loba. (aiōn )
Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. (aiōn )
Dilia hou dilisu mae ogogoma! Nowa dunu da osobo bagade hou dawa: beba: le, hi da na bagade dawa: su hisu da dawa: sea, defea, amo dunu da ea hou fonobone, gagaoui agoane hamomu da defea. Amasea, e da bagade dawa: sudafa bu ba: mu. (aiōn )
Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. (aiōn )
Amaiba: le ha: i manu da na fi dunu ea wadela: i hou hamosu logo fodosa galea, na fi dunu da wadela: le hamosa: besa: le, na da fedege agoane bu ha: i manu huluane hamedafa manu. (aiōn )
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn )
Amo liligi huluane da eno dunu dawa: ma: ne, ilima doaga: i dagoi. Nini wali esalebe dunuma sisasu olelema: ne, amo sia: da dedei diala. Bai soge wadela: mu eso da gadenene, ninia dawa: (aiōn )
Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse. (aiōn )
Bogosu! Dia hasalasisu da habila: ? Bogosu! Dia ninima se imunu da hamedei galebe.” (Hadēs )
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs )
Wadela: i osobo bagade ‘gode’ (Sa: ida: ne) da ilia asigi dawa: su gasi agoane hamoiba: le, ilia dafawaneyale hame dawa: be. Hadigi ilima mabe, amo hadigi da Gode Sia: Ida: iwane gala. Gode Sia: da Yesu Gelesu E da Gode defele esala amo olelesa. Be wadela: i osobo bagade ‘gode’ da amo hadigi logo damusa: (aiōn )
Mulungu wa dziko lapansi anachititsa khungu anthu osakhulupirira, kuti asathe kuona kuwala kwa Uthenga Wabwino umene umaonetsa ulemerero wa Khristu, amene ndi chifaniziro cha Mulungu. (aiōn )
Ninia waha se nabasu da fonobahadi amola waha fawane. Hobea amo houba: le, ninia bidi amo waha hou bagadewane baligi, eso huluane hame dasasu liligi lamu. (aiōnios )
Pakuti masautso athu ndi opepuka ndi a kanthawi, koma akutitengera ulemerero wamuyaya umene ndi wopambana kwambiri. (aiōnios )
Bai ninia da ba: su liligi mae dawa: le, hame ba: su liligi dawa: beba: le, bidi lamu. Siga ba: su liligi da eso bagahame ba: lalu, fisimu. Be hame ba: su liligi da eso huluane mae fisili dialalalumu. (aiōnios )
Motero sitiyangʼana zinthu zimene ndi zooneka ndi maso, koma zinthu zimene ndi zosaoneka. Pakuti zimene zimaoneka ndi zosakhalitsa, koma zimene sizioneka ndi zamuyaya. (aiōnios )
Fedege agoane, ninia da: i hodo da ninia osobo bagade diasu gala. Gode da amo mugulusia, e da Hebene soge amo ganodini eso huluane dialalalumu diasu, Hi fawane hamoi liligi ninima imunu, amo ninia dawa: (aiōnios )
Popeza tikudziwa kuti ngati msasa wa dziko lapansi umene tikukhalamo uwonongeka, tili ndi nyumba yochokera kwa Mulungu, nyumba yamuyaya yakumwamba, osati yomangidwa ndi manja a anthu. (aiōnios )
Gode Sia: da amane dedei diala, “E da hame gagui dunu ilima baligili iaha. Ea asigidafa hou da eso huluane dialalalumu.” (aiōn )
Paja analemba kuti, “Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya.” (aiōn )
Na da Hina Gode Yesu amo Ea Ada Gode (Ea Dioba: le eso huluane hahawane dogolegele nodonanumu da defea) Ema hame ogogosa, amo E dawa: (aiōn )
Mulungu, Atate a Ambuye Yesu, amene tiyenera kumutamanda nthawi zonse, akudziwa kuti sindikunama. (aiōn )
Yesu Gelesu da osobo bagade dunu ilia wali hou hamobe, amo ninia yolesima: ne, Ea esalusu yolesi dagoi. E da ninia wadela: i hou gogolema: ne olofomusa: , ninia Ada Gode Ea sia: nabawane, bogoi dagoi. (aiōn )
Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn )
Gode da eso huluane hadigiwane, mae dagole esalalalumu. Amo dawa: ma: ne, ninia Godema nodone sia: mu da defea. Ama. (aiōn )
Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
E da hi hanai hou ha: i manu hawa: agoane bugisia, e da fa: no bogosu fage agoane faimu. Be e da A: silibu hou dawa: beba: le, amo hou ha: i manu agoane bugisia, e da eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu fage agoane faimu. (aiōnios )
Pakuti amene amafesa zokondweretsa thupi lake la uchimo, kuchokera ku khalidwe limenelo adzakolola chiwonongeko; amene amafesa zokondweretsa Mzimu, kuchokera kwa Mzimu adzakolola moyo wosatha. (aiōnios )
Gelesu da wali Hebene ouligisu dunu huluane, gasa bagade ouligisu dunu amola hina dunu huluanedafa, ilima Ouligisudafa esala. Wali Yesu Gelesu Ea Dio da osobo bagade ganodini ouligisu dio asuli dunu amola fa: no misunu osobo gaheabolo ganodini ouligisu dio asulimu dunu, amo ouligisu dunu huluane ilia dio bagadewane baligisa. (aiōn )
Anamukhazika pamwamba pa ulamuliro onse ndi mafumu, mphamvu ndi ufumu, ndiponso pamwamba pa dzina lililonse limene angalitchule, osati nthawi ino yokha komanso imene ikubwerayo. (aiōn )
Amo esoga, dilia osobo bagade wadela: i hou amoma fa: no bobogei. Dilia wadela: i a: silibu hina dunu amo wali e da Gode sia: hame nabasu dunuma hina hamonana, amola hisi amo ganodini wadela: i a: silibuma hina hamonana, dilia ema fa: no bobogei. (aiōn )
mmene inu munkakhalamo pamene munkatsatira njira za dziko lapansi ndi za ulamuliro waufumu wa mlengalenga, mzimu umene ukugwira ntchito tsopano mwa amene samvera. (aiōn )
E da ninima bagadewane asigiba: le, Yesu Gelesu ninima i dagoi. E da fa: no misunu dunu huluanedafa ilia Ea hahawane dogolegele iasu hou noga: le ba: ma: ne, amo hou hamosu. (aiōn )
ndi cholinga chakuti mʼnthawi imene ikubwera, Iyeyo adzaonetse chuma choposa cha chisomo chake, choonetsedwa mwa kukoma mtima kwake kwa ife mwa Khristu Yesu. (aiōn )
Dunu huluane ilia Gode Ea musa: wamolegei ilegesu da wali osobo bagadega hawa: hamomu, amo ilia dawa: ma: ne, Gode, liligi huluane Hahamosu Dunu, da musa: ode huluane amoga amo hou wamolegei. (aiōn )
Ndinasankhidwa kuti ndifotokoze momveka bwino kwa munthu aliyense za chinsinsi chimenechi, chinsinsi chimene kuyambira kale chinali chobisika mwa Mulungu amene analenga zinthu zonse. (aiōn )
Gode da musa: amo hou hamomusa: ilegei dagoi. Amola E da Hina Gode Yesu Gelesu Ea hawa: hamobeba: le, hamoi dagoi. (aiōn )
Chimenechi chinali chikonzero chamuyaya cha Mulungu, chimene chinachitika kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōn )
Amaiba: le Yesu Gelesu Ea fa: no bobogesu fi amo ganodini amola Yesu Gelesu Ea hou amo ganodini, Gode Ea hadigidafa hou eso huluane mae dagole dialalaloma: ne, ninia sia: ne gadomu da defea. Ama. (aiōn )
Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Bai ninia da hu amola maga: mega hamoi osobo bagade dunu ilima hame gegesa. Be wadela: i a: silibu hisi amo ganodini esala amola gasi ea hina dunu amola wadela: i gasa bagade hou ouligisu a: silibu muagado ganodini, ilima gegenana. (aiōn )
Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. (aiōn )
Ninia Ada Godema eso huluane mae dagole nodonanumu da defea. Ama. (aiōn )
Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Amo hou musa: hemone, dunu huluane mae ba: ma: ne, Gode da wamolegei. Be wali E da Ea fi dunuma amo wamolegei hou olelei dagoi. (aiōn )
chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima. (aiōn )
Be dilima se iasu dunu, amo ilia se dabe iasu ba: mu. Ilia se dabe iasu da ilia eso huluane gugunufinisi dagoi ba: mu, amola eso huluane ilia da Hina Gode amola ea gasa bagade hadigi hou amoma afafai dagoi ba: mu. (aiōnios )
Adzalangidwa ndi chiwonongeko chamuyaya ndipo sadzaonanso nkhope ya Ambuye ndi ulemerero wamphamvu zake (aiōnios )
Ninia Hina Gode Yesu Gelesu amola ninia Ada Gode, amo da ninima asigi galu amola ninima hahawane dogolegele iasu iabeba: le, ninia da mae beda: iwane hobea dafawane hamoma: beyale dawa: lusu lai dagoi. (aiōnios )
Ambuye athu Yesu Khristu mwini ndi Mulungu Atate wathu, amene anatikonda ife ndipo mwachisomo chake anatipatsa kulimba mtima kwamuyaya ndi chiyembekezo chabwino, (aiōnios )
Be Yesu Gelesu da wadela: i dunu fidima: ne, Ea asigidafa hou amo eno dunu ilia fa: no Ea hou lalegaguli eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu dawa: mu, E da dawa: i galu. Amo dunu ilia da na gaga: i dagoi ba: ma: ne, Gode da nama gogolema: ne olofosu hou olelei. (aiōnios )
Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha. (aiōnios )
Amaiba: le, eso huluane Esalalala Hina Bagadedafa, E da bogosu hame dawa: , dunu ea siga hame ba: sa, Hi fawane da Godedafa, Ema hadigi ima: ne ninia eso huluane nodonanumu da defea. Ama. (aiōn )
Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Dafawaneyale dawa: su hehenasu amo ganodini di eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu lama: ne baligiliwane hehenama! Di da Yesu Gelesu Ea hou lalegagui dagoi, amo dunu bagohame ba: ma: ne di da ilegele sia: i dagoiba: le, Gode da di eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu lama: ne, dima wele sia: i dagoi. (aiōnios )
Menya nkhondo yabwino yachikhulupiriro. Gwiritsitsa moyo wosatha umene anakuyitanira pamene unavomereza bwino lomwe pamaso pa mboni zambiri. (aiōnios )
Hisu da esalalalusu Dunu. E da Hadigi (osobo bagade dunu da amo gadenenewane doaga: mu hamedei ba: sa) amo ganodini esala. Dunu afae da Gode hame ba: su amola ba: mu gogolei. Godema eso huluane nodonanumu da defea. E da eso huluane Hinawane esalalalumu da defea. Ama. (aiōnios )
Ndiye yekha wosafa ndipo amakhala mʼkuwala koopsa. Mulungu amene munthu aliyense sanamuone. Kwa Iye kukhale ulemu ndi mphamvu mpaka muyaya. Ameni. (aiōnios )
Dia bagade gagui dunu, ilima ilia hidale gasa fi mae hamoma: ne sia: ma! Be ilia hedolo dasasu liligima dawa: su hou yolesili, bu Gode (E da nini hahawane ba: ma: ne liligi huluane ninima iaha) amo Ea hou gasawane lalegaguma: ne sia: ma. (aiōn )
Anthu onse amene ali ndi chuma uwalamule kuti asanyade kapena kuyika mitima yawo pa chuma chimene nʼchosadalirika. Koma chiyembekezo chawo chikhale mwa Mulungu amene amatipatsa mowolowamanja zonse zotisangalatsa. (aiōn )
Ninia hawa: hamobeba: le hame, be E da hahawane dogolegele imunu hanaiba: le, Gode da nini gaga: le, Ea fidafa hamoi dagoi. Osobo bagade hame hahamoi eso amoga E da amo hahawane dogolegele iasu imunusa: dawa: i galu. E da Yesu Gelesu amo Ea hawa: hamomuba: le, amo ninima ilegemusa: dawa: i galu. (aiōnios )
Iye anatipulumutsa ndipo anatiyitanira ku moyo oyera mtima, osati chifukwa cha chilichonse chimene tinachita, koma chifukwa cha chikonzero ndi chisomo chake. Chisomo chimenechi anatipatsa ife mwa Khristu Yesu nthawi isanayambe. (aiōnios )
Amaiba: le, Gode Ea ilegei fi, ilia da Yesu Gelesu Ea gaga: su hou amola eso huluane esalalalusu hadigi lama: ne, amo hou fidimusa: , na da se nabimu hame hihisa. (aiōnios )
Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha. (aiōnios )
Dimase da osobo bagade hou amoma asigiba: le, e da na yolesili, Desalouniga moilai bai bagadega asi. Galesenes da Gala: isia sogega asi. Daidase da Da: lama: idia sogega asi. (aiōn )
Paja Dema anandisiya chifukwa chokonda dziko lapansi lino, ndipo anapita ku Tesalonika. Kresike anapita ku Galatiya ndipo Tito anapita ku Dalimatiya. (aiōn )
Wadela: mu liligi huluane nama doaga: sea, Hina Gode da na gaga: mu. E da na mae dafane Ea Hebene amo ganodini Hinadafa Hou amoga na oule masunu. Ninia da Ema eso huluane nodonanumu da defea. Ama. (aiōn )
Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake wakumwamba. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya. (aiōn )
Ninia dafawaneyale dawa: su ea bai da eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu. Ninia osobo bagade da hame dialeawane, hidadea Gode da amo eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu ninima imunu ilegele sia: i. Gode da ogogosu hame dawa: (aiōnios )
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios )
Amo hou da ninia wadela: i esalusu hou amola osobo bagade wadela: i hanai hou, amo yolesili, bu ninia hou amoma ouligisuwane esalusu hou, moloidafa hou amola Godema dawa: su hou, amo huluane hamoma: ne, Gode Ea hahawane dogolegele iasu amola gaga: su hou da ninima olelesa. (aiōn )
Chisomo chimatiphunzitsa kukana moyo osalemekeza Mulungu komanso zilakolako za dziko lapansi. Ndipo chimatiphunzitsa kukhala moyo odziletsa, olungama ndi opembedza Mulungu nthawi ino, (aiōn )
Gode da nini afadenei bu ida: iwane hamoi amola ninia hanai liligi, amo da eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu amola Ea hahawane iasu, amo huluane dawa: ma: ne, Gode da Ea A: silibu ninima i dagoi. (aiōnios )
kuti titalungamitsidwa mwachisomo chake, tikhale olowamʼmalo okhala ndi chiyembekezo cha moyo wosatha. (aiōnios )
Amabela: ? Ounisimase da fa: no eso huluane dia fidisu dunu esaloma: ne, musa: dia hawa: hamosu yolesili, ga sogega fonobahadi esalumusa: hobea: i. (aiōnios )
Mwina chifukwa chimene unasiyana naye kwa kanthawi ndi chakuti ukhale nayenso nthawi zonse. (aiōnios )
Be wali, soge wadela: mu eso da gadeneiba: le, E da Eagofe asunasili, Ea Sia: dafa ninima olelei dagoi. Gode da Eagofe Ea loboga osobo bagade, mu amola liligi huluane hahamoi. Gode da Eagofe amo soge wadela: mu eso doaga: sea, liligi huluane gaguma: ne, Ema ilegei dagoi. (aiōn )
Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn )
Be Gode da Egefedafa, amo Ea hou olelema: ne, amane sia: i, “Gode! Dia Hinadafa Hou da eso huluane dialalalumu. Di da moloidafa Dia fi dunu ouligilalumu. (aiōn )
Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn )
E eno amane sia: i, “Di da eso huluane hawa: hamonanoma: ne, Na da Di Gobele Salasu Dunu, Melegisedege ea fi gobele salasu dunu agoane ilegei dagoi.” (aiōn )
Ndipo penanso anati, “Iwe ndiwe wansembe mpaka muyaya, monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
Yesu Ea hou noga: idafa hamoi ba: loba, Gode da E eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu Gaga: su, (Ema nabasu dunu ilia lamu liligi) amo ea Bai hamoi. (aiōnios )
Atasanduka wangwiro kotheratu, anakhala gwero la chipulumutso chosatha kwa onse omvera Iye. (aiōnios )
Amaiba: le, ninia asigilai olelesu liligi dawa: ma: ne, bisili olelesu liligi yolesili, mae beba: le hagomodini masunu da defea. Musa: olelesu bai da ninia hamedei hawa: hamobeba: le Gode Ea hou hame dawa: mu, be Gode Ea hou dafawaneyale dawa: beba: le fawane gaga: su ba: mu. Eno da hanoga fane salasu hou, dunu ilegema: ne ea da: i hodo da: iya lobo ligisisu, bogoi bu wa: legadosu amola eso huluane se imunusa: fofada: su. Amo musa: olelesu bai fawane ninia bu baligiliwane dawa: mu da defea hame. (aiōnios )
(parallel missing)
Hebrews 6:2 (Ahebri 6:2)
(parallel missing)
za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza. (aiōnios )
Ilia da lalegaguiba: le, Gode Ea Sia: da ida: iwane ilia da dawa: i galu. Ilia da Gode Ea Hinadafa Hou dafawane doaga: sea, gasa bagade ba: mu, amo dawa: i galu. (aiōn )
Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera. (aiōn )
Yesu Gelesu da ninima bisili Hadigidafa Momei Sesei amo ganodini golili sa: i dagoi. E da Gobele Salasu Ouligisu dunu amo Melegisedege ea fi agoane hamoi dagoi. (aiōn )
Yesu anatitsogolera kupita kumeneko, nalowako mʼmalo mwathu. Iye anasanduka Mkulu wa ansembe onse wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. (aiōn )
Bai Gode Sia: da agoane dedei diala, “Na da Di Gobele Salasu Dunu eso huluane esalalaloma: ne, ilegei dagoi. Di da Melegisedege ea fi gobele salasu dunu agoane ba: mu.” (aiōn )
Pakuti Mulungu anamuchitira umboni kuti, “Iwe ndi wansembe wamuyaya, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.” (aiōn )
Be Gode da Yesu Gobele Salasu Dunu ilegele, E da Hi Dioba: le dafawane hamomu sia: i, amane, “Hina Gode da Hi Dioba: le dafawane hamomu sia: beba: le, E da Ea asigi dawa: su hamedafa afadenemu. Di da Gobele Salasu Dunu eso huluane esalalaloma: ne hamoi dagoi.” (aiōn )
Koma Yesu ankakhala wansembe ndi lumbiro pamene Mulungu anati, “Ambuye analumbira ndipo sangasinthe maganizo ake, ‘Iwe ndi wansembe wamuyaya.’” (aiōn )
Be Yesu da mae bogole, eso huluane esalalalusu dawa: Amaiba: le, E da hame bogomuba: le, Ea Gobele Salasu hawa: hamosu da hamedafa dagomu. (aiōn )
Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. (aiōn )
Mousese ea Sema dawa: le, osobo bagade dunu (dafasu dawa: dunu) ilia da gobele salasu Ouligisu dunu ilegesa. Be Gode Ea hahawane imunu ilegele sia: i liligi (amo E da Ea Dioba: le dafawane hamomu sia: i), amo da Sema amoga fa: no misi. Amo dawa: le, Gode da Egefedafa amo da ida: iwane logo dibi amoga doaga: i dagoi Dunu, Ema Gobele Salasu Ouligisudafa ilegei dagoi. (aiōn )
Pakuti lamulo limasankha anthu amene ndi ofowoka kukhala akulu a ansembe; koma lumbiro, lomwe linabwera pambuyo pa lamulo, linasankha Mwana, amene anapangidwa kukhala wangwiro kwamuyaya. (aiōn )
Gelesu da abula diasu golili sa: ili, Hadigidafa Momei Sesei amo ganodini asili, E goudi amola bulamagau, amo ilia maga: me gobele salimusa: hame gaguli asi. Be Hi maga: me ganodini gaguli asili, ninima eso huluane esalalalumusa: , gaga: su hamoi dagoi. (aiōnios )
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios )
Amo hou da dafawaneba: le, Gelesu Ea maga: me da baligiliwane ledo dodofesa, amo ninia dawa: E da eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu A: silibu amo Ea gasaga, Hi da: i hodo gobele salasu ida: iwanedafa, Godema i dagoi. Ninia Esalalala Godema hawa: hamoma: ne, Yesu Gelesu Ea maga: me da ninia asigi dawa: su noga: le dodofemusa: dawa: Amaiba: le, ninia hamedei osobo bagade dodofesu hou bu hame dawa: mu. (aiōnios )
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios )
Amaiba: le, dunu amo Gode da ilima misa: ne sia: i, ilia Gode Ea esalalalumu hahawane imunu sia: i liligi lama: ne, Gelesu da Gaheabolo Gousa: su Sema amoma Ouligisu Dunu esala. Dunu afae da bogoiba: le, dunu eno ilia musa: Sema amoga ouligibiba: le wadela: le hamoi, amo hou gogolema: ne olofoi dagoi ba: sa. (aiōnios )
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios )
Amane hamoi ganiaba, E da osobo bagade hahamoi eso hemone, amogainini wali, amo ode huluane E da se nabasu eso bagohame amoga nabala: loba. Be wali, soge wadela: mu eso gadeneiba: le, E afadafa fawane, Ea da: i hodo gobele salasu agoane wadela: i hou fadegamusa: , misi dagoi. (aiōn )
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn )
Gode da Ea Sia: (amo da hame ba: su liligi) amoga E da osobo bagade, mu amola liligi huluane (amo da siga ba: su liligi), amo hahamoi. Ninia da dafawaneyale dawa: su hou lalegaguiba: le amo dawa: (aiōn )
Ndi chikhulupiriro timazindikira kuti dziko lapansi ndi la mmwamba zinapangidwa ndi Mawu a Mulungu, ndikuti zinthu zoonekazi zinachokera ku zinthu zosaoneka. (aiōn )
Yesu Gelesu da aya, wali amola eso huluane, mae afadenene amaiwane musa: esalu amola wali esala amola hobea esalalalumu. (aiōn )
Yesu Khristu ndi yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse. (aiōn )
Hina Gode Yesu da gobele salasu hamoma: ne bogobeba: le, eso huluane dialalalumu gousa: su Sema dafawane hamoi dagoi. Yesu da amo gobele salasu hou hamobeba: le, ninia Sibi Ouligisu Bagade hamoi dagoi. Gode da Yesu Ea bogoi wa: legadolesi. Gode, ninia Olofosu Iasu, E da dilima, Ea hawa: hamomusa: defele, dilima liligi huluane imunu amola ninia Yesu Gelesuma madelagiba: le, Ea hanai hou huluane ninia dogo ganodini hamomu, da defea. Yesu Gelesu da eso huluane hadigiwane esalumu. Amaiba: le Ema nodonanumu da defea. Ama. (aiōn , aiōnios )
Mulungu wamtendere, amene kudzera mʼmagazi a pangano lamuyaya anaukitsa Ambuye athu Yesu kwa akufa, amene ndi Mʼbusa wamkulu, (aiōnios )
Hebrews 13:21 (Ahebri 13:21)
(parallel missing)
akupatseni chilichonse chabwino kuti muchite chifuniro chake ndipo Mulungu achite mwa ife, chimene chingamukomere kudzera mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ku nthawi zanthawi, Ameni. (aiōn )
Gona: su da lalu agoane. Amo da wadela: i liligi ninia da: i hodo ganodini. Wadela: i sia: sia: beba: le, ninia da: i hodo liligi huluanedafa da wadela: sa. Helo lalu da gona: su amoga dunu ilia esalusu huluane gia: iwane nenana. (Geenna )
Lilime nalonso ndi moto, dziko la zoyipa pakati pa ziwalo za thupi. Limawononga munthu yense wathunthu. Limayika zonse za moyo wake pa moto, ndipo moto wake ndi wochokera ku gehena. (Geenna )
Bai Gode Ea Sia: ida: iwane da esalawane amola eso huluane dialalalumu. Amo nababeba: le, dilia da bu lalelegele, Gode Ea mano hamoi. Dilia Ada da bogomu dunu hame. E da eso huluane mae bogole esalalalumu. (aiōn )
Popeza mwabadwanso, osati ndi mbewu imene imawonongeka, koma imene siwonongeka, ndiye kuti ndi Mawu a Mulungu amoyo ndi okhalitsa. (aiōn )
Be Hina Gode Ea Sia: da eso huluane esalalalumu.” Amo sia: da Gode Ea Sia: Ida: iwane Gala, amo ninia da dilima olelesu. (aiōn )
koma mawu a Ambuye adzakhala mpaka muyaya.” Ndipo awa ndi mawu amene tinalalikira kwa inu. (aiōn )
Nowa dunu da sia: olelesa, e da Gode Ea olelei fawane olelema: ne sia: ma. Nowa da fidisu hou hamosea, e da gasa amo Gode da ema i amoga hawa: hamomu da defea. Amasea, hou huluane ganodini, dunu da Yesu Gelesuma madelagiba: le, Godema nodonanumu. Gode da hadigi amola gasadafa, eso huluane mae fisili esalalaloma: mu. Ama. (aiōn )
Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
Be dilia da fonobahadi se nabawane ouesalu, Gode da hahawane dogolegele iasu huluane iaha, amo dawa: ma. E da dili Gelesuma madelagiba: le, Ea eso huluane dialalalumu hadigi hou gilisili lama: ne dilima misa: ne sia: i. Amo Gode Hi da dilia hou asigilama: ne hamomu amola dilima gasa hou amola dafawaneyale dawa: su baidafa dilima imunu. (aiōnios )
Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. (aiōnios )
Gode da eso huluane gasadafa gaguiwane esalalaloma: mu! Ama. (aiōn )
Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni. (aiōn )
Agoane hamosea, dilia ninia Hina Gode amola Gaga: su Yesu Gelesu amo ea eso huluane dialalalumu Hinadafa Hou amo ganodini golili sa: ima: ne, Gode da dilima logo hahawane doasimu. (aiōnios )
Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. (aiōnios )
Gode da a: igele dunu dafai ilima mae asigili, Helo sogega galadigi. Amogawi, ilia gasi ganodini sia: inega la: gi, Fofada: su Eso amo doaga: ma: ne ouesala. (Tartaroō )
Pakuti Mulungu sanalekerere angelo atachimwa paja, koma anawaponya mʼndende, nawayika mʼmaenje amdima, kuwasunga kuti adzaweruzidwe. (Tartaroō )
Be ninia Hina Gode amola Gaga: su Yesu Gelesu amo Ea hahawane dogolegele iasu amola bagade dawa: su, da dilia dogo ganodini asigilaluma: mu. Ema eso huluane wali amola hobea, mae yolesili nodonanumu da defea. Ama. Sia: Ama Dagoi (aiōn )
Koma kulani mu chisomo ndi mʼchidziwitso cha Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Amo eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu Sia: dafa da dunu ba: ma: ne da: i hodo lai, amo ninia ba: i dagoi. Amaiba: le, ninia amo hou olelesa. Eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu da musa: Gode amola gilisili esalu. Ada Gode da ninima olelebeba: le, ninia da bu dilima olelesa. (aiōnios )
Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. (aiōnios )
Osobo bagade amola amo ganodini liligi huluane amoma dunu ilia da hanai, amo da bu mae ba: ma: ne mugululala. Be nowa dunu da Gode Ea hanai hou hamosa, e da eso huluane esalalalumu. (aiōn )
Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. (aiōn )
Amo hou da Gelesu ninima imunu sia: i liligi, amo eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu. (aiōnios )
Ndipo chimene anatilonjeza nʼchimenechi: moyo wosatha. (aiōnios )
Nowa da ea fi dunu ilima ha lai galea, amo da fane legesu dunu. Amola fane legesu dunu da eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu hamedafa dawa: , amo dilia dawa: (aiōnios )
Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha. (aiōnios )
Gode Ea ba: su hou da agoane diala; Gode da ninima eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu i dagoi. Amola eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu ea Bai da Gode Egefedafa. (aiōnios )
Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. (aiōnios )
Dilia Gode Egefedafa amo ea hou dafawaneyale dawa: be dunu, dilia da eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu lai dagoi amo dafawaneyale dawa: ma: ne, na da dilima amo meloa dedesa. (aiōnios )
Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Gode Egefe da misi dagoi. Amola ninia da Gode Egefedafa amo noga: le dawa: ma: ne, E da dawa: su hou ninima i, amo dawa: Ninia da Godedafa - Egefe Yesu Gelesu, Ema madelagi esala. Ninia Gode da Godedafa amola amo hou da eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu. (aiōnios )
Tikudziwa kuti Mwana wa Mulungu anafika ndipo anatipatsa nzeru, kuti timudziwe Iye amene ali woona. Ndipo ife tili mwa Iye amene ndi woona, Mwana wake, Yesu Khristu. Iye ndi Mulungu woona ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Bai dafawanedafa hou da ninia dogo ganodini diala amola mae fisili eso huluane dialumu. (aiōn )
Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn )
Amola a: igele dunu mogili, ilia ouligisu hou alalo mae dawa: le, hame nabasu hou hamone, ilia sogebi yolesi, amo bu dawa: ma. Ilia da wali sia: ine hame fadegamu liligi amoga la: gili, hagudu gasi sogebi amo ganodini esala. Gode da ilima se imunusa: fofada: mu eso ilegei, amo doaga: ma: ne, ilia oualigisa. (aïdios )
Ndipo mukumbukire angelo amene sanakhutire ndi maudindo awo, koma anasiya malo awo. Angelo amenewa Mulungu anawamanga ndi maunyolo osatha, ndipo akuwasunga mʼmalo a mdima mpaka tsiku lalikulu lachiweruzo. (aïdios )
Dilia Sodame, Goumola amola eno gadenene moilai ilia hou bu dawa: ma. Amo fi dunu da waha sia: i dafai a: igele defele, wadela: i uda lasu hou amola inia uda adole lasu hou hamonanusu. Dunu huluane sisasu noga: le ba: ma: ne, amo dunu da lalu hame haba: dosu liligi amoga se nabalebe. (aiōnios )
Musayiwale mizinda ya Sodomu ndi Gomora ija, ndi mizinda yoyandikana nayo. Anthu mʼmenemo anadziperekanso kuchita zadama ndi kuchita zonyansa zachilendo. Mizinda imeneyi yakhala ngati chitsanzo cha amene adzalangidwa ndi moto wosatha. (aiōnios )
Ilia da waiyabo bagade hano gafului nimi bagade hamoi agoane ba: sa. Ilia wadela: i hou da amo ea dubu agoane ba: sa. Ilia da udigili lalebe gasumuni agoane ba: sa. Ilia eso huluane gasidafa amo ganodini esaloma: ne, Gode da ilima sogebi ilegei dagoi. (aiōn )
Iwowa ali ngati mafunde awukali apanyanja, amene amatulutsa thovu la zonyansa zawo. Amenewa ali ngati nyenyezi zosochera, ndipo Mulungu akuwasungira mdima wandiweyani mpaka muyaya. (aiōn )
Hina Gode Yesu Gelesu amo dilima asigiba: le eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu imunusa: ouesalebeba: le, dilia Gode Ea asigidafa hou amo ganodini esaloma. (aiōnios )
Khalani mʼchikondi cha Mulungu pamene mukudikira chifundo cha Ambuye athu Yesu Khristu kuti akubweretsereni moyo wosatha. (aiōnios )
Amaiba: le, ninia Gode, ninia Gaga: sudafa, Ema, ninia Hina Gode Yesu Gelesu da hamobeba: le, hadigi, gasa bagade Hina hou amola Hinadafa Hou, amo musa: hemonega hamonanu, wali hamosa amola hobea mae yolesili hamonanumu, amo E da eso huluane amaiwane esalomu. Amo dawa: le, ninia da mae fisili, Ema nodonanumu da defea! Ama! Sia: Ama Dagoi (aiōn )
kwa Mulungu yekhayo, Mpulumutsi wathu, kwa Iye kukhale ulemerero, ukulu, mphamvu ndi ulamuliro, mwa Yesu Khristu Ambuye athu, kuyambira isanayambe nthawi, tsopano mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
Yesu da nini Ea Ada Gode amo Ea hawa: hamomusa: gini, E da ninia osobo bagade hou fadegale, bu nini gobele salasu dunu ouligisu fi hamoi. Yesu Gelesu da hadigiwane, gasawane eso huluane esalalalumu. Ema nodonanumu da defea. Ama. (aiōn )
ndipo watisandutsa mafumu ndi ansembe kuti tizitumikira Mulungu ndi Atate ake. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu ku nthawi zosatha, Ameni. (aiōn )
Na da esalalalusu Dunu! Na da bogoi, be wali Na da eso huluane esalalalumusa: esala. Na da bogosu amola bogosu soge, amoma Hina esala. (aiōn , Hadēs )
Ine ndine Wamoyo; ndinali wakufa ndipo taona ndine wamoyo mpaka muyaya! Ndipo ndili ndi makiyi a imfa ndi Hade. (aiōn , Hadēs )
Esalebe liligi biyaduyale gala ilia da Fisu da: iya fibi Dunu, amo da eso huluane Esalalala Dunu Ema ilia nodone gesami hea: lala. (aiōn )
Nthawi zonse zamoyozo zimapereka ulemerero, ulemu ndi mayamiko kwa uja wokhala pa mpando waufumu, amene ali ndi moyo wamuyaya. (aiōn )
Ilia agoane hamonanea, asigilai dunu 24 da Fisu da: iya fibi Dunu, amo da eso huluane esalalala, amo Ea midadi beguduli, Ema nodone sia: ne gadosa. Ilia gouli habuga Fisu midadi sanasili, amane sia: sa, (aiōn )
Izi zikamachitika akuluakulu 24 aja amadzigwetsa pansi pamaso pa wokhala pa mpando waufumuyo, namupembedza wokhala ndi moyo wamuyayayo. Iwo amaponya pansi zipewa zawo zaufumu patsogolo pa mpando waufumu nati: (aiōn )
Amola liligi huluane Hebene ganodini, osobo bagadega, hagudu soge amoga esala liligi huluanedafa gesami hea: lalebe na da amane nabi, “Dunu huluane da Fisu da: iya fibi Gode amola Sibi Mano amoma mae yolesili, nodonanumu da defea!” (aiōn )
Kenaka ndinamva mawu a cholengedwa chilichonse kumwamba, pa dziko lapansi, kunsi kwa dziko lapansi, pa nyanja ndi zonse zili mʼmenemo zikuyimba kuti, “Kwa wokhala pa mpando waufumu ndi kwa Mwana Wankhosa, kukhale mayamiko, ulemu, ulemerero ndi mphamvu (aiōn )
Na ba: loba, haliga: i hosi da misi. Ema fila heda: i dunu ea dio amo Bogosu ba: i. Bogosu Soge da gadenenewane fa: no bobogelalebe ba: i. Gode da elama gasa bagade hou iasu, amo ela da osobo bagade biyaduyale mogili, la: ididili afadafa amo sogega gegesu, ha: i bagade, olosu amola nimi ohe fi, amoga ela da amo la: idi dunu medomusa: dawa: i. (Hadēs )
Nditayangʼana patsogolo panga ndinaona kavalo wotuwa! Wokwerapo wake dzina lake linali Imfa ndipo Hade inali kumutsatira pambuyo pake. Anapatsidwa ulamuliro pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi kuti aphe ndi lupanga, njala, mliri, ndi zirombo zakuthengo za mʼdziko lapansi. (Hadēs )
“Ama! Ninia Gode da hadigi, bagade dawa: su, asigidafa amola gasa bagade. Amaiba: le Ema eso huluane mae yolesili nodonanumu da defea. Ama!” (aiōn )
Iwo anati, “Ameni! Matamando ndi ulemerero, nzeru, mayamiko, ulemu, ulamuliro ndi mphamvu zikhale kwa Mulungu wathu kunthawi zanthawi, Ameni!” (aiōn )
Amalalu, a:igele dunu bi da dalabede fulaboi. Na ba: loba, gasumuni afae da osoboga sa: i. Gode da gi ema i. Amo gi da Gelabo Nosonodafa (A: bisi), amo doasimu gi e da lai dagoi. (Abyssos )
Mngelo wachisanu anayimba lipenga lake, ndipo ndinaona nyenyezi ikugwa pa dziko lapansi kuchokera ku thambo. Nyenyeziyo inapatsidwa kiyi ya ku chidzenje chakuya. (Abyssos )
Gasumuni da amo uli dogoi doasili, mobi amo lalu bagade mobi defele heda: beba: le, eso hadigi uligiba: le, gasi bagade ba: i. (Abyssos )
Nyenyeziyo itatsekula pa chidzenje chakuyacho panatuluka utsi ngati wochokera mʼngʼanjo yayikulu. Dzuwa ndi thambo zinada chifukwa cha utsi ochokera mʼdzenjemo. (Abyssos )
Ilia ouligisu da a: igele dunu amo da Gelabo Nosonodafa (A: bisi) gala amoma ouligisu esala. Ea dio da Hibulu sia: ga “Aba: dane.” Galigi sia: ga, ea dio da Abolione (dawa: loma: ne da “Gugunufinisisu Dunu”). (Abyssos )
Mfumu yawo inali mngelo wolamulira Chidzenje chakuya chija. Mʼchihebri dzina lake ndi Abadoni ndipo mʼChigriki ndi Apoliyoni (tanthauzo lake ndiye kuti, Wowononga). (Abyssos )
E da Gode, amo da Hebene amola osobo bagade amola amo ganodini liligi huluane hahamoi, amo Ea Dioba: le amane sia: i, “Gode da bu hame oualigimu! (aiōn )
Mngeloyo analumbira mʼdzina la Iye wokhala ndi moyo mpaka muyaya, amene analenga kumwamba ndi zonse zili kumeneko, dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo, nyanja ndi zonse zili mʼmenemo, nati, “Pasakhalenso zochedwa tsopano! (aiōn )
Ela Gode Ea sia: olelei dagoiba: le, ohe fi liligi bagade amo da Gelabo Nosonodafa (A: bisi) gala amoga manebe liligi, amo da elama gegemu. E da ela fane legemu. (Abyssos )
Tsono zikadzatsiriza umboni wawowo, chirombo chotuluka mʼChidzenje chakuya chija chidzachita nawo nkhondo nʼkuzigonjetsa mpaka kuzipha. (Abyssos )
Amalalu, a:igele fesu da dalabede fulaboi. Sia: bagade muagadodi manebe nabi, amane, “Ninia Hina Gode amola Ea ilegei Mesaia, da osobo bagadega Hinawane esaloma: ne gasa lai dagoi. E da eso huluane mae yolesili ouligilalumu.” (aiōn )
Mngelo wachisanu ndi chiwiri anawomba lipenga lake, ndipo kumwamba kunamveka mawu ofuwula amene anati, “Ufumu wa dziko lapansi uli mʼmanja mwa Ambuye athu ndi Khristu wake uja, ndipo adzalamulira mpaka muyaya.” (aiōn )
Amalalu, na da a: igele dunu eno muagado gadodilidafa hagili ahoanebe ba: i. E da Gode Ea Sia: Ida: iwane Gala amo dunu fifi asi gala, sia: hisu, fi hisu amola ouligisu hisu, amo huluanema olelela ahoa. (aiōnios )
Kenaka ndinaona mngelo wina akuwuluka mu mlengalenga ndipo anali ndi Uthenga Wabwino wamuyaya woti akalalikire kwa anthu okhala pa dziko lapansi, kwa a mtundu uliwonse, a fuko lililonse, a chiyankhulo chilichonse ndi kwa anthu onse. (aiōnios )
Ilima se dabe iasu ima: ne lalu, amo ea mobi da mae yolesili eso huluane heda: lala. Nowa da ohe fi liligi amola ea loboga hamoi agoaila liligi, amoma nodone sia: ne gadosa amola e dawa: digima: ne dedesu ilia lai dagoi, ilia da mae helefili se nabalumu.” (aiōn )
Ndipo utsi wa moto wowazunzawo udzakwera kumwamba mpaka muyaya. Sikudzakhala kupumula usana ndi usiku kwa amene anapembedza chirombo chija ndi fano lake kapena kwa aliyense amene analembedwa chizindikiro cha dzina lake lija.” (aiōn )
Amalalu, esalebe liligi biyaduyale gala, amo afadafa da gouliga hamoi ofodo fesuale gala amo a: igele dunu lobofaseleyale gala ilima i. Amo ofodo ganodini, eso huluane Esalalala Gode amo Ea ougi hou nabaiwane ba: i. (aiōn )
Ndipo kenaka chimodzi cha zamoyo zinayi zija chinapereka kwa angelo asanu ndi awiri mbale zisanu ndi ziwiri zodzaza ndi ukali wa Mulungu amene ali ndi moyo mpaka muyaya. (aiōn )
Amo ohe fi liligi da musa: esalu, be wali hame esala. E da Gelabo Nosonodafa (A: bisi) amoga gadodili heda: musa: dawa: lala. Amasea, Gode da amo wadela: mu. Osobo bagade dunu, amo ilia dio da osobo bagade hahamoi eso amo bisili eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu Buga amo ganodini hame dedei galea, amo dunu ilia ohe fi liligi ba: beba: le, fofogadigimu. Bai amo ohe fi liligi da musa: esalu, be wali hame esala. Be e da bu esalebe ba: mu. (Abyssos )
Chirombo chimene wachionachi chinalipo kale koma tsopano kulibe ndipo chidzatuluka ku chidzenje chakuya ndi kupita kukawonongedwa. Anthu okhala pa dziko lapansi amene mayina awo sanalembedwe mʼbuku lamoyo kuyambira pa kulengedwa kwa dziko lapansi adzadabwa pamene adzaona chirombocho, chifukwa chinalipo kale, tsopano kulibe, komabe chidzabwera. (Abyssos )
Ilia da bu eno wele sia: i, “Godema nodoma! Lalu da moilai bai bagade nenana, amo ea mobi da mae yolesili heda: lalumu!” (aiōn )
Ndipo anafuwulanso kuti, “Haleluya! Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” (aiōn )
Hosiga fila heda: i dunu da ohe fi liligi amola ogogosu balofede dunu afugili, se iasu diasu ganodini sali. (Ogogosu balofede dunu da ohe fi liligi ba: ma: ne, gasa bagade musa: hame ba: su hou hamosu. Amoga e da dunu amo ilia ohe fi liligi ea dawa: digima: ne dedesu lai amola ea loboga hamoi agoaila liligi amoma nodone sia: ne gadosu, amoma e da ogogoi.) Ilia da ohe fi liligi amola ogogosu balofede dunu, ili esaleawane lalu wayabo amo da salafaga nenana, amoga ha: digi. (Limnē Pyr )
Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. (Limnē Pyr )
Amalalu, na da Hebene amoga a: igele dunu dalebe ba: i. E da ea lobo ganodini Gelabo Nosonodafa (A: bisi) amo gi gagui amola gasa bagade sia: ine gagui. (Abyssos )
Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. (Abyssos )
A: igele da hanome Gelabo Nosonodafa (A: bisi) amo ganodini sanasili, amo ea logo ga: si dagoi. E da fifi asi gala dunu amo ode 1000 amoga bu ogogomu hamedei agoane ba: i. Be ode 1000 gidigili, ea se iasu diasu logo doasimuba: le, fonobahadi bu lalumu. (Abyssos )
Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe. (Abyssos )
Amalalu, Debele, (e da amo dunu ilima ogogoi), e da lalu wayabo amo da salafaga nenanebe amoga ha: digi dagoi ba: i. Amoga musa: ohe fi liligi amola ogogosu balofede dunu ha: digi dagoi ba: i. Ilia da eso huluane mae dagole, eso amola gasi, amoga se nabalumu. (aiōn , Limnē Pyr )
Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya. (aiōn , Limnē Pyr )
Amalalu, bogoi dunu musa: hanoga gela sa: ili bogoi amola bogoi amo bogoi sogebi amo ganodini dialu, amo da fofada: musa: wa: legadoi. Huluane da ilia hawa: hamoi defele fofada: su ba: i. (Hadēs )
Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. (Hadēs )
Amalalu, Gode da bogosu hou amola bogosu sogebi, lalu wayabo amoga ha: digi. (Amo lalu wayabo da Bogosu Ageyadu) (Hadēs , Limnē Pyr )
Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. (Hadēs , Limnē Pyr )
Nowa dunu da ea dio eso huluane mae bogole Fifi Ahoanusu Buga ganodini hame dedei dialebe ba: loba, e da lalu wayabo amo ganodini ha: digi dagoi ba: i. (Limnē Pyr )
Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto. (Limnē Pyr )
Be beda: i dunu, hohonosu dunu, wadela: i uda lasu hamosu dunu, wamuni dawa: su o yagono dawa: su, loboga hamoi ‘gode’ liligi ilima sia: ne gadosu dunu amola ogogosu dunu, amo huluane ilia ilegei soge da wayabo amo da lalu amola salafa amoga nenanebe ba: sa. Amo da Bogosu Ageyadu gala!” (Limnē Pyr )
Koma amantha, osakhulupirira, okonda zonyansa, opha anthu, achiwerewere, amatsenga, opembedza mafano ndi abodza, malo awo adzakhala nyanja yamoto ya sulufule wotentha. Iyi ndi imfa yachiwiri.” (Limnē Pyr )
Gasi da bu hame ba: mu. Hina Gode da ilia Hadigi esalumuba: le, ilia da gamali amola eso hadigi hamedei liligi ba: mu. Ilia da hina bagade agoane eso huluane ouligilalumu. (aiōn )
Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn )
Amo ogogosu olelesu dunu ilia da hano nasu hai dagoi agoane ba: sa. Ilia da mu mobi foga sefasilala agoane ba: sa. Gode da gasidafa sogebi amo ganodini ili esaloma: ne ilegei dagoi. ()