< 1 Golidia 8 >
1 Wali, dilia ha: i manu loboga hamoi ‘gode’ liligi ilima imunusa: , dilia meloa dedei adole ba: su liligi, amoma na da adole imunu. Dunu da amane sia: sa, “Ninia huluane da dawa: su gala.” Dafawane! Be amo dawa: su da gasa fi hou olelesa. Be asigidafa hou da eno dunu ilia hou asigilama: ne fidisa.
Tsopano za chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano: Ife tidziwa kuti tonse tili ndi chidziwitso. Komatu chidziwitso chokha chimadzitukumula, koma chikondi ndicho chimapindulitsa.
2 Nowa dunu da hidale hi hou da bagade dawa: sa, amo da houdafa dawa: su hamedafa dawa:
Munthu amene amaganiza kuti amadziwa kanthu, ndiye kuti sakudziwa monga mmene amayenera kudziwira.
3 Be nowa da Godema asigi galea, Gode da amo dunu dawa:
Koma munthu amene amakonda Mulungu amadziwika ndi Mulunguyo.
4 Amaiba: le, ha: i manu loboga hamoi ‘gode’ ilima i liligi, ninia da moma: bela: ? Loboga hamoi ‘gode’ liligi da hamedafa esala liligi ea agoaila agoane, amo ninia dawa: Gode afadafa fawane esala, amo ninia dawa:
Choncho kunena za chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano; ife tikudziwa kuti mafano si kanthu nʼpangʼonongʼono pomwe pa dziko lapansi, ndiponso kuti palibe Mulungu wina koma mmodzi yekha.
5 Be dunu ilia lafidili ‘gode’ liligi amola ‘hina’ liligi eno, Hebene ganodini amola osobo bagade ganodini esala ilia da sia: sa.
Popeza kuti ngakhale pali yotchedwa milungu, kaya ndi kumwamba kapena pa dziko lapansi (poti ilipodi milungu yambirimbiri ndi ambuye ambirimbiri),
6 Be ninima Gode afadafa fawane da esala. E da Edadafa, liligi huluane hahamoi dagoi. Ea hou olelemusa: , ninia da esala. Amola Hina Gode afadafa fawane, amo Yesu Gelesu esala. Ea hawa: hamobeba: le, liligi huluane hahamoi dagoi ba: i, amola Ea hamobeba: le, ninia da esala.
koma kwa ife pali Mulungu mmodzi yekha, Atate, zinthu zonse zinachokera mwa Iye ndipo ndife ake. Komanso pali Ambuye mmodzi Yesu Khristu kumene zinthu zonse zinachokera ndipo mwa Iye ife tili ndi moyo.
7 Be mogili ilia amo dafawane sia: hame dawa: Lalegagui dunu mogili da eso huluane musa: loboga hamoi ‘gode’ liligi amola eno a: silibu ea hou ilima bagadewane dawa: beba: le, amola ilia wali amo ha: i manu nasea, amo ha: i manu da loboga hamoi ‘gode’ amo ea liligi dawa: lala. Ilia asigi dawa: su da gasa hameba: le, ilia amo ha: i manu nasea, ilia hou wadela: mu ilia dawa: sa.
Koma saliyense amadziwa zimenezi. Alipo ena ozolowera mafano kwambiri mwakuti akadya chakudya chotere amaganiza kuti chakudyacho chinaperekedwa nsembe kwa mafano. Ndiye poti chikumbumtima chawo nʼchofowoka chimadetsedwadi.
8 Be ha: i manu da ninia Godema a: silibu dawa: su hou hame fidisa. Ninia ha: i manu hame nasea, ninia a: silibu hou hame fisimu. Amo ha: i manuba: le, ninia a: silibu hou da hame asigilamu.
Koma chakudya sichitisendeza kufupi ndi Mulungu. Tikapanda kudya si vuto, tikadya sitisinthikanso.
9 Dilia da amo hou ganodini sema hame gala. Be dawa: ma! Dilia sema hame gala hou da gasa hame lalegagui dunu ilima dafasu hou olelesa: besa: le, dawa: ma!
Komabe samalani kuti ufulu wanu ochita zinthu usafike pokhumudwitsa ofowoka.
10 Di da ‘dawa: su’ dunu, eno ilia da sia: sa. Be di da loboga hamoi ‘gode’ liligi amo ea debolo diasu ganodini ha: i manu nasea, asigi dawa: su gasa hame dunu da amo hou ba: sea, e da amo ha: i manu beda: i, be dia hou ba: beba: le e da mae dafawaneyale dawa: le manu.
Pakuti ngati aliyense wachikumbumtima chofowoka akakuonani achidziwitsonu mukudya mʼnyumba yopembedzera mafano, kodi iyeyo sichidzamulimbitsa mtima kuti azidya chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano?
11 Amo gasa hame dunu da dia fi dunu. Amola e gaga: ma: ne Yesu Gelesu da bogoi dagoi. Be amo dunu da dia ‘dawa: su’ hou ba: beba: le, gugunufinisi dagoi ba: mu.
Kotero kuti chifukwa cha chidziwitso chanu mʼbale wofowokayu amene chifukwa cha iye, Khristu anafa, wawonongeka chifukwa cha chidziwitso chanu.
12 Amaiba: le, agoane hamosea, di da dia Yesu Ea hou lalegagui fi dunu, ea asigi dawa: su wadela: lesiba: le, ema wadela: le hamoi dagoi ba: mu. Amola Gelesuma wadela: le hamoi dagoi ba: mu.
Mukamachimwira abale anu motere ndikuwawonongera chikumbumtima chawo chofowokacho, mukuchimwira Khristu.
13 Amaiba: le ha: i manu da na fi dunu ea wadela: i hou hamosu logo fodosa galea, na fi dunu da wadela: le hamosa: besa: le, na da fedege agoane bu ha: i manu huluane hamedafa manu. (aiōn )
Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse. (aiōn )