< Yoube 12 >

1 Yoube da amane sia: i,
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 “Dafawane! Dilia da dunu huluane ilia lafi agoai gala! Dilia da bogosea, asigi dawa: su noga: idafa amolawane da bogoi dialebe ba: mu!
“Ndithudi inuyo ndinu anthu ndipo nzeru zanu zidzafera nanu pamodzi!
3 Be na asigi dawa: su da dilia asigi dawa: su defele gala. Dilia hou da na hou hame baligisa. Dilia waha sia: be amo dunu huluane ilia dawa:
Koma inenso ndili nazo nzeru ngati inu; ineyo sindine munthu wamba kwa inu. Ndani amene sadziwa zonse zimene mwanenazi?
4 Be wali na na: iyadodafa amolawane ilia naba: le habosesele oufesega: sa. Be na hou da moloidafa amola na da wadela: le hamosu hame dawa: Be musa: , Gode da na sia: ne gadosu nabane, adole iasu.
“Ndasanduka chinthu choseketsa kwa abwenzi anga, ngakhale ndinkapemphera kwa Mulungu ndipo Iye ankandiyankha. Ine ndasanduka chinthu chongoseketsa, ngakhale ndili wolungama ndi wosalakwa!
5 Dilia da bidi hamosu hame dawa: Be dilia da nama habosesele oufesega: sa. Dilia da dunu amo da dafamu gadenei, amo fasa.
Anthu amene ali pabwino amanyoza anzawo amene ali pa tsoka. Tsokalo limagwa pa amene wayamba kale kugwa.
6 Wamolasu dunu amola Gode Ea hou hame lalegagui dunu ilia ‘gode’ da ilila: gasa fawane. Be ilia da osobo bagadega olofoiwane esala.
Nyumba za anthu achifwamba zimakhala pa mtendere, ndipo anthu amene amaputa Mulungu amakhala pabwino, amene amanyamula milungu yawo mʼmanja.
7 Be sio fi amola ohe fi da dilima olelemusa: dawa:
“Koma funsa nyama zakuthengo ndipo zidzakuphunzitsa, kapena mbalame zamumlengalenga ndipo zidzakuwuza;
8 Dilia osobo bagadega amola hano wayabo bagadega esalebe liligi, amo ilia da dilima olelema: ne, adole ba: mu da defea.
kapena uyankhule ndi dziko lapansi ndipo lidzakuphunzitsa, kapena ulole nsomba zamʼnyanja kuti zikufotokozere.
9 Ilia huluane da Hina Gode da ili hamoi, amo dawa:
Kodi mwa zonsezi ndi chiti chimene sichidziwa kuti lachita zimenezi ndi dzanja la Yehova?
10 Gode Hi fawane da Ea hamoi liligi huluane, ilia esalusu ouligisa. Dunu huluane ilia esalusu da Ea gasaha diala.
Mʼmanja mwake ndi mʼmene muli moyo wa cholengedwa chilichonse, ndiponso moyo wa anthu a mitundu yonse.
11 Be dilia! Dilia gona: su da ha: i manu ea hedai hahawane naba. Amo defele, dilia ge da udigili sia: dabe hahawane naba.
Kodi khutu sindiye limene limamva mawu monga mmene lilime limalawira chakudya?
Kodi nzeru sipezeka pakati pa anthu okalamba? Kodi moyo wautali sumabweretsa nzeru zomvetsa zinthu?
13 Da: i hamoi dunu ilia da asigi dawa: su bagade gala. Be Gode da asigi dawa: su bagadedafa amola gasa bagade gala. E da Ea hawa: hamomu defele, gasa bagadedafa gala.
“Kwa Mulungu ndiye kuli nzeru ndi mphamvu; uphungu ndi kumvetsa zinthu ndi zake.
14 Gode da dunu ilia gagui liligi mugulusia, nowa da bu gaguma: bela: ? Gode da dunu amo se iasu diasu ganodini sanasisia, nowa da amo se iasu diasu logo doasima: bela: ?
Chimene Iye wapasula palibe angachimangenso. Akatsekera munthu mʼndende palibe angamutulutse.
15 Gode da gibu dabe logo ga: sisia, ha: bagade ba: sa. E da gibu bagade iasisia, hano da bagadewane heda: le, osobo dedebosa.
Iyeyo akamanga mvula dziko limawuma; akamasula mvulayo, madzi amasefukira pa dziko.
16 Gode da gasa bagade amola E da Ea ha lai dunu eso huluane hasala. Ogogosu dunu amola dunu ilima ilia ogogoi, ilia gilisili Gode Ea gasaha esalebe.
Kwa Iye kuli mphamvu ndi kupambana; munthu wopusitsidwa ndiponso wopusitsa onse ali mu ulamuliro wake.
17 Gode da ouligisu dunu ilia asigi dawa: su samogesa. E da bagade dawa: su ouligisu dunu ilia hou afadenene, amasea ilia da gagaoui dunu agoai hamosa.
Iye amalanda aphungu nzeru zawo ndipo amapusitsa oweruza.
18 E da hina bagade dunu ilia ouligibi fadegale, ili se iasu diasu ganodini sala.
Iye amachotsa zingwe zimene mafumu anawamanga nazo ndipo amawamanga lamba mʼchiwuno mwawo.
19 E da gobele salasu dunu amola gasa bagade dunu, ilia hou fonobosa.
Iye amasocheretsa ansembe atawalanda nzeru zawo ndipo amagonjetsa anthu amphamvu amene ndi okhazikika.
20 Osobo bagade dunu da eno dunu ilia hou dafawaneyale dawa: be. Be Gode da amo dunu ouiya: ma: ne, ilia lafi ga: sisa. E da da: i hamoi dunu ilia bagade dawa: su hou samogesa.
Iye amakhalitsa chete aphungu odalirika ndipo amalanda chidziwitso cha anthu akuluakulu.
21 E da gasa bagade ouligisu dunu gogosiama: ne hamosa, amola ilia gasa bagade hou hedofasa.
Iye amanyoza anthu otchuka ndipo anthu anyonga amawatha mphamvu.
22 E da gasi bagade sogebi amoga hadigi iasisa.
Iye amatulutsira poyera zinthu zozama za mu mdima ndipo mdima wandiweyaniwo amawusandutsa kuwala.
23 E da fifi asi gala amo gasa bagade heda: ma: ne hamosa. Amalalu, E da amo fifi asi gala hasalasili, ili gugunufinisisa.
Iye amakuza mitundu ya anthu ndipo amayiwononganso; amachulukitsa mitundu ya anthu ndipo amayimwazanso.
Iye amalanda nzeru za atsogoleri a dziko lapansi; amawayendetsa mʼthengo mopanda njira.
25 E da ilia ouligisu dunu gagaoui dunu agoane hamosa. Amasea, ilia da udigili doulasili, gasi ganodini adini ba: i dunu defele feloasa.
Iwo amafufuzafufuza njira mu mdima wopanda chowunikira; Iye amawayendetsa dzandidzandi ngati oledzera.

< Yoube 12 >