< Yoube 11 >

1 Soufa da amane sia: i,
Pamenepo Zofari wa ku Naama anayankha kuti,
2 “Nowa da amo gagaoui sia: amoma adole ima: bela: ? Di da sia: bagade sia: beba: le, bu moloidafa hamobela: ? Hame mabu!
“Kodi mawu ambirimbiriwa nʼkukhala osayankhidwa? Kodi munthu woyankhulayankhulayu nʼkulungamitsidwa?
3 Yoube! Di adi dawa: bela: ? Di da ninia dima adole imunu da hamedei amo dawa: sala: ? Di da habosesele sia: beba: le, ninia da sia: hamedei agoane ba: mu, di da dawa: sala: ?
Kodi anthu nʼkukhala chete atamva kubwebweta kwakoku? Kodi palibe wina amene adzakudzudzule pamene ukuyankhula zonyoza?
4 Dia sia: da dafawane, di da sia: sa. Di da Gode Ea ba: ma: ne moloi fawane, di da sia: sa.
Iwe ukunena kwa Mulungu kuti, ‘Zikhulupiriro zanga ndi zopanda zolakwika ndipo ndine wangwiro pamaso panu.’
5 Na hanai da Gode Hisu da dima adole imunu da defea.
Aa, nʼkanakonda Mulungu akanayankhula kuti Iye atsekule pakamwa pake kutsutsana nawe
6 E da dima adole iabe ganiaba, E da dima Ea asigi dawa: su houdafa da osobo bagade dunu ilia asigi dawa: su bagadewane baligisa, amo adole ia: noba. Gode da dia hamobe defele, se hame iaha.
ndi kukuwululira chinsinsi cha nzeru yake, pakuti nzeru yeniyeni ili ndi mbali ziwiri. Dziwa izi: Mulungu wayiwala machimo ako ena.
7 Di da Gode Ea bagadedafa hou amola gasa bagade hou huluane dawa: mu da hamedei.
“Kodi iwe ungathe kumvetsa zinsinsi za Mulungu? Kodi ungafufuze malire a nzeru za Wamphamvuzonse?
8 Di da mu digili ba: mu gogolesa. Be Gode da mu amola liligi huluane baligisa. Gode da bogoi dunu ilia soge dawa: be. Be di da amo hame dawa: (Sheol h7585)
Zili kutali kupambana mayiko akumwamba, nanga ungachite chiyani? Ndi zakuya kupambana kuya kwa manda, nanga ungadziwe chiyani? (Sheol h7585)
9 Gode Ea bagadedafa hou da osobo bagade amola hano wayabo bagade elea ba: de baligisa.
Muyeso wa nzeru zake ndi wautali kupambana dziko lapansi ndipo ndi wopingasa kupambana nyanja.
10 Gode da di afugili gagulaligisia, amola fofada: musa: di oule ahoasea, nowa da Ea logo hedofama: bela: ?
“Ngati Iye atabwera ndi kukutsekera mʼndende nakutengera ku bwalo la milandu, ndani angathe kumuletsa?
11 Gode da hamedei dunu huluane dawa: E da ilia wadela: i hou huluane ba: lala.
Ndithudi, Mulungu amazindikira anthu achinyengo; akaona choyipa, kodi sachizindikira?
12 Sigua dougi da fofoi dougi defele lalelegesea, amo esoga gagaoui dunu da muni bagade dawa: su dunu defele ba: mu.
Munthu wopanda nzeru sizingatheke kukhala wanzeru monganso mwana wa bulu wakuthengo sangasanduke munthu.
13 Yoube! Dia hou moloma! Godema sinidigima!
“Koma ngati upereka mtima wako kwa Iye ndi kutambasulira manja ako kwa Iyeyo,
14 Dia wadela: i hou yolesima!
ngati utaya tchimo limene lili mʼdzanja lako ndi kusalola choyipa kuti chikhale mʼmoyo mwako,
15 Amasea, di mae beda: iwane, osobo bagadega bu hahawane esaloma!
udzatukula mutu wako wosachita manyazi; udzayima chilili ndipo sudzachita mantha.
16 Amasea, di da dia bidi hamosu amo bu hame dawa: mu. Hano leda: sea, fonobahadi dialu, bu hasa. Amo defele, dia bidi hamosu wali diala, da hobea bu hame ba: mu.
Udzayiwala ndithu zowawa zako, zidzakhala ngati madzi amene apita kale.
17 Dia esalusu da eso dogoa digagala: be defele ba: mu. Amola dia se nabasu eso da hehebolo mabe defele ba: mu.
Moyo wako udzawala kupambana usana, ndipo mdima udzakhala ngati mmawa.
18 Di da gaga: iwane amola dafawane hamoma: beyale dawa: iwane esalumu. Gode da di gaga: le, dima helefisu imunu.
Udzalimba mtima popeza pali chiyembekezo; ndipo udzayangʼana mbali zonse ndi kugona mosatekeseka.
19 Di da dia ha lai dunuma hame beda: mu. Dunu bagohame da dia ili fidima: ne adole ba: mu.
Udzagona pansi, popanda wina wokuopseza ndipo ambiri adzakupempha kuti uwachitire chifundo.
20 Be wadela: le hamosu dunu da ba: le gagale, da: i dioi fawane ba: mu. Ilia da hobeamu logo hame ba: mu. Ilia hanai da ilia hedolowane bogoma: ne fawane dawa: sa.”
Koma anthu oyipa adzafuna thandizo osalipeza, ndipo adzasowa njira yothawirapo; chiyembekezo chawo chidzakhala imfa basi.”

< Yoube 11 >