< 2 Hina 18 >

1 Isala: ili hina bagade Housia (Ila egefe) amo ea ouligibi ode osoda amoga, Hesegaia (A: iha: se egefe) e da Yuda hina bagade hamoi.
Mʼchaka chachitatu cha Hoseya mwana wa Ela mfumu ya Israeli, Hezekiya mwana wa Ahazi mfumu ya Yuda analowa ufumu.
2 Hesegaia da lalelegele ode 25 esalu, e da muni Yuda hina bagade hamoi, amola e da Yelusaleme moilai bai bagadega esala, Isala: ili fi ode 29 agoanega ouligilalu. Ea ame da Abaidia, Segalaia ea idiwi.
Anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka 29. Amayi ake anali Abi, mwana wa Zekariya.
3 E da ea musa: aowa, hina bagade Da: ibidi ea hou defele, Hina Gode hahawane ba: ma: ne, moloi hou hamoi.
Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova monga anachitira Davide kholo lake.
4 E da ogogosu ‘gode’ma nodone sia: ne gadosu sogebi huluane wadela: lesi. E da wadela: i gele golasu ifa, amo fili sasali. Amola e da wadela: i uda ‘gode’ Asila agoaila loboga hamoi ‘gode’ huluane damuni fasi. Amola e da balasega hamoi sania (amo musa: Mousese hamoi amola amoma ilia da Nehasiada: ne dio asuli) amo e da goudane fasi. Bai musa: amoganini, Isala: ili dunu da giadofale amo liligima nodone sia: ne gadoma: ne, gabusiga: manoma gobele salasu.
Anachotsa malo opembedzerako mafano, anaphwanya miyala yachipembedzo ndiponso anadula mafano a Asera. Iye anaphwanya njoka yamkuwa imene Mose anapanga, pakuti mpaka kufikira nthawi imeneyi Aisraeli amafukiza lubani kwa njoka imeneyi. (Imatchedwa Nehusitani).
5 Hesegaia da Isala: ili fi ilia Hina Gode Ea hou dafawaneyale dawa: beba: le, lalegagui dagoi. Yuda soge ganodini, hina bagade e agoai da hame ba: su, amola fa: no e agoai hame ba: i.
Hezekiya anadalira Yehova Mulungu wa Israeli. Kotero panalibe wina wofanana naye pakati pa mafumu onse a Yuda, asanakhale mfumu kapena atakhala kale mfumu.
6 E da Hina Gode mae yolesili, hame nabasu hou hamedafa hamoi. E da molole dawa: iwane amo hamoma: ne sia: i huluane Hina Gode da Mousesema sia: i, amoma fa: no bobogei.
Iye anakangamira Yehova ndipo sanamusiye koma anasunga malamulo amene Yehova anapatsa Mose.
7 Amaiba: le, Hina Gode da e fuligala: beba: le, ea hamobe huluane da didili hamoi ba: i. E da Asilia hina bagade ema odoga: ne, amola ea hamoma: ne sia: i hame hamosu.
Ndipo Yehova anali naye ndipo kulikonse kumene anapita zinthu zinkamuyendera bwino. Iye anagalukira mfumu ya ku Asiriya ndipo sanayitumikirenso.
8 E da Filisidini fi dunu hasali. E da ilia moilai (fonobahadi amola bagade, amola Ga: isa moilai bai bagade amola soge amoga sisiga: le dialu) amo huluane e da doagala: i.
Iye anakantha Afilisti kuyambira ku nsanja ya alonda mpaka ku mzinda wotetezedwa. Anakafika mpaka ku Gaza ndi ku malire ake.
9 Hesegaia ea ouligibi ode biyadu amoga (amo ode da Isala: ili hina bagade Housia ea ouligibi ode fesuale), amo odega Asilia hina bagade Sia: lama: nisa da Isala: ili doagala: le, Samelia moilai bai bagade eale disi.
Mʼchaka chachinayi cha Mfumu Hezekiya, chimene chinali chaka chachisanu ndi chiwiri cha Hoseya mwana wa Ela mfumu ya Israeli, Salimenezeri, mfumu ya ku Asiriya anabwera kudzathira nkhondo mzinda wa Samariya ndi kuwuzinga
10 Sia: lama: nisa da Samelia doagala: le, eale disili, ode udianaga hasali. Amo ode da Hesegaia ea ouligibi ode gafeyale amola Housia ea ouligibi ode sesegeyale, amogalu agoane hamosu.
Asiriya analanda mzindawu patatha zaka zitatu. Choncho mzinda wa Samariya unalandidwa chaka chachisanu ndi chimodzi cha Hezekiya, chimene chinali chaka chachisanu ndi chinayi cha Hoseya mfumu ya Israeli.
11 Asilia hina bagade da Isala: ili dunu mugululi, udigili hawa: hamomusa: , Asilia sogega oule asi. E da amo dunu mogili Hala moilaiga, mogili Gousa: ne soge (Ha: ibo Hano gadenene) amola mogili Midia soge moilai, amolaliga fima: ne asunasisi.
Mfumu ya ku Asiriya inatenga Aisraeli kupita nawo ku ukapolo ku Asiriya ndipo anakawakhazika ku Hala, ku Habori pafupi ndi mtsinje wa Gozani ndi mʼmizinda ya Amedi.
12 Samelia fi dafai ea bai da, ilia da Isala: ili Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i hame nabasu. Ilia Gousa: su amo E da ilima hahamoi amo fi dagoi. Amola ilia da sema huluane amo Hina Gode Ea hawa: hamosu dunu Mousesemadili i, amo hame nabi. Ilia da amo huluane hame nabi, amola nabasu hou hame hamosu.
Izi zinachitika chifukwa sanamvere zonena za Yehova Mulungu wawo, koma anaphwanya pangano lake ndi zonse zimene Mose mtumiki wa Yehova anawalamula. Iwo sanamvere malamulowo kapena kuwagwiritsa ntchito.
13 Yuda hina bagade Hesegaia ea ouligibi ode 14 amoga, Asilia hina bagade Sena: gelibi da Yuda soge gagili sali moilai ilima doagala: le, hasali.
Mʼchaka chakhumi ndi chinayi cha ulamuliro wa Mfumu Hezekiya, Senakeribu mfumu ya ku Asiriya anathira nkhondo mizinda yonse yotetezedwa ya Yuda, nayilanda.
14 Hesegaia da Sena: gelibi, La: igisi moilai bai bagade ganodini esala, ema amane sia: si, “Na da giadofale hamoi! Dia doagala: lalu yolesima! Amasea, bidi dia ima: ne sia: be defele, na da dima imunu.” Asilia hina bagade da bu dabe sia: si, “Silifa 10,000 gilo defei amola gouli 1,000 defei, amo nama iasima!”
Choncho Hezekiya mfumu ya Yuda anatumiza uthenga kwa mfumu ya ku Asiriya ku Lakisi wonena kuti, “Ine ndalakwa. Chokani kuno ndipo ndidzakupatsani chilichonse chimene munene.” Mfumu ya ku Asiriya inalamula mfumu Hezekiya, mfumu ya Yuda, kuti azipereka makilogalamu a siliva okwana 3,000 ndi makilogalamu a golide 1,000.
15 Hesegaia da silifa huluane amo da Debolo diasu amola hina bagade diasu noga: i liligi ligisisu sesei ganodini dialu, amo huluane ema iasi.
Mfumu Hezekiya inapereka siliva yense amene anapezeka mʼNyumba ya Yehova ndi mʼnyumba zosungiramo chuma cha mfumu.
16 Amola e da gouli amo da Debolo logo ga: su legei, amola gouli amogamusu logo ga: su golasu ifa dedeboi, amo huluane hosoga: le, Sena: gelibi ema iasi.
Nthawi imeneyi Hezekiya mfumu ya Yuda anakanganula golide amene anakuta zitseko ndi mphuthu za chipata cha Nyumba ya Yehova namupereka kwa mfumu ya ku Asiriya.
17 Asilia hina bagade da La: igisi amoga dadi gagui dunu wa: i bagade, Yelusaleme doagala: ma: ne asunasi. Ea baligili bagade eagene ouligisu dunu udiana da amo dadi gagui dunu wa: i ouligi. Ilia da Yelusaleme moilai bai bagadega doaga: le, ilia da abula hahamosu dunu ilia hawa: hamosu sogebi logoga (hano amo da gadodili hano wayaboga fugala: le ha: ina dasu, amo logo gadenene dialu) amo sogebiga ilia da fi dialu.
Mfumu ya ku Asiriya inatuma Taritani, Rabusarisi ndi Rabusake pamodzi ndi gulu lalikulu la ankhondo, kwa Mfumu Hezekiya ku Yerusalemu kuchokera ku Lakisi. Iwo anafika ku Yerusalemu nakayima pafupi ndi ngalande ya madzi yochokera ku Dziwe Lakumtunda, pa msewu waukulu wopita ku malo a Munda wa Mmisiri Wochapa.
18 Amalalu, ilia da hina bagade Hesegaia misa: ne sia: i. Hesegaia ea eagene ouligisu dunu udiana da gadili asi. Ilia da Ilaiagime (e da Hiligaia egefe. E da hina bagade diasu ouligi), Siebena (hina bagade diasu esalebe fi sia: dedesu dunu) amola Youa (A: isa: fe egefe. E da Hamonanu Meloa dedesu dunu).
Iwo anayitana mfumu, ndipo Eliyakimu mwana wa Hilikiya woyangʼanira nyumba ya mfumu, Sebina mlembi wa bwalo ndi Yowa mwana wa Asafu mlembi wa zochitika anapita kwa anthuwo.
19 Asilia ouligisu dunu afae da ilima amane adole ba: i, “Hina bagade Hesegaia da abuliba: le ninia da e hame hasalimu dawa: sala: ?
Ndipo Rabusake anawawuza kuti, “Kamuwuzeni Hezekiya kuti, “‘Mfumu yayikulu, mfumu ya ku Asiriya ikunena kuti, ‘Kodi chikukulimbitsa mtima ndi chiyani?’
20 Dilia adi dawa: bela: ? Lafidili sia: fawane da gasa bagade dadi gagui wa: i amola gegesu bagade dawa: su hou amo hasalasima: bela: ? Dilia da Asilia hina bagadema odoga: beba: le, nowa da dili fidima: bela: ?
Iwe ukuti uli ndi luso ndiponso mphamvu pa nkhondo, komatu ukuyankhula mawu opanda pake. Kodi tsono iwe ukudalira yani kuti undiwukire ine?
21 Dilia da Idibidi fi ilia dili fidima: ne dawa: lala! Be amo da fedege agoane dilia da saga: amoga galiamo hamosu defele. Amo da gasa hame galea da fili gala: le, dia lobo somu. Dunu ilia da Idibidi hina bagade ea fidisu lamu dawa: sea, e da amo defele ba: sa.”
Taona tsono, iwe ukudalira Igupto, bango lothyokalo, limene limalasa mʼmanja mwa munthu ngati waliyesa ndodo yoyendera! Umo ndi mmene Farao mfumu ya ku Igupto imachitira aliyense amene akuyidalira.’”
22 Asilia ouligisu dunu da hidale eno amane sia: i, “Dilia da nama, dilia Hina Gode Ea fidisu lamu, amo sia: ma: bela: ? Hesegaia da Yuda fi dunu amola Yelusaleme dunu amo Yelusalemega fawane nodone sia: ne gadoma: ne olelesa. Be e da Hina Gode Ea oloda amola nodone sia: ne gadosu sogebi huluane gugunufinisi dagoi.
Ndipo ngati ukunena kwa ine kuti, “Ife tikudalira Yehova Mulungu wathu.” Kodi si Mulungu yemweyo amene nyumba zake ndi maguwa ake Hezekiya anachotsa, nawuza anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu kuti, “Muzipembedza pa guwa lansembe ili mu Yerusalemu?”
23 Na da Asilia hina bagade ea dioba: le, agoane bidi lasu ilegele sia: sa. Dilia da hosi da: iya fila heda: su dawa: dunu 2,000 agoane hogole ba: sea, na da dilima hosi 2,000 agoane imunu.
“‘Ndipo tsopano bwera udzakambirane ndi mbuye wanga, mfumu ya ku Asiriya: ine ndidzakupatsa akavalo 2,000 ngati ungathe kupeza okwerapo!
24 Fonobahadidafa Asilia ouligisu dunu ea hou da dilia hou bagade baligisa. Amaiba: le, dilia abuliba: le, Idibidi dunu da dilima ‘sa: liode’ amola hosi da: iya fila heda: su dadi gagui dunu, amo dilima asunasima: ne dawa: sala: ?
Ungathe bwanji kugonjetsa ngakhale mmodzi mwa akazembe angʼonoangʼono a mbuye wanga, pamene ukudalira Igupto kuti akupatse magaleta ndi anthu okwera pa akavalo?
25 Dilia adi dawa: bela: ? Na da udigili, Hina Gode na mae fidiliwane, dilia soge doagala: bela: ? Hame mabu! Hina Gode Hisu da na Yuda doagala: le, amo gugunufinisima: ne sia: i dagoi.
Kuwonjezera pamenepa, kodi ine ndabwera kudzathira nkhondo ndi kuwononga malo ano popanda chilolezo cha Yehova? Yehova mwini ndiye anandiwuza kuti ndidzathire nkhondo ndi kuwononga dziko lino.’”
26 Amalalu, Ilaiagime, Siebena, amola Youa da Asilia ouligisu dunuma amane sia: i, “Hina! A: lama: iege sia: ga ninima sia: ma! Ninia amo sia: dawa: Hibulu sia: ga mae sia: ma! Bai Yelusaleme dunu huluane gagoi da: iya fi dialebe, ilia da amo sia: ga: sia: be nabala.”
Pamenepo Eliyakimu mwana wa Hilikiya, Sebina ndi Yowa anawuza Rabusakeyo kuti, “Chonde yankhulani kwa atumiki anufe mʼChiaramu, popeza timachimva. Musayankhule nafe mu Chihebri kuopa kuti anthu onse amene ali pa khomapa angamve.”
27 Be Asilia ouligisu dunu da bu adole i, “Dilia da Asilia hina bagade da dili amola Yuda hina bagade dilima fawane asunasi dawa: sala: ? Hame mabu! Na amolawane da dunu gagoi da: iya fi diala, ilima sia: sa. Bai dili defele, ilila: iga amola baeya nanebe ba: mu.”
Koma Rabusake anayankha kuti, “Kodi mbuye wanga wandituma kuti ndidzanene zinthu izi kwa mbuye wanu yekha ndi inu nokha basi? Ayi, komanso kwa anthu amene akhala pa khomawa. Iwowa adzadya chimbudzi chawo chomwe ndi kumwa mkodzo wawo womwe monga momwe mudzachitire inuyonso.”
28 Amalalu, Asilia ouligisu dunu da wa: legadole, Hibulu sia: ga amane wele sia: i, “Asilia hina bagade ea dilima sia: be nabima!
Tsono Rabusake anayimirira nafuwula mu Chihebri kuti, “Imvani mawu a mfumu yayikulu, mfumu ya ku Asiriya!
29 E da dilima amane sisane sia: sa, ‘Hesegaia da dilima ogogosu sia: mae nabima! Hesegaia da dili gaga: mu hame dawa: !
Zimene mfumu ikunena ndi izi: ‘Musalole kuti Hezekiya akunamizeni. Iye sangakupulumutseni mʼdzanja langa.
30 Amola e da dilima, Hina Gode Ea gaga: su hou dafawaneyale dawa: ma: ne sia: sea, ea sia: mae nabima! Hina Gode da dili gaga: le amola Asilia dadi gagui wa: i dilia moilai mae hasalima: ne logo ga: mu, amo mae dawa: ma! Hina Gode da dili fidimusa: hame dawa: !
Hezekiya asakukakamizeni kudalira Yehova ndi mawu akuti, ‘Ndithu, Yehova adzatipulumutsa; ndipo sadzapereka mzindawu mʼdzanja la mfumu ya ku Asiriya.’
31 Hesegaia ea sia: mae nabima! Asilia hina bagade da dilima amane hamoma: ne sia: sa, Dilia moilai fisili gadili ahoasea, dilia da goaya: ma! E da dili huluane dilisu waini sagaiga waini fage moma: ne amola figi sagaiga figi fage moma: ne amola si hanoga hano moma: ne, amo logo doasimu.
“Musamumvere Hezekiya. Zimene mfumu ya ku Asiriya ikunena ndi izi: Pangani mtendere ndi ine ndipo mutuluke mu mzinda. Mukatero aliyense wa inu adzadya mphesa ndi nkhuyu za mʼmunda mwake ndiponso adzamwa madzi a mʼchitsime chake,
32 Amasea, Asilia hina bagade da dili mugululi, oule asili, dili soge, dilia soge agoai amo ganodini ha: ini fima: ne, oule masunu. Amogawi, dilia da waini hano moma: ne waini sagai amola agi ga: gi hamoma: ne gala: ine amola olife ifa sagai amola olife susuligi amola agime hano huluane dialebe ba: mu. Dilia da ea hamoma: ne sia: i nabawane hamosea, dilia da mae bogole, esalumu. Hesegaia, ea ogogosu sia: amoga da Hina Gode da dilia gaga: ma: bela: le mae dawa: ma!
mpaka nditabwera kudzakutengani kupita ku dziko lofanana ndi lanuli, dziko la tirigu ndi vinyo watsopano, dziko la chakudya ndi minda ya mipesa, dziko la mitengo ya olivi ndi uchi. Sankhani moyo osati imfa! “Musamvere zonena Hezekiya, pakuti iye akukusocheretsani ponena kuti, ‘Yehova adzatipulumutsa.’
33 Fifi asi gala oda ilia ‘gode’, ilia da Asilia hina bagade da ili mae hasalima: ne, gaga: bela: ? Hame mabu!
Kodi mulungu wa anthu a mtundu wina uliwonse wapulumutsapo dziko lake mʼdzanja la mfumu ya ku Asiriya?
34 Amo ‘gode’ huluane wali da habila: ? Ha: ima: de fi ilia ‘gode’ amola Aba: de, Sefafa: ime, Hina, Ifai amo soge huluane ilia ‘gode’ huluane da habila: ? Nowa da Samelia gaga: bela: ?
Kodi ili kuti milungu ya Hamati ndi Aripadi? Ili kuti milungu ya Sefaravaimu, Hena ndi Ivani? Kodi inapulumutsa Samariya mʼdzanja langa?
35 Amo soge huluane ilia ‘gode’ ilia da ninia Asilia hina bagade mae hasalima: ne habogala gaga: bela: ? Ili gaga: mu da hamedei ba: i. Amaiba: le, dilia abuliba: le Hina Gode da Yelusaleme gaga: mu defele esala, dawa: sala: ?”
Kodi ndi milungu iti mwa milungu yonse ya mayiko awa amene anapulumutsa dziko lake mʼdzanja langa? Nanga tsono Yehova adzapulumutsa Yerusalemu mʼdzanja langa motani?”
36 Yuda hina bagade Hesegaia ea sia: i defele, Yelusaleme fi dunu da ouiya: le esalu. Dunu afae da hame sia: baoui.
Koma anthu anakhala chete ndipo sanayankhepo kanthu, chifukwa mfumu inawalamula kuti, “Musayankhe.”
37 Amalalu, Ilaiagime amola Siebena amola Youa da da: i dioiba: le, ilia abula gadelale sali. Ilia da Yuda hina bagadema asili, Asilia ouligisu dunu ea sia: si, ema olelei.
Pamenepo anthu atatu aja Eliyakimu, mwana wa Hilikiya amene ankayangʼanira nyumba ya mfumu, Sebina mlembi wa bwalo ndi Yowa mwana wa Asafu, mlembi wa zochitika anapita kwa Hezekiya atangʼamba zovala zawo ndipo anamuwuza Hezekiya zonse zimene anayankhula Rabusake uja.

< 2 Hina 18 >