< 2 Hina 17 >
1 Yuda hina bagade A: iha: se ea ouligibi ode fagoyale amoga, Housia (Ila egefe) da Isala: ili hina bagade hamoi. E da Samelia moilai bai bagadega esala, ode sesegeyale agoane Isala: ili fi ouligilalu.
Mʼchaka cha 12 cha Ahazi mfumu ya Yuda, Hoseya mwana wa Ela anakhala mfumu ya Israeli mu Samariya ndipo analamulira zaka zisanu ndi zinayi.
2 E da Hina Godema wadela: i hou hamoi. Be hina bagade ilia da musa: bisili Isala: ili ouligilalu, amo ilia wadela: i hou defele amai hame.
Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova, koma osafanana ndi mafumu a Israeli amene ankalamulira iye asanalowe ufumuwo.
3 Asilia hina bagade Sia: lama: nisa da ema doagala: beba: le, Housia da goaya: i. Amalalu, e da ode huluane amoga, Sia: lama: nisama su dabe i.
Salimenezeri mfumu ya ku Asiriya anabwera kudzathira nkhondo Hoseya amene anali pansi pa ulamuliro wake ndipo ankapereka msonkho kwa iyeyo.
4 Be ode afaega, Housia da sia: adola ahoasu dunu, ili Idibidi hina bagade Sou, amo ea fidisu adole ba: ma: ne, asunasi. Amalalu, e da Asilia fima odega su dabe iasu bu hame i. Sia: lama: nisa da amo nababeba: le, ea dunu ilia da Housia gagulaligili, se iasu diasu ganodini sanasi.
Koma mfumu ya ku Asiriya inazindikira kuti Hoseya akuwukira, pakuti Hoseyayo anali atatumiza nthumwi kwa So mfumu ya Igupto ndiponso analeka kukhoma msonkho kwa mfumu ya ku Asiriya, monga ankachitira chaka ndi chaka. Choncho Salimenezeri anagwira Hoseya ndi kumuyika mʼndende.
5 Amalalu, Sia: lama: nisa da Isala: ili soge doagala: le, golili sa: ili, Samelia eale disi. E da ode udiana agoanega Samelia dunu doagala: la afufusu.
Mfumu ya ku Asiriya inapita kukathira nkhondo dziko lonse la Israeli ndipo inapita mpaka ku Samariya ndipo inazinga mzindawo kwa zaka zitatu.
6 Amo ode ganodini, (Housia ea ouligibi ode sesegeyale gala) Asilia hina bagade da Samelia hasalalu, fedelai. E da Isala: ili dunu udigili hawa: hamoma: ne, Asilia sogega mugululi asi. Ea sia: beba: le, Isala: ili mugululi asi dunu mogili da Ha: ila sogega fi galu, mogili da Gousa: ne soge (Ha: ibo Hano gadenene) amola mogili da Midia soge moilai amo ganodini fi.
Mʼchaka chachisanu ndi chinayi cha Hoseya, mfumu ya ku Asiriya inalanda Samariya ndipo inatenga Aisraeli ndi kupita nawo ku Asiriya. Anakawakhazika ku Hala ndi Habori mʼmbali mwa mtsinje wa Gozani ndi mʼmizinda ya Amedi.
7 Samelia moilai bai bagade hasali ea bai da Isala: ili dunu ilia da ilia Hina Godema wadela: le hamoi. Musa: , Hina Gode da ili Idibidi hina bagadema gaga: le, Isala: ili dunu ilia Idibidi soge fisimusa: gadili oule asi. Be amo mae dawa: le, ilia Ema wadela: le hamoi. Ilia da ogogosu ‘gode’ma nodone sia: ne gadosu.
Zonsezi zinachitika chifukwa Aisraeli anachimwira Yehova Mulungu wawo, amene anawatulutsa mʼdziko la Igupto pansi pa ulamuliro wa Farao mfumu ya Igupto. Iwo ankapembedza milungu ina,
8 Ga: ina: ne soge fi musa: esalu dunu da wadela: i hou bagadedafa hamobeba: le, Isala: ili dunu da gusuba: i mogodigili ahoanoba, Hina Gode da Ga: ina: ne dunu gadili sefasi. Be Isala: ili fi dunu da Ga: ina: ne fi ilia wadela: i hou defele hamoi. Amola Isala: ili hina bagade ilia da ga fi ilia wadela: i hou hamoiba: le, Isala: ili fi dunu da amo fa: no bobogesu.
ndiponso ankatsatira miyambo ya anthu a mitundu imene Yehova anayichotsa pamene iwo ankafika mʼdzikomo pamodzinso ndi miyambo yonse imene mafumu a Israeli anayambitsa.
9 Isala: ili fi dunu da Hina Gode Ea higa: i ba: su hou, amo hamosu. Ilia da ilia moilai huluane, fonobahadi amola bagade, amo ganodini ogogosu ‘gode’ma nodone sia: ne gadosu sogebi gaguli gagai.
Ndipo Aisraeli ankachita zoyipa mwamseri kutsutsana ndi Yehova Mulungu wawo. Kuchokera ku nsanja ya alonda mpaka ku mzinda wotetezedwa, mʼmizinda yawo yonse anamangamo malo opembedzeramo mafano.
10 Agolo huluane da: iya amola ifa huluane ougiha, ilia da gele golasu ifa amola wadela: i uda ‘gode’ Asila agoaila hahamone, bugisisi.
Anayimika miyala ya chipembedzo ndi mitengo ya mafano a Asera pa phiri lililonse lalitali ndi pansi pa mtengo uliwonse wa masamba ambiri.
11 Wadela: i fi dunu amo Hina Gode da Isala: ili sogega gadili sefasi, ilia wadela: i hou defele, Isala: ili dunu da ogogosu ‘gode’ ilia oloda da: iya, gabusiga: manoma gobele salalusu. Ilia wadela: le bagadewane hamobeba: le, Hina Gode da ougi bagade ba: i.
Pa malo aliwonse opembedzera mafano, anthuwa ankafukiza lubani monga momwe ankachitira anthu a mitundu imene Yehova anayichotsa pamene iwo ankafika. Iwo anachita zinthu zoyipa zomwe zinaputa mkwiyo wa Yehova.
12 Hina Gode da ilima ogogole ‘gode’ agoai ilima mae nodone sia: ne gadoma: ne sia: i. Be ilia da Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i hamedafa nabi.
Ndipo iwowo ankapembedza mafano ngakhale Yehova ananena kuti, “Musadzachite zimenezi.”
13 Hina Gode da musa: Ea sia: adola ahoasu dunu amola balofede dunu ili Isala: ili fi amola Yuda fi ilima sisane amane sia: ma: ne asunasi. “Dilia wadela: i hou yolesili, Na hamoma: ne sia: i nabawane hamoma! Na hamoma: ne sia: i huluane da Sema (amo Na da Na hawa: hamosu balofede dunu ilia lafidili dilia aowalalima iasu) amo ganodini dedei diala.”
Yehova anachenjeza Israeli ndi Yuda kudzera mwa aneneri ake onse ndi alosi kuti, “Lekani mchitidwe wanu woyipawo. Mverani malamulo anga ndi malangizo anga potsatira zonse zolembedwa mʼmalamulo a Mose, zimene ndinalamulira makolo anu kuti azimvere, kudzera mwa aneneri, atumiki anga.”
14 Be ilia da nabasu hou hamedafa dawa: i. Ilia aowalalia da Hina Gode Ea hou dafawaneyale hame dawa: i, amola Isala: ili fifi misi dunu da ilia hou defele, gawamaga: i.
Koma anthuwa sanamvere ndipo anawumitsa khosi ngati momwe analili makolo awo, amene sanadalire Yehova Mulungu wawo.
15 Ilia Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i hame nabasu. Ilia da hamedei loboga hamoi ‘gode’ agoaila ilima nodone sia: ne gadoiba: le, ilisu da hamedei dunu agoai ba: i. Ilia da fifilai ilia soge sisiga: le dialu, amo ilia hou fa: no bobogei. Ilia da Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i, “Ga fi ilia hou defele mae hamoma!” amo nabawane hame hamosu.
Anakana malangizo ake ndi pangano anachita ndi makolo awo ndipo ananyoza zochenjeza za Yehova. Iwo anatsatira mafano achabechabe nasanduka achabechabe. Anthuwa anatsanzira mitundu ya anthu owazungulira ngakhale kuti Yehova anawalamula kuti, “Musamachite zomwe iwo amachita,” koma iwo anachita zomwe Yehova anawaletsa.
16 Ilia da ilia Hina Gode Ea sema huluane fi dagoi. Ilia da amoma nodone sia: ne gadomusa: , bulamagau gawali mano aduna gouliga hamoi. Amola ilia da ogogosu uda ‘gode’ Asila e agoaila hamoi, amola gasumuni ilima nodone sia: ne gadosu, amola ogogosu ‘gode’ Ba: ilema hawa: hamosu.
Iwowo anasiya malamulo onse a Yehova Mulungu wawo, nadzipangira mafano awiri osungunula a ana angʼombe ndiponso fano la Asera, napembedza zonse zamlengalenga ndi kutumikira Baala.
17 Ilia da ilia dunu mano amola ilia uda mano amo ogogosu ‘gode’ma wadela: i hou dabe ima: ne, gobele salalusu. Ilia da gesami dasu amola wadela: i ba: la: lusu dunu, ilima fada: i sia: nabi. Ilia eno liligi mae dawa: le, Hina Gode ba: ma: ne, wadela: i hou fawane hamonanusu. Amaiba: le, Hina Gode da ougi ba: i.
Ndipo anadutsitsa mʼmoto ana awo aamuna ndi aakazi. Iwo ankawombeza mawula, namachitanso zanyanga ndipo anadzipereka kuchita zoyipa pamaso pa Yehova namukwiyitsa.
18 Hina Gode da Isala: ili fi ilima ougiba: le, E da ili bu mae ba: ma: ne, ili mugululi ga asunasi. Yuda fi fawane da ilia soge ganodini esalebe ba: i.
Choncho Yehova anakwiya nawo kwambiri Aisraeli ndipo anawachotsa pamaso pake. Palibe amene anatsala kupatula fuko la Yuda lokha.
19 Be Yuda fi amolawane da ilia Hina Gode Ea sema nabawane hame hamosu. Ilia da Isala: ili fi ilia hou lalegagui, amo ba: beba: le, defele hamoi.
Yuda nayenso sanasunge malamulo a Yehova Mulungu wawo. Iwo ankatsatira machitidwe amene Israeli anayambitsa.
20 Hina Gode da Isala: ili fi higale, ilima dawa: ma: ne se dabe i, amola E da logo doasiba: le, dodona: gi ha lai dunu da ilima se bagade iasu. Amalalu, E da ili bu mae ba: ma: ne, ili mugululi ga asunasi.
Motero Yehova anakana Aisraeli onse. Iye anawazunza nawapereka mʼmanja mwa anthu ofunkha mpaka Iye atawachotseratu pamaso pake.
21 Hina Gode da Isala: ili mogili, na: iyado Isala: ili amola na: iyado Yuda hamonanu, Isala: ili fi da Yelouboua: me (Niba: de egefe) ilia hina bagade hamoi. Yelouboua: me da ili Hina Gode yolesima: ne hamoi, amola wadela: i hou baligili hamoma: ne, ili oule asi.
Yehova atangʼamba Israeli kumuchotsa ku nyumba ya Davide, Aisraeliwo anasankha Yeroboamu mwana wa Nebati kukhala mfumu yawo. Yeroboamu ananyengerera Aisraeli kuti asatsatire Yehova ndipo anawachimwitsa tchimo lalikulu.
22 Ilia da Yelouboua: mema fa: no bobogele, wadela: i hou huluane ea hamosu, amo defele hamoi.
Aisraeli anakakamira machimo onse amene Yeroboamu anachita ndipo sanawasiye
23 Amalalu, fa: no Hina Gode da E da musa: Ea balofede dunu amodili sisai defele, ili ba: mu higa: iba: le, ilia sogega fadegale, mugululi ga asunasi.
mpaka pamene Yehova anawachotsa pamaso pake monga anawachenjezera kudzera mwa atumiki ake onse, aneneri. Choncho Aisraeli anachotsedwa mʼdziko lawo kupita ku ukapolo ku Asiriya ndipo ali komweko mpaka lero lino.
24 Asilia hina bagade da Isala: ili dunu Samelia soge ganodini esalu, mugululi Asilia sogega asunasi. Amalalu, e da Asilia dunu amo da Ba: bilone, Giudia, Aifa, Ha: ima: de, Sefafa: ime amo ganodini esalu, amo dunu lale, ili huluane Samelia soge ganodini ha: ini fima: ne oule asi. Ilia da Samelia soge moilai huluane lale, amo ganodini ha: ini fi.
Mfumu ya ku Asiriya inabweretsa anthu a ku Babuloni, Kuta, Awa, Hamati ndi a ku Sefaravaimu kudzawakhazika mʼmizinda ya Samariya kulowa mʼmalo mwa Aisraeli. Iwo anatenga Samariya ndi kukhala mʼmizinda yake.
25 Ilia da degabo ha: ini fisia, ilia da Hina Godema hame nodone sia: ne gadosu. Amaiba: le, Hina Gode da laione wa: me asunasili, ili mogili fane legei.
Iwo atayamba kukhala kumeneko, sanapembedze Yehova choncho Yehova anatumiza mikango pakati pawo ndipo inapha ena mwa iwo.
26 Asilia hina bagade da dunu e da Samelia soge ganodini ha: ini fima: ne asunasi, amo da Samelia sogega Gode sema amo noga: le hame dawa: beba: le, amo Gode da ili medoma: ne laione wa: me asunasi, amane sia: nabi.
Tsono mfumu ya ku Asiriya inawuzidwa za nkhaniyi kuti, “Anthu amene munawatumiza ndi kuwakhazika mʼmizinda ya Samariya sakudziwa chimene Mulungu wa dzikolo amafuna. Choncho Iye watumiza mikango pakati pawo imene ikuwapha chifukwa anthuwo sadziwa chimene Mulungu wa dzikolo amafuna.”
27 Amaiba: le, e da amane hamoma: ne sia: i, “Gobele salasu dunu amo nini gagulaligisa, niniga afae bu asunasima. E da Samelia sogega bu fimusa: ahoanoba, e da ninia dunuma, Samelia soge fi ilia sema noga: le olelema: ne sia: ma!”
Tsono mfumu ya ku Asiriya inalamula kuti, “Tengani wansembe mmodzi mwa amene munawagwira ukapolo, mupite naye kumeneko ndipo akakhale komweko nakaphunzitse anthu zimene Mulungu wa dzikolo amafuna.”
28 Amaiba: le, Isala: ili mugululi asi gobele salasu dunu afae da Bedele moilaiga buhagi. Amogawi, e da dunu ilima Hina Godema nodone sia: ne gadosu hou olelei.
Choncho mmodzi mwa ansembe amene anawatenga ku Samariya anabwera kudzakhala ku Beteli ndipo ankaphunzitsa anthuwo kupembedza Yehova.
29 Be Asilia dunu amo da Samelia ganodini ha: ini fi, ilia da mae fisili, ilia loboga hamoi ‘gode’ liligi hamosu. Ilia da amo liligi ilima nodone sia: ne gadosu sogebi amo Isala: ili dunu da hamoi, amo ganodini sali. Momogi afae afae da loboga hamoi ‘gode’ afae afae ilia esalebe moilai ganodini hahamoi.
Koma mtundu uliwonse wa anthu unkapangabe mafano a milungu yawoyawo mʼmizinda yambiri imene anthuwo ankakhala, ndipo anayika milunguyo mʼnyumba za milungu zimene anthu a ku Samariya anamanga ku malo opembedzera mafano.
30 Ba: bilonega misi dunu da ogogosu ‘gode’ Sagode Binode amo agoaila hahamoi. Guidiaga misi dunu da ogogosu ‘gode’ Na: igale amo agoaila hahamoi. Ha: ima: dega misi dunu da ogogosu ‘gode’ Asiaima amo agoaila hahamoi.
Anthu a ku Babuloni anapanga Sukoti-Benoti, anthu a ku Kuti anapanga Nerigali, ndipo anthu a ku Hamati anapanga Asima;
31 Aifaga misi dunu da ogogosu ‘gode’ Nibiha: se amola Dada: ge elea agoaila hahamoi. Amola Sefafa: imega misi dunu da ilia ogogosu ‘gode’ aduna, Ana: melege amola A: dala: melege elama ilia mano gobele salalusu.
Aava anapanga Nibihazi ndi Taritaki, ndipo Asefaravaimu ankawotcha ana awo pa moto ngati nsembe kwa Adirameleki ndi Anameleki, milungu ya Asefaravaimu.
32 Amo dunu huluane da Hina Godema amolawane nodone sia: ne gadoi. Ilia da ilia gilisisu amoga dunu amo gobele salasu dunu hamoma: ne udigili ilegei. Amo dunu da ilia ogogosu ‘gode’ oloda amoga gobele salasu hou hamonanusu.
Iwo ankapembedza Yehova, koma ankadzisankhira okha pakati pawo anthu wamba kuti akhale ansembe awo ku nyumba za milungu za ku malo opembedzera mafano.
33 Amaiba: le, ilia da Hina Godema nodone sia: ne gadosu, be ilia da soge fi amoga ilia misi, amo ilia hou defele, ogogosu ‘gode’ ilima gilisili nodone sia: ne gadosu.
Iwowo ankapembedza Yehova, komanso ankatumikira milungu yawo molingana ndi miyambo ya mitundu ya kumene ankachokera.
34 Amola ilia da amogainini wali eso amola ilia musa: hou hamonana. Ilia da Hina Godema nodone sia: ne gadosu hame hamosa. Amola ilia da sema amola hamoma: ne sia: i amo E da Ya: igobe (Gode da ema Isala: ili dio asuli) amo egaga fima i, amo ilia da nabawane hame hamosa.
Mpaka lero lino iwo akupitirizabe kuchita zimene ankachita poyamba. Sapembedza Yehova kapenanso kutsata malangizo ake ndi malamulo ake, chiphunzitso chake monga mwa malamulo amene Yehova anawapereka kwa zidzukulu za Yakobo, amene anamutcha Israeli.
35 Hina Gode da musa: Isala: ili dunuma gousa: su hamoi. Amola E da ilima amane hamoma: ne sia: i, “Eno ‘gode’ ilima mae nodone sia: ne gadoma. Ilima mae beguduma, amola ilima gobele salasu hou mae hamoma!
Pamene Yehova anachita pangano ndi Aisraeli, Iye anawalamula kuti, “Musapembedze milungu ina kapena kuyigwadira iyo, kuyitumikira kapena kupereka nsembe kwa iyoyo.
36 Na, Hina Godedafa, da gasa bagadewane dili Idibidi sogega esalu, gadili oule asi. Amaiba: le, dilia Na hamoma: ne sia: i fawane nabima! Dilia Nama fawane beguduma, amola Nama fawane gobele salasu hamoma!
Koma Yehova amene anakutulutsani mʼdziko la Igupto ndi dzanja lake lamphamvu ndiye amene muyenera kumupembedza.
37 Dilia eso huluane, sema amola hamoma: ne sia: i, Na da dilia dawa: ma: ne dedei, amo huluane nabawane hamoma! Eno ‘gode’ma nabasu hou maedafa hamoma!
Muyenera kusamalitsa nthawi zonse kusunga malangizo anga ndi malemba anga, chiphunzitso ndi malamulo amene anakulemberani. Musapembedze milungu ina.
38 Amola gousa: su amo Na da dilima hamoi, amo maedafa gogolema!
Musayiwale pangano limene ndinapangana nanu ndipo musamapembedze milungu ina.
39 Na da dilia Hina Godedafa! Na sia: fawane nabima! Amasea, Na da dilima ha lai dunu amoga gaga: mu.”
Mʼmalo mwake muzipembedza Yehova Mulungu wanu pakuti ndiye amene adzakulanditsani mʼdzanja la adani anu onse.”
40 Be eno Samelia sogega misi dunu da Gode Ea Sia: nabimu higa: i. Ilia da mae fisili, ilia musa: hou hamonanusu.
Komabe iwo sanamvere ndipo anapitiriza kuchita zomwe ankachita kale.
41 Amaiba: le, amo dunu da Hina Godema nodone sia: ne gadoi, amola gilisili ilia ogogosu loboga hamoi ‘gode’, ilima nodone sia: ne gadosu. Amola amogainini wali eso iligaga fi da amaiwane hamosa.
Ngakhale anthuwo ankapembedza Yehova, ankatumikiranso mafano awo. Mpaka lero lino ana awo ndi zidzukulu zawo zikupitiriza kuchita zomwe ankachita makolo awo.