< Yohani 19 >

1 Pe pano uPilato akantoola uYesu na kukunkopa ni mijeledi.
Kenaka Pilato anatenga Yesu namukwapula mwankhanza.
2 Avasikali vala vakatenda ingeela ija mifua, vakamfwasia ku mutu, kange vakamfwasia isopeka indangali.
Asilikali analuka nkhata yaminga ndi kumuveka pamutu pake. Kenaka anamuveka mkanjo wapepo
3 Pe vakava viveela kwa mwene na kukunnenela viiti, “Uve, ghwe ntwa ghwa Vayahudi! Vakava vikuntova na mapi.
ndipo ankapita kwa Iye mobwerezabwereza ndi kumanena kuti, “Moni mfumu ya Ayuda?” Ndipo amamumenya makofi.
4 akahuma kange kunji, akavavuula akati, “Pulikisia, umuunhu nikumuleta kulyumue kunji kuno mukagule kuuti une nanikuvwagha uvuhosi vumonga kwa mwene.”
Pilato anatulukanso ndipo anati kwa Ayuda, “Taonani, ine ndikumubweretsa kuti inu mudziwe kuti ine sindikupeza chifukwa chomuyimbira mlandu.”
5 Pe uYesu akahuma kunji afwalile ingeela ija mifua ni sopeka indangali. UPilato akajova akati, 'Lolagha, umunu ujuo ghwe uju.”
Pamenepo Yesu anatuluka atavala nkhata yaminga ndi mkanjo wapepo ndipo Pilato anawawuza kuti, “Nayu munthu uja!”
6 Avavaha va vatekesi na valoleleli ye vamwaghile, vakoova vakati, “Unkomelele pa kikovekano!” UPilato akavavuula akati, “Muntoole jumue mukankomelele, ulwakuva une nivona nsila nkome.”
Atangomuona Iye akulu a ansembe ndi akuluakulu ena anafuwula kuti, “Mpachikeni! Mpachikeni!” Koma Pilato anayankha kuti, “Inu mutengeni ndi kumupachika. Koma ine sindikupeza chifukwa chomuyimbira mlandu.”
7 Avayahudi vakamwamula vakati, “Usue tuli nu lulaghilo, vwimila ululaghilo uluo uju anoghile kufua ulwakuva umwene ivikile Mwana ghwa Nguluve.
Ayuda anayimirira nati, “Ife tili ndi lamulo, ndipo molingana ndi lamulolo, Iyeyu ayenera kuphedwa chifukwa akudzitcha kuti ndi Mwana wa Mulungu.”
8 UPilato ye apulike amasio aguo, akoghopa kyongo,
Pilato atamva zimenezi, anachita mantha kwambiri,
9 pe akingila kange munyumba jaake ija kitwa, akamposia uYesu akati, 'Uve ghuhuma kuughi?” Neke uYesu naalyamwamwile kimonga.
ndipo anabwereranso mʼnyumba yaufumu. Iye anafunsa Yesu kuti, “Kodi umachokera kuti?” Koma Yesu sanayankhe.
10 Pe uPilato akati, “Kiki naghukunyamula? Asi, nukagwile kuuti une nili nu vutavulilua uvwa kukudindulila, nu vwa kukukomelela pa kikovekano?
Pilato anati, “Kodi ukukana kundiyankhula ine? Kodi sukuzindikira kuti ine ndili ndi mphamvu yokumasula ndiponso mphamvu yokupachika?”
11 UYesu akamwamula akati, “Uve naghwale ghuuva nu vutavulilua kulyune, nave nupelilue kuhuma kukyanya. Lino umuunhu juno ambikile mu mavoko ghaako mhosi kukila uve.”
Yesu anayankha kuti, “Inu simukanakhala ndi mphamvu pa Ine akanapanda kukupatsani kumwamba. Nʼchifukwa chake amene wandipereka Ine kwa inu ndiye wochimwa kwambiri.”
12 Kuhuma unsiki ughuo, uPilato akava ilonda isila ija kun'dindulila uYesu. Neke aVayahudi vakoova vakati, “Ungan'dindulile umuunhu uju, naghuuva mmanyaani ghwa ntwa um'baha uKaisali. Umuunhu juno ikuviika kuuva ntwa, ikaana uvutwa vwa ntwa umbaha uKaisali.”
Kuyambira pamenepo Pilato anayesa kuti amumasule Yesu, koma Ayuda anapitirira kufuwula kuti, “Ngati mumumasula munthuyu kuti apite, inu si bwenzi la Kaisara.”
13 UPilato ye apulike amasio aghuo, akahuma nu Yesu kunji, akikala pa kitengo kya vuhighi, munjovele ija Kiebulania pitambulua Gabata kwe kuti, Lwalo lwa mavue.
Pilato atamva zimenezi, iye anamutulutsa Yesu kunja ndi kukhala pansi pa mpando wa woweruza pamalo otchedwa Mwala Wowaka (umene pa Chiaramaiki ndi Gabata).
14 Ikighono ikio kilyale kighono kya kuling'hania ikyimike ikya Pasaka, kaale kavalilo ka ntanda ndiiki. UPilato akavavuula aVayahudi akati, “Lolagha, uju ghwe ntwa ghwinu!”
Linali tsiku lokonzekera Sabata la Paska ndipo nthawi inali ora lachisanu ndi chimodzi masana. Pilato anati kwa Ayuda, “Nayi mfumu yanu.”
15 Aveene vakoova vakati “M'busie, m'busie, unkomelele pa kikovekano.” UPilato akavaposia akati, “Asi, ninkomelele pa kikovekano untwa ghwinu?” Avavaha va vatekesi vakati, “Usue natuli nu ntwa ujunge, looli ju Kaisali!”
Koma iwo anafuwula kuti, “Choka nayeni! Choka nayeni! Mpachikeni!” Pilato anafunsa kuti, “Kodi ine ndipachike mfumu yanuyi?” Akulu a ansembe anayankha kuti, “Ife tilibe mfumu ina koma Kaisara.”
16 Pe pano uPilato akam'biika uYesu mumavoko ghaake kuuti vankomelele
Pomaliza Pilato anamupereka kwa iwo kuti akapachikidwe. Choncho asilikali anamutenga Yesu.
17 Pe vakantoola uYesu, akahuma mulikaaja apindile ikikovekano kyake kuhanga kufika pano pakatambulwagha mu Kiebulania Golgota, kwekuti ling'hala lya mutu.
Atanyamula mtanda wake, anapita kumalo otchedwa “Malo a Bade” (mʼChiaramaiki amatchedwa Gologota).
18 Apuo vakankomelela uYesu palikimo na vange vavili, jumo ulubale ulwa kundio ujunge ulwa kung'highi umwene akava pakate.
Pamenepo iwo anamupachika Iye pamodzi ndi anthu ena awiri, mmodzi mbali ina ndi wina mbali inanso ndipo Yesu pakati.
19 Pepano uPilato akalemba amasio na kuviika pakyanya pa kikovekano kya Yesu. Amasio aghuo ghalyalembilue, 'UYESU UMUNASALETI, UNTWA GHWA VAYAHUDI.
Pilato analemba chikwangwani chomwe anachikhoma pa mtandapo. Panalembedwa mawu akuti, yesu wa ku nazareti, mfumu ya ayuda.
20 Amasio aghuo ghalyalembilue mu njovele ija Kiebulania, ija Kilooma nija Kiyunaani. Avaanhu vinga vakava vikwimba amalemba aghuo, ulwakuva pano alyakomelilue palyale piipi ni likaaja.
Ayuda ambiri anawerenga chikwangwanichi, pakuti pamalo pamene Yesu anapachikidwapo panali pafupi ndi mzinda ndipo chikwangwanicho chinalembedwa mu Chiaramaiki, Chilatini ndi Chigriki.
21 Avavaha va vatekesi ava Vayahudi vakam'buula iPilato vakati, “Nungalembaghe, 'Ntwa ghwa Vayahudi; ulembe kuuti,' Umuunhu uju alyatiile, UNE NENE NTWA GHWA VAYAHUDI.”
Kenaka mkulu wa ansembe wa Ayuda anakadandaula kwa Pilato nati, “Musalembe kuti ‘Mfumu ya Ayuda,’ koma kuti munthuyu amadzitcha kuti ndi mfumu ya Ayuda.”
22 UPilato akavamula akati, “Sino nilembile, nilembile.”
Pilato anayankha kuti, “Chimene ine ndalemba, ndalemba.”
23 Avasikali ye vankomeliile uYesu vakatoola amenda ghaake, vakaghava fighavo fine, pe nujunge akatoola ikighavo kyake. Kange vakatoola isopeka jaake. Isopeka ijio najilyahonilue, ulwene jilyatavulue kuhuma ku mutu kuhanga kufika ku maghulu.
Asilikali atamupachika Yesu, anatenga zovala zake ndi kuzigawa zigawo zinayi, gawo limodzi la aliyense wa iwo, ndi kutsala mwinjiro wamʼkati wokha. Chovala ichi chinawombedwa kuyambira pamwamba mpaka pansi wopanda msoko.
24 Avasikali avuo vakavulana vakati, “Isopeka iji tuleke pidemula, ulwene tusodolele kuuti jiive jaani. “Isio silyavombiike kukwilanisia aMalembe aMimike ghano ghiiti, “Valyaghavinie amenda ghango na kuviika ulusodolelo isopeka jaango.”
Iwo anati kwa wina ndi mnzake, “Tiyeni tisachingʼambe koma tichite maere kuti tione amene achitenge.” Izi zinachitika kuti malemba akwaniritsidwe amene anati, “Iwo anagawana zovala zanga pakati pawo ndi kuchita maere pa zovala zangazo.” Choncho izi ndi zimene asilikali anachita.
25 Enendiiki fye valyavombile avasikali. Un'ghina ghwa Yesu, unnuuna ghwa ng'ina ghwa Yesu, UMaliamu umhuma mu kikaja ikya Magidala, vakimile piipi ni kikovekano kya Yesu.
Pafupi ndi mtanda wa Yesu panayima amayi ake, mngʼono wa amayi ake, Mariya mkazi wa Kaliyopa ndi Mariya wa ku Magadala.
26 UYesu akamwagha ung'ina nu m'bulanisivua juno alyamughanile, vimile piipi nu mwene, akam'buula ung'ina akati, “Mama, lolagha ujuo mwanaako.”
Yesu ataona amayi ake pamenepo ndi wophunzira amene Iye anamukonda atayima pafupipo, Iye anati kwa amayi ake, “Amayi nayu mwana wanu.”
27 Kange akam'buula um'bulanisivua jula akati, “Lolagha, ujuo mama ghwako.” Unsiki ughuo um'bulanisivua jula akantoola umama jula, kuluta naghwo kukaaja kwa mwene.
Anawuzanso wophunzirayo kuti, “Nawa amayi ako.” Kuyambira nthawi imeneyo, wophunzirayo anatenga amayiwo kupita nawo kwawo.
28 UYesu ye avwene sooni sivombike akati, “Numilue.” Alyajovile enendiiki kukwilanisia aMalembe aMimike.
Atadziwa kuti zonse zatha tsopano komanso kuti malemba akwaniritsidwe, Yesu anati, “Ine ndili ndi ludzu.”
29 Apoonu pala pwekilyale ikikong'olo kino kimemile uluhuuje ulukali ulwa sabibu. Vakatoola ikyenda vakasuvika mu luhuuje, vakakinjenga mu lupiki ulwa mpiki umuhisopo, vakantwalila pa mulomo.
Pomwepo panali mtsuko wodzaza ndi vinyo wosasa, choncho iwo ananyika chinkhupule ndi kuchisomeka ku mtengo wa hisope nachifikitsa kukamwa kwa Yesu.
30 UYesu ye anywile uluhuuje lula akati, “Sooni sivombiike!” Akinamisia umutu, akakunguka.
Yesu atalandira chakumwachi anati, “Kwatha.” Ndipo Iye anaweramitsa mutu wake napereka mzimu wake.
31 Ikighono ikio kyale kighono kya kuling'hania iSabati. Avayahudi navakalondagha amavili gha vafue ghajighe pa kikovekano pa kighono ikya Sabati, ulwakuva ikighono ikio kilyale kivaha! Pe vakansuuma uPilato avitikisie kuuti amaghulu agha vanhu avuo, ghadenyue, neke vavavusie pa kiko vekano.
Popeza linali Tsiku Lokonzekera ndipo tsiku linalo linali Sabata lapadera; Ayuda sanafune kuti mitembo ikhale pa mtanda pa Sabata, iwo anapempha Pilato kuti akathyole miyendo ndi kutsitsa mitemboyo.
32 Pe avasikali vakaluta, vakadeenya amaghulu agha muunhu ghwa kwanda nu ghwa vuvili vano valyakomelilue palikimo nu Yesu.
Chifukwa chake asilikali anabwera ndi kuthyola miyendo ya munthu oyamba amene anapachikidwa ndi Yesu ndipo kenaka ya winayo.
33 Neke ye vafikile pa Yesu, vakavona afwile. Mu uluo navakadeenya amaghulu ghaake.
Koma atafika pa Yesu ndi kupeza kuti anali atamwalira kale, iwo sanathyole miyendo yake.
34 Umuunhu umo mu vasikali akamhoma ni mhalala uYesu pa luvafu, jikahuma idanda na malenga.
Mʼmalo mwake, mmodzi wa asilikaliwo anamubaya Yesu ndi mkondo mʼnthiti, ndipo nthawi yomweyo munatuluka magazi ndi madzi.
35 Imhola isi silembilue nu muunhu juno alyasivwene ye sivombeka. Sino ijova sa kyang'haani, kange ghwope akagwile kuuti sino ijova sa kyang'haani, ikwoleka neke na jumue mwitike.
Munthu amene anaona izi wapereka umboni ndipo umboni wake ndi woona. Iye akudziwa kuti akunena choonadi kuti inunso mukhulupirire.
36 Isio silyavombiiki kukwilanisia aMalembe aMimike ghano ghiiti, “Nambe umfupa ghwake ghumo naghudenyua.
Zinthu izi zinachitika kuti malemba akwaniritsidwe: “Palibe limodzi la mafupa limene lidzathyoledwa,”
37 Kange aMalembe aMimike aghange ghiiti” Vikumulolagha juno vamhomile.”
ndi monga lemba linanso linena, “Iwo adzayangʼana Iye amene iwo anamubaya.”
38 Isio ye sivombiike, akiisa uYesufu umhuma mu likaaja ilya Alimatia. Umuunhu uju alyale m'bingilili ghwa Yesu kisyefu, ulwakuva akoghopa avalongosi va Vayahudi. Akansuuma uPilato kuuti avusie um'bili ghwa Yesu pakikovekano. UPilato akamwitikisia, pe akaluta akaghuvusia.
Kenaka, Yosefe wa ku Arimateyu anakapempha mtembo wa Yesu kwa Pilato. Tsono Yosefe anali wophunzira wa Yesu koma mobisa chifukwa iye ankaopa Ayuda. Atalandira chilolezo kwa Pilato, anakatsitsa mtembo wa Yesu.
39 Naju Nikodemu, juno ikighono kimonga alyalutile kwa Yesu pakilo, akiisa na mafuta amanya lunusi ulunono. Amafuta aghuo ghalyale ikiilo fijigho fitatu ndiiki.
Nekodimo, munthu amene poyamba pake anabwera kwa Yesu usiku, anatenga mafuta osakaniza ndi mure ndi aloe wolemera pafupifupi makilogalamu 32.
40 Vooni ve vaviili vakatoola umbili ghwa Yesu vakaghuniengelela nu mwenda umpala palikimo na mafuta ghala amanya lunusi ulunono ndavule lulyale lwiho lwa Vayahudi ulwa kusyila avaanhu.
Pamenepo anatenga mtembo wa Yesu nawukulunga pamodzi ndi zonunkhiritsa mu nsalu za mtundu woyera monga mwa mwambo wa maliro wa Ayuda.
41 Pano valyankomeliile uYesu pweghulyale umughunda. Mu mughunda ghula mwejilyale imbiipa imia jino navaghelile kuviika nambe muunhu.
Pamalo pamene anapachikidwa Yesu panali munda ndipo mʼmundamo munali manda atsopano mʼmene munali simunayikidwemo aliyense.
42 Lino, ulwakuva ku Vayahudi ikighono kyale kighono ikya kuling'hania iSabati, vakaviika um'bili ghwa Yesu mu mbiipa jila, ulwakuva jilyale piipi.
Chifukwa linali Tsiku la Ayuda Lokonzekera ndi kuti mandawo anali pafupipo, iwo anayika Yesu mʼmenemo.

< Yohani 19 >