< 1 Vathesalonike 3 >
1 Mu uluo panonatukale natuwesia kufumilia kyongo, kutasaghile kuva kanono kujigha ku athene kula twevene.
Nʼchifukwa chake pamene sitinathenso kupirira, tinaganiza kuti kunali bwino kuti atisiye tokha ku Atene.
2 Tulyan'sughile u timotheo, unyalukolo ghwitu nu n'sughwa ghwa Nguluve mulivangili lya Kilisite, kukuvakangasia na kuvavavighilila kulutia ulwitiko lwinu.
Tinatuma Timoteyo, mʼbale wathu ndi mnzathu wogwira naye ntchito ya Mulungu yofalitsa Uthenga Wabwino wa Khristu, kuti adzakulimbitseni mitima ndi kukukhazikitsani mʼchikhulupiriro chanu,
3 Tulyavombile agha neke kuti nangavisaghe ghoghoni ughwa kutetema nulupumuko ulu, lwakuva jumue mkagula kuti tusalulivue mu ili.
ndi cholinga chakuti wina asasunthike ndi mavutowa. Inu mukudziwa bwino lomwe kuti ndife oyenera kukumana ndi zimenezi.
4 Lwa lweli, un'siki ghunotulyale palikomo numue, tulyalongwile kukuvelesia kuva tulyale pipi kupata ulupumuko, naghuo ghakahumile ndavule mkagula.
Kunena zoona, pamene tinali nanu, tinkakuwuzani kuti tidzayenera kuzunzidwa. Ndipo monga mukudziwa bwino, zimenezi zinachitikadi.
5 Kunangile ja iji panonikale naniwesia kufumilila kange, nilyan'sung'ile neke nipate kukagula mulwitiko lwinu. labda umuhesi alyale avaghesisie, ni mbombo jinu jikiva vuvule.
Nʼchifukwa chake, pamene sindikanathanso kupirira, ndinatuma Timoteyo kuti adzaone mmene chikhulupiriro chanu chilili. Ndinkaopa kuti mwina wonyengayo, wakunyengani mʼnjira ina yake ndi kuti ntchito zathu zasanduka zosapindula.
6 Neke lelo utumotheo alisile kuyusue kuhumila kulymue akatuletela imhola inofu ja lwitiko nulughano lwinu. alyatuvulile ja kuti mulinikumbukumbu jitu nakuti munoghelua kukutuvona ndavule pano najusue tunoghelua kukuvavona umue.
Koma tsopano Timoteyo wabwera kuchokera kwanuko ndipo watibweretsera nkhani yabwino ya chikhulupiriro chanu ndi chikondi chanu. Iye watiwuzanso kuti masiku onse mumatikumbukira mokondwa, ndipo kuti mumafunitsitsa kutionanso, monga momwe ifenso timalakalakira kukuonani inuyo.
7 Mu uluo, vanyalukolo tukahovwike kyongo numue vwimila mu lwitiko lwinu, taabu ni mumuko situ soni.
Motero abale, mʼmasautso ndi mʼmazunzo athu onse, chikhulupiriro chanu chatilimbikitsa.
8 Lino tukukala tukukala, ndeve mukwima kikangafu mwa Mutwa.
Ife tsopano tili moyodi, pakuti mukuyima molimbika mwa Ambuye.
9 Neke lwe luhongesio luki tum'pele u Nguluve kwaajili jinu, mulukelo lwoni tulinalwo pamaso gha Nguluve kulyumue?
Tingathe bwanji kuyamika Mulungu mokwanira poona chimwemwe chonse chimene tili nacho pamaso pa Mulungu wathu chifukwa cha inu?
10 Tusuma kyongo pakilo napamwisi neke tuwesie kukusagha isula sinu na kukuvongelesia kinokipunguka mu lwitiko lwinu.
Usana ndi usiku timapemphera ndi mtima wonse kuti tionanenso nanu, ndi kukwaniritsa zimene zikusowa pa chikhulupiriro chanu.
11 Unguluve ghwitu nu Naata jujuo, nu Mutwa ghwitu u Yesu atulongosie isila jitu tufike kulyumue,
Tikupempha kuti Mulungu ndi Atate athu mwini, ndi Ambuye athu Yesu, atikonzere njira yabwino kuti tidzafike kwanuko.
12 nu Mutwa avavombe mwongelele na kukila mu lughano, mungaghanane nakuvaghana avanhu voni, ndavule finotukuvavombela umue.
Ambuye achulukitse chikondi chanu ndi kuti chisefukire kwa wina ndi mnzake ndiponso kwa wina aliyense, monga momwe chikondi chathu chichitira kwa inu.
13 Naavombe ndiki neke kukangasia amojo ghinu ghave kisila lupiko muvwimike pamaso gha Nguluve ghwitu nu Naata ghwitu mulwisilo/pavugomokele vwa Mutwa Yesu palikimo na vimike vake vooni.
Iye alimbikitse mitima yanu kuti mukhale opanda cholakwa ndi oyera mtima pamaso pa Mulungu ndi Atate athu pamene Ambuye athu Yesu akubwera ndi oyera ake onse.