< Zǝbur 57 >
1 Nǝƣmiqilǝrning bexiƣa tapxurulup, «Ⱨalak ⱪilmiƣaysǝn» degǝn aⱨangda oⱪulsun dǝp, Dawut yazƣan «Mihtam» küyi, (u Saul padixaⱨtin ⱪeqip, ɵngkürdǝ yoxurunuwalƣan qaƣda yezilƣan): — I Huda, manga xǝpⱪǝt kɵrsǝtkǝysǝn, Manga xǝpⱪǝt kɵrsǝtkǝysǝn, Qünki jenim Seni panaⱨim ⱪildi. Muxu balayi’apǝt ɵtüp kǝtküqǝ, ⱪanatliring sayisidǝ panaⱨ tapimǝn.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Ndakatulo ya Davide, pamene anathawa Sauli kupita ku phanga. Mundichitire chifundo, Inu Mulungu mundichitire chifundo, pakuti mwa Inu moyo wanga umathawiramo. Ndidzathawira mu mthunzi wa mapiko anu mpaka chiwonongeko chitapita.
2 Hudaƣa, yǝni Ⱨǝmmidin Aliy Bolƣuqiƣa, Ɵzüm üqün ⱨǝmmini orunlaydiƣan Tǝngrigǝ nida ⱪilimǝn;
Ine ndikufuwulira kwa Mulungu Wammwambamwamba, kwa Mulungu amene amakwaniritsa cholinga chake pa ine.
3 U ǝrxtin yardǝm ǝwǝtip meni ⱪutⱪuzidu; Manga ⱪarap nǝpsi yoƣinap, meni ⱪoƣlawatⱪanlarni U rǝswa ⱪilidu; (Selaⱨ) Huda Ɵz meⱨir-xǝpⱪiti wǝ ⱨǝⱪiⱪitini ǝwǝtidu!
Mulungu amanditumizira kuchokera kumwamba ndi kundipulumutsa, kudzudzula iwo amene akundithamangitsa kwambiri. Mulungu amatumiza chikondi chake ndi kukhulupirika kwake.
4 Jenim xirlar arisida ⱪaldi; Mǝn nǝpisi yalⱪun kǝbi bolƣanlar arisida yatimǝn! Adǝm baliliri — Ularning qixliri nǝyzǝ-oⱪlardur, Ularning tili — ɵtkür ⱪiliqtur!
Ine ndili pakati pa mikango, ndagona pakati pa zirombo zolusa; anthu amene mano awo ndi milomo yawo ndi mivi, malilime awo ndi malupanga akuthwa.
5 I Huda, ǝrxlǝrdin yuⱪiri uluƣlanƣaysǝn, Xan-xǝriping yǝr yüzini ⱪapliƣay!
Mukwezekedwe Inu Mulungu, kuposa mayiko onse akumwamba; mulole kuti ulemerero wanu ukhale pa dziko lonse lapansi.
6 Ular ⱪǝdǝmlirimgǝ tor ⱪurdi; Jenim egilip kǝtti; Ular mening yolumƣa orǝk koliƣanidi, Lekin ɵzliri iqigǝ qüxüp kǝtti.
Iwo anatchera mapazi anga ukonde ndipo ndinawerama pansi mosautsidwa. Anakumba dzenje mʼnjira yanga koma agweramo okha mʼmenemo.
7 Iradǝm qing, i Huda, iradǝm qing; Mǝn mǝdⱨiyǝ nahxilarni eytip, Bǝrⱨǝⱪ Seni küylǝymǝn!
Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu mtima wanga ndi wokhazikika. Ndidzayimba nyimbo, nyimbo yake yamatamando.
8 Oyƣan, i roⱨim! I nǝƣmǝ-sazlirim, oyƣan! Mǝn sǝⱨǝr ⱪuyaxinimu oyƣitimǝn!
Dzuka moyo wanga! Dzukani zeze ndi pangwe! Ndidzadzuka mʼbandakucha.
9 Mǝn hǝlⱪ-millǝtlǝr arisida seni uluƣlaymǝn, i Rǝb; Əllǝr arisida Seni küylǝymǝn!
Ndidzakutamandani Ambuye, pakati pa mitundu ya anthu, ndidzayimba za Inu pakati pa mayiko.
10 Qünki ɵzgǝrmǝs muⱨǝbbiting ǝrxlǝrgǝ yǝtküdǝk uluƣdur; Ⱨǝⱪiⱪiting bulutlarƣa taⱪaxti.
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kufikira ku mayiko akumwamba; kukhulupirika kwanu kwafika ku mitambo.
11 I Huda, ǝrxlǝrdin yuⱪiri uluƣlanƣaysǝn, Xan-xǝriping yǝr yüzini ⱪapliƣay!
Mukwezekedwe Inu Mulungu kuposa mayiko akumwamba, mulole kuti ulemerero wanu ukhale pa dziko lonse lapansi.