< Zǝbur 112 >
1 Ⱨǝmdusana! Pǝrwǝrdigardin ǝyminidiƣan, Uning ǝmrlirini zor hursǝnlik dǝp bilidiƣan adǝm bǝhtliktur!
Tamandani Yehova. Wodala munthu amene amaopa Yehova, amene amakondwera kwambiri ndi malamulo ake.
2 Uning nǝsli zeminda turup küq-ⱪudrǝtlik bolidu; Duruslarning dǝwri bǝhtlik bolidu.
Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko; mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa.
3 Uning ɵyidǝ dɵlǝt ⱨǝm bayliⱪlar bolidu; Ⱨǝⱪⱪaniyliⱪi mǝnggügǝ turidu.
Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake, ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
4 Ⱪarangƣuluⱪta turƣan durus adǝmgǝ nur pǝyda bolidu; U xǝpⱪǝtlik, rǝⱨimdil ⱨǝm ⱨǝⱪⱪaniydur.
Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima; wokoma mtima, wachifundo ndi wowongoka mtima.
5 Hǝyrhaⱨ, ɵtnǝ berip turidiƣan adǝmning bǝhti bolidu; U ɵz ixlirini adilliⱪ bilǝn yürgüzidu.
Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu, amene amachita ntchito yake mwachilungamo.
6 Bǝrⱨǝⱪ, u ǝbǝdiy tǝwritilmǝydu; Ⱨǝⱪⱪaniy adǝm mǝnggügǝ ǝslinidu.
Ndithu sadzagwedezeka; munthu wolungama sadzayiwalika mpaka muyaya.
7 U xum hǝwǝrdin ⱪorⱪmaydu; Uning kɵngli toⱪ ⱨalda, Pǝrwǝrdigarƣa tayanƣan.
Saopa akamva zoyipa zimene zachitika; mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.
8 Dili mǝⱨkǝm ⱪilinƣan, u ⱪorⱪmaydu; Ahirida u rǝⱪiblirining mǝƣlubiyitini kɵridu.
Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha; potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano.
9 U ɵziningkini mǝrdlǝrqǝ tarⱪatⱪan, Yoⱪsullarƣa beridu; Uning ⱨǝⱪⱪaniyliⱪi mǝnggügǝ turidu; Uning münggüzi izzǝt-xɵⱨrǝt bilǝn kɵtürülidu.
Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka, chilungamo chake chimanka mpaka muyaya; nyanga yake idzakwezedwa mwaulemu.
10 Rǝzil adǝm buni kɵrüp qidimaydu, Qixlirini ƣujurlitidu, u erip ketidu; Rǝzillǝrning arzu-ⱨǝwisi yoⱪitilidu.
Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima; adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka. Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.