< Nǝⱨǝmiya 3 >
1 Xu qaƣda bax kaⱨin Əliyaxib wǝ uning kaⱨin ⱪerindaxliri ⱪopup «Ⱪoy ⱪowuⱪi»ni yengiwaxtin yasap qiⱪti; ular ⱪowuⱪning ⱪanatlirini ornitip, uni [Hudaƣa] atap muⱪǝddǝs dǝp bekitti; ular «Yüzning munari» bilǝn «Ⱨananiyǝlning munari»ƣiqǝ bolƣan ariliⱪtiki sepilni ongxap, uni muⱪǝddǝs dǝp bekitti;
Pambuyo pake Eliyasibu mkulu wa ansembe ndi ansembe anzake anayamba kugwira ntchito ndipo anamanganso Chipata cha Nkhosa. Iwo anachipatulira Mulungu ndipo anayika zitseko zake. Khoma limene analipatula linafika mpaka pa Nsanja ya Zana ndi Nsanja ya Hananeli.
2 Uningƣa tutax ⱪismini Yeriholuⱪlar yasidi; yǝnǝ uningƣa tutax ⱪismini Imrining oƣli Zakkur yasidi.
Anthu a ku Yeriko anamanga chigawo china pambali pake ndipo Zakuri mwana wa Imuri anamanga chigawo chinanso choyandikana nawo.
3 «Beliⱪ ⱪowuⱪi»ni Sǝnaaⱨning oƣulliri yasidi; ular uning lim-kexǝklirini selip, ⱪanatliri, taⱪaⱪliri wǝ baldaⱪlirini ornatti.
Chipata cha Nsomba chinamangidwanso ndi ana a fuko la Hasena. Iwo anayika mitanda yake ndi zitseko, zotsekera zake, ndi mipiringidzo yake.
4 Uningƣa tutax ⱪismini Ⱨakozning nǝwrisi, Uriyaning oƣli Mǝrǝmot yasidi; uningƣa tutax ⱪismini Mǝxǝzabǝlning nǝwrisi, Bǝrǝkiyaning oƣli Mǝxullam yasidi. Uningƣa tutax ⱪismini Baanaⱨning oƣli Zadok yasidi.
Meremoti mwana wa Uriya, mwana wa Hakozi, anakonza chigawo choyandikana nacho. Motsatana naye, Mesulamu mwana wa Berekiya, mwana wa Mesezabeli anakonza chigawo china. Pambali pake, Zadoki mwana wa Baana anakonzanso chigawo china.
5 Uningƣa tutax ⱪismini Tǝkoaliⱪlar yasidi; lekin ularning qongliri ɵz hojisining ixini zimmisigǝ ilixⱪa unimidi.
Pambali pa iwowa anthu a ku Tekowa anakonza chigawo china. Koma wolemekezeka awo anakana kugwira ntchito imene akuluakulu awo anawapatsa.
6 «Kona ⱪowuⱪ»ni Pasiyaning oƣli Yǝⱨoda bilǝn Besodiyaning oƣli Mǝxullam yasidi; ular uning lim-kexǝklirini selip, ⱪanatliri, taⱪaⱪliri wǝ baldaⱪlirini ornatti.
Chipata cha Yesana chinakonzedwa ndi Yoyada mwana wa Paseya ndi Mesulamu mwana wa Besodeya. Iwo anayika mitanda yake ndi kuyika zitseko, zotsekera zake ndi mipiringidzo yake.
7 Ularning yenidiki tutax ⱪismini Gibeonluⱪ Mǝlatiya, Meronotluⱪ Yadon ⱨǝmdǝ Dǝryaning bu ƣǝrbiy tǝripidiki waliylarning baxⱪuruxi astidiki Gibeonluⱪlar bilǝn Mizpaⱨliⱪlar yasidi.
Pambali pawo Melatiya Mgibeyoni ndi Yadoni Mmerenoti ndiponso anthu a ku Gibiyoni ndi a ku Mizipa anakonza chigawo chawo mpaka ku nyumba ya bwanamkubwa wa chigawo cha Patsidya pa Yufurate.
8 Ularning yenidiki tutax ⱪismini zǝrgǝrlǝrdin bolƣan Harⱨayaning oƣli Uzziyǝl yasidi. Uningƣa tutax ⱪismini huxbuy buyum yasaydiƣan ǝtirqilǝrdin Ⱨananiya yasidi. Ular Yerusalem [sepilini] taki «Ⱪelin tam»ƣiqǝ ongxap yasidi.
Pambali pawo Uzieli mwana wa Harihaya wa mʼgulu amisiri osula golide anakonzanso chigawo china. Pambali pake Hananiya mmodzi mwa anthu oyenga mafuta onunkhira, anakonzanso chigawo china. Iwo anakonzanso Yerusalemu mpaka ku Khoma Lotambasuka.
9 Ularning yenidiki tutax ⱪismini Yerusalemning yerimining ⱨakimi bolƣan Hurning oƣli Refaya yasidi.
Refaya mwana wa Huri wolamulira theka la chigawo cha Yerusalemu anakonza chigawo china motsatana nawo.
10 Ularning yenida, Harumafning oƣli Yǝdaya ɵzining ɵyining udulidiki ⱪismini yasidi. Ularning yenidiki ⱪismini Haxabniyaning oƣli Ⱨattux yasidi.
Kulumikiza ichi, Yedaya mwana wa Harumafi anakonza chigawo choyangʼanana ndi nyumba yake, ndipo Hatusi mwana wa Hasabaneya anakonzanso motsatana naye.
11 Ⱨarimning oƣli Malkiya bilǝn Paⱨat-Moabning oƣli Ⱨaxxub sepilning baxⱪa bir bɵliki bilǝn «Humdanlar munari»ni yasidi.
Malikiya mwana wa Harimu ndi Hasubu mwana wa Pahati-Mowabu anakonzanso chigawo china ndiponso Nsanja ya Ngʼanjo.
12 Ularning yenidiki tutax ⱪismini Yerusalemning yerimining ⱨakimi Halloⱨǝxning oƣli Xallom ɵzi wǝ uning ⱪizliri yasidi.
Salumu mwana wa Halohesi wolamulira theka la chigawo cha Yerusalemu, anakonzanso chigawo chotsatana nawo mothandizidwa ndi ana ake akazi.
13 «Jilƣa ⱪowuⱪi»ni Ⱨanun bilǝn Zanoaⱨ xǝⱨirining aⱨalisi yasidi. Ular uni yasap, uning ⱪanatliri, taⱪaⱪliri wǝ baldaⱪlirini ornatti wǝ yǝnǝ «Tezǝk ⱪowuⱪi»ƣiqǝ ming gǝz sepilnimu yasidi.
Chipata cha ku chigwa chinakonzedwa ndi Hanuni ndi anthu okhala ku Zanowa. Iwo anachimanganso ndi kuyika zitseko zake ndi zotsekera ndi mipiringidzo yake. Iwo anakonzanso khoma lotalika mamita 450 mpaka ku Chipata cha Zinyalala.
14 «Tezǝk ⱪowuⱪi»ni Bǝyt-Ⱨakkǝrǝm yurtining baxliⱪi Rǝkabning oƣli Malkiya yasidi; ular uni yasap, uning ⱪanatliri, taⱪaⱪliri wǝ baldaⱪlirini ornatti.
Chipata cha Zinyalala chinakonzedwa ndi Malikiya mwana wa Rekabu, wolamulira chigawo cha Beti-Hakeremu. Iye anachimanganso ndi kuyika zitseko zake, zotsekera zake ndi mipiringidzo.
15 «Bulaⱪ ⱪowuⱪi»ni Mizpaⱨ yurtining baxliⱪi Kol-Ⱨozǝⱨning oƣli Xallum yasidi. U uni yasap, ɵgzisini yepip, uning ⱪanatliri, taⱪaⱪliri wǝ baldaⱪlirini ornatti wǝ yǝnǝ xaⱨanǝ baƣning yenidiki Siloam kɵlining sepilini «Dawutning xǝⱨiri»din qüxidiƣan pǝlǝmpǝygiqǝ yengiwaxtin yasidi.
Chipata cha Kasupe chinakonzedwa ndi Saluni mwana wa Koli-Hoze, wolamulira chigawo cha Mizipa. Iye anachimanganso ndi kuyikanso denga ndiponso zitseko, zotsekera ndi mipiringidzo yake. Iye anakonzanso khoma la Dziwe la Siloamu limene lili pafupi ndi munda wa mfumu mpaka ku makwerero otsikira potuluka mzinda wa Davide.
16 Uningdin keyinki tutax ⱪismini Dawutning ⱪǝbrilirining udulidiki wǝ uningdin keyinki sün’iy kɵlgǝ ⱨǝm uning kǝynidiki «Palwanlarning ɵyi»gǝ ⱪǝdǝr Bǝyt-Zur yurtining yerimining ⱨakimi, Azbukning oƣli Nǝⱨǝmiya yasidi.
Pambali pa iyeyo, Nehemiya mwana wa Azibuki, wolamulira theka la chigawo cha Beti Zuri anakonza chigawo china mpaka kumalo oyangʼanana ndi manda a Davide, mpaka ku dziwe lokumba ndi ku nyumba ya anthu ankhondo.
17 Uningdin keyinki tutax ⱪismini Lawiylar — Yǝni Banining oƣli Rǝⱨum yasidi, uning yenidiki tutax ⱪismini Keilaⱨning yerim yurtining ⱨakimi Ⱨaxabiya ɵz yurtiƣa wakalitǝn yasap qiⱪti.
Pambali pake Alevi anakonza chigawo china, ndipo mtsogoleri wawo anali Rehumi mwana wa Bani. Pambali pa iye Hasabiya wolamulira theka la chigawo cha Keyila anagwira ntchito ku chigawo chake.
18 Uning yenidiki tutax ⱪismini ularning ⱪerindaxliri — Keilaⱨning ikkinqi yerimining ⱨakimi, Ⱨenadadning oƣli Baway yasidi.
Pambuyo pa iyeyu abale awo anapitiriza kukonza, ndipo mtsogoleri wawo anali Bawai mwana wa Henadadi, wolamulira theka lina la chigawo cha Keyila.
19 Uning yenida, Mizpaⱨning ⱨakimi Yǝxuyaning oƣli Ezǝr ⱪoral-yaraƣ ambiriƣa qiⱪix yolining udulida, sepilning doⱪmuxidiki yǝnǝ bir bɵlikini yasidi.
Motsatana naye Ezeri mwana wa Yesuwa, wolamulira Mizipa anakonza chigawo chinanso choyangʼanana ndi chikweza chofikira ku nyumba yosungira zida za nkhondo pa ngodya.
20 Zabbayning oƣli Baruⱪ uningdin keyinki yǝnǝ bir bɵlikini, yǝni sepilning doⱪmuxidin taki bax kaⱨin Əliyaxibning ɵyining dǝrwazisiƣiqǝ bolƣan bɵlikini kɵngül ⱪoyup yasidi.
Motsatana naye, Baruki mwana wa Zakai anakonzanso chigawo china kuchokera pa ngodya mpaka pa chitseko cha nyumba ya Eliyasibu mkulu wa ansembe.
21 Uning yenida Ⱨakozning nǝwrisi, Uriyaning oƣli Mǝrǝmot sepilning Əliyaxibning ɵyining dǝrwazisidin taki Əliyaxibning ⱨoylisining ahiriƣiqǝ bolƣan yǝnǝ bir bɵlikini yasidi.
Motsatana naye, Meremoti mwana wa Uriya, mwana wa Hakozi anakonzanso chigawo china kuchokera ku chitseko cha nyumba ya Eliyasibu mpaka kumapeto kwake.
22 Bulardin keyinki bir ⱪismini Iordan tüzlǝnglikidikilǝr, kaⱨinlar yasidi.
Pambuyo pake ansembe okhala ku chidikha anakonzanso chigawo china.
23 Bularning yenida, Binyamin bilǝn Ⱨaxxub ɵz ɵyining udulidiki bɵlikini yasidi. Ulardin keyin Ananiyaning nǝwrisi, Maaseyaⱨning oƣli Azariya ɵz ɵyining yenidiki ⱪisimni yasidi.
Pambuyo pawo, Benjamini ndi Hasubu anakonza kutsogolo kwa nyumba zawo. Ndipo motsatana nawo, Azariya mwana wa Maaseya mwana wa Ananiya, anakonza chigawo choyangʼanana ndi nyumba zawo.
24 Uning yenida, Azariyaning ɵyidin taki sepilning doⱪmuxiƣiqǝ bolƣan yǝnǝ bir bɵlikini Ⱨenadadning oƣli Binnuiy yasidi.
Motsatana naye, Binuyi mwana wa Henadadi anakonzanso chigawo china, kuchokera pa nyumba ya Azariya kukafika potsirizira pa ngodya.
25 [Uning yenida], Uzayning oƣli Palal padixaⱨ ordisining doⱪmuxi, xuningdǝk ordidiki qoⱪqiyip turƣan, zindan ⱨoylisining yenidiki egiz munarning udulidiki bɵlikini yasidi. Uningdin keyinki bir bɵlikini Paroxning oƣli Pidaya yasidi.
Palali mwana Uzai anakonza chigawo china choyangʼanana ndi ngodya ndi nsanja yotuluka pa nyumba yapamwamba ya mfumu ku bwalo la alonda. Motsatana naye, Pedaya mwana wa Parosi,
26 Əmdi Ofǝldǝ turidiƣan ibadǝthana hizmǝtkarliri künqiⱪix tǝrǝptiki «Su ⱪowuⱪi»ning udulidiki wǝ qoⱪqiyip turƣan munarning udulidiki sepilni yasidi.
ndi otumikira mʼNyumba ya Mulungu amene amakhala pa khoma la Ofeli anakonza chigawo china mpaka pa malo oyangʼanana ndi Chipata cha Madzi kuloza kummawa ndiponso nsanja yayitali ija.
27 Qoⱪqiyip turƣan qong munarning udulida Tǝkoaliⱪlar taki Ofǝl sepiliƣiqǝ bolƣan ikkinqi bir bɵlikini yasidi.
Motsatana nawo, anthu a ku Tekowa anakonzanso chigawo china choyangʼanana ndi nsanja ija yayikulu ndi yayitali mpaka ku khoma la Ofeli.
28 «At ⱪowuⱪi»ning yuⱪiri bir bɵlikini kaⱨinlar ⱨǝrbiri ɵz ɵyining udulidiki ⱪismini yasidi.
Kuyambira ku Chipata cha Akavalo anakonza ndi ansembe ena ndipo aliyense amakonza khoma loyangʼanana ndi nyumba yake.
29 Immǝrning oƣli Zadok ularning yenida, keyinki ⱪismini, ɵz ɵyining udulidiki bir bɵlikini yasidi. Uning yenidiki tutax ⱪismini «xǝrⱪiy dǝrwaza»ning dǝrwaziwǝni Xekaniyaning oƣli Xemaya yasidi.
Motsatana nawo, Zadoki mwana wa Imeri anakonza chigawo china choyangʼanana ndi nyumba yake. Motsatana naye, Semeya mwana wa Sekaniya, mlonda wa Chipata cha Kummawa, anakonzanso khoma.
30 Uning yenida, Xǝlǝmiyaning oƣli Ⱨananiya bilǝn Zalafning altinqi oƣli Ⱨanun ikkinqi bir bɵlikini yasidi; ularning yenida, Bǝrǝkiyaning oƣli Mǝxullam ɵz ⱪorusining udulidiki bir bɵlǝkni yasidi.
Hananiya mwana wa Selemiya ndiponso Hanuni mwana wachisanu ndi chimodzi wa Zalafi anakonza chigawo china. Motsatana naye, Mesulamu mwana wa Berekiya anakonza chigawo choyangʼanana ndi chipinda chake.
31 Uning yenida, xu yǝrdin tartip ibadǝthana hizmǝtkarliri bilǝn sodigǝrlǝrning ⱪoruliridin ɵtüp, «Tǝkxürüx ⱪowuⱪi»ning udulidiki sepil doⱪmuxining balihanisiƣiqǝ bolƣan bɵlikini zǝrgǝrlǝrdin bolƣan Malkiya yasidi.
Motsatana naye, Malikiya mmodzi mwa amisiri a golide anakonza chigawo china mpaka ku nyumba ya atumiki a ku Nyumba ya Mulungu ndiponso ku nyumba ya anthu amalonda moyangʼanana ndi chipata cha Mifikade ndiponso mpaka pa chipinda chapamwamba chapangodya.
32 Doⱪmuxning balihanisi bilǝn «Ⱪoy ⱪowuⱪi»ning ariliⱪidiki bɵlǝkni zǝrgǝrlǝr bilǝn sodigǝrlǝr yasidi.
Ndipo pakati pa chipinda chapamwamba chapangodya ndi Chipata cha Nkhosa anakonza ndi amisiri a golide ndi anthu amalonda.