< Zebur 104 >
1 Perwerdigargha teshekkür-medhiye qaytur, i jénim! I Perwerdigar Xudayim, intayin ulughsen; Shanu-shewket we heywet bilen kiyin’gensen;
Tamanda Yehova, iwe moyo wanga. Inu Yehova Mulungu wanga, ndinu wamkulu kwambiri; mwavala ulemerero ndi ufumu.
2 Libas bilen pürken’gendek yoruqluqqa pürken’gensen, Asmanlarni chédir perdisi kebi yayghansen.
Iye wadzifunditsa kuwala ngati chovala; watambasula miyamba ngati tenti
3 U yuqiriqi rawaqlirining limlirini sulargha ornatqan, Bulutlarni jeng harwisi qilip, Shamal qanatliri üstide mangidu;
ndipo wayika pa madzi mitanda ya chipinda chake. Iye amasandutsa mitambo kukhala galeta lake, ndi kuwuluka pa mapiko a mphepo.
4 U perishtilirini shamallar, Xizmetkarlirini ot yalquni qilidu.
Amapanga mphepo kukhala amithenga ake, malawi amoto kukhala atumiki ake.
5 Yerni U ulliri üstige ornatqan; U esla tewrinip ketmeydu.
Anakhazikitsa dziko lapansi pa maziko ake; silingasunthike.
6 Libas bilen oralghandek, uni chongqur déngizlar bilen orighansen, Sular taghlar choqqiliri üstide turdi.
Munaliphimba ndi nyanja yozama ngati chovala; madzi anayimirira pamwamba pa mapiri.
7 Séning tenbihing bilen sular beder qachti, Güldürmamangning sadasidin ular tézdin yandi;
Koma pakudzudzula kwanu madzi anathawa, pa mkokomo wa bingu lanu iwo anamwazika;
8 Taghlar örlep chiqti, Wadilar chüshüp ketti, [Sular] Sen békitken jaygha chüshüp ketti.
Inu munamiza mapiri, iwo anatsikira ku zigwa kumalo kumene munawakonzera.
9 Ular téship, yerni yene qaplimisun dep, Sen ulargha cheklime qoyghansen.
Inu munayika malire ndipo sangathe kudutsa, iwo sadzamizanso dziko lapansi.
10 [Tengri] wadilarda bulaqlarni échip urghutidu, Suliri taghlar arisida aqidu.
Iye achititsa akasupe kutulutsa madzi kupita ku zigwa; madziwo amayenda pakati pa mapiri.
11 Daladiki herbir janiwargha ussuluq béridu, Yawayi éshekler ussuzluqini qanduridu.
Iwo amapereka madzi kwa zirombo zonse zakuthengo; abulu akuthengo amapha ludzu lawo.
12 Köktiki qushlar ularning boyida qonidu, Derex shaxliri arisida sayraydu.
Mbalame zamlengalenga zimayika zisa mʼmbali mwa madzi; zimayimba pakati pa thambo.
13 U yuqiridiki rawaqliridin taghlarni sughiridu; Yer Séning yasighanliringning méwiliridin qandurulidu!
Iye amathirira mapiri kuchokera ku zipinda zake zapamwamba; dziko lapansi limakhutitsidwa ndi chipatso cha ntchito yake.
14 U mallar üchün ot-chöplerni, Insanlar üchün köktatlarni östüridu, Shundaqla nanni yerdin chiqiridu;
Amameretsa udzu kuti ngʼombe zidye, ndi zomera, kuti munthu azilima kubweretsa chakudya kuchokera mʼdziko lapansi:
15 Ademning könglini xush qilidighan sharabni, Insan yüzini parqiritidighan mayni chiqiridu; Insanning yürikige nan bilen quwwet béridu;
vinyo amene amasangalatsa mtima wa munthu, mafuta amene amachititsa nkhope yake kuwala, ndi buledi amene amapereka mphamvu.
16 Perwerdigarning derexliri, Yeni Özi tikken Liwan kédir derexliri [su ichip] qanaetlinidu.
Mitengo ya Yehova ndi yothiriridwa bwino, mikungudza ya ku Lebanoni imene Iye anadzala.
17 Ene ashular arisigha qushlar uwa yasaydu, Leylek bolsa, archa derexlirini makan qilidu.
Mbalame zimamanga zisa zawo; kakowa ali ndi malo ake mʼmikungudzamo.
18 Égiz choqqilar tagh öchkilirining, Tik yarlar sughurlarning panahi bolidu.
Mapiri ataliatali ndi a mbalale; mʼmingʼalu ya miyala ndi mobisalamo mbira.
19 Pesillerni békitmek üchün U ayni yaratti, Quyash bolsa pétishini bilidu.
Mwezi umasiyanitsa nyengo ndipo dzuwa limadziwa nthawi yake yolowera.
20 Sen qarangghuluq chüshürisen, tün bolidu; Ormandiki janiwarlarning hemmisi uningda shipir-shipir kézip yüridu.
Inu mumabweretsa mdima nukhala usiku, ndipo zirombo zonse za ku nkhalango zimatuluka.
21 Arslanlar olja izdep hörkireydu, Tengridin ozuq-tülük sorishidu;
Mikango imabangula kufuna nyama, ndi kufunafuna chakudya chawo kuchokera kwa Mulungu.
22 Quyash chiqipla, ular chékinidu, Qaytip kirip uwilirida yatidu.
Dzuwa limatuluka ndipo iyo imapita kukabisala; imabwerera kukagona pansi mʼmapanga awo.
23 Insan bolsa öz ishigha chiqidu, Ta kechkiche méhnette bolidu.
Pamenepo munthu amapita ku ntchito yake, kukagwira ntchito yake mpaka madzulo.
24 I Perwerdigar, yasighan herxil nersiliring neqeder köptur! Hemmisini hékmet bilen yaratqansen, Yer yüzi ijat-bayliqliring bilen toldi.
Ntchito zanu ndi zochulukadi Inu Yehova! Munazipanga zonse mwanzeru, dziko lapansi ladzaza ndi zolengedwa zanu.
25 Ene büyük bipayan déngiz turidu! Uningda san-sanaqsiz ghuzh-ghuzh janiwarlar, Chong we kichik haywanlar bar.
Kuli nyanja yayikulu ndi yotambalala, yodzaza ndi zolengedwa zosawerengeka, zamoyo zanu zazikulu ndi zazingʼono zomwe.
26 Shu yerde kémiler qatnaydu, Uningda oynaqlisun dep sen yasighan léwiatanmu bar;
Kumeneko sitima zapamadzi zimayenda uku ndi uku, ndiponso Leviyatani amene munamulenga kuti asewere kumeneko.
27 Waqtida ozuq-tülük bergin dep, Bularning hemmisi Sanga qaraydu.
Zonsezi zimayangʼana kwa Inu kuti muzipatse chakudya chawo pa nthawi yake yoyenera.
28 Ulargha berginingde, tériwalidu, Qolungni achqiningdila, ular nazunémetlerge toyidu.
Mukazipatsa, zimachisonkhanitsa pamodzi; mukatsekula dzanja lanu, izo zimakhutitsidwa ndi zinthu zabwino.
29 Yüzüngni yoshursang, ular dekke-dükkige chüshidu, Rohlirini alsang, ular jan üzüp, Yene tupraqqa qaytidu.
Mukabisa nkhope yanu, izo zimachita mantha aakulu; mukachotsa mpweya wawo, zimafa ndi kubwerera ku fumbi.
30 Rohingni ewetkiningde, ular yaritilidu, Yer-yüzi yéngi [bir dewr bilen] almishidu.
Mukatumiza mzimu wanu, izo zimalengedwa ndipo mumakozanso maonekedwe a dziko lapansi.
31 Perwerdigarning shan-shöhriti ebediydur, Perwerdigar Öz yaratqanliridin xursen bolidu.
Ulemerero wa Yehova ukhalebe mpaka muyaya; Yehova akondwere ndi ntchito ya manja ake;
32 U yerge baqqinida, yer titreydu, Taghlargha tegkinide, ular tütün chiqiridu.
Iye amene amayangʼana dziko lapansi ndipo limanjenjemera, amene amakhudza mapiri ndipo amatuluka utsi.
33 Hayatla bolidikenmen, Perwerdigargha naxsha éytimen; Wujudum bolsila Xudayimni küyleymen.
Ine ndidzayimbira Yehova moyo wanga wonse; ndidzayimbira matamando Mulungu wanga nthawi yonse imene ndili ndi moyo.
34 U sürgen oy-xiyallirimdin söyünse! Perwerdigarda xushallinimen!
Zolingalira zanga zikhale zomukomera Iye, pamene ndikusangalala mwa Yehova.
35 Gunahkarlar yer yüzidin tügitilidu, Reziller yoq bolidu. I jénim, Perwerdigargha teshekkür-medhiye qaytur! Hemdusana!
Koma anthu ochimwa awonongeke pa dziko lapansi ndipo anthu oyipa asapezekenso. Tamanda Yehova, Iwe moyo wanga. Tamandani Yehova.