< Псалми 87 >

1 Синів Коре́євих. Псалом, Пісня.
Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2 Госпо́дь любить брами Сіону понад усі се́лища Яковові.
Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
3 Славне розповіда́ють про тебе, місто Боже! (Се́ла)
Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
4 „Тим, хто знає мене, нагадаю про Ра́гав та про Вавило́н; ось Филисте́я та Тир з Ку́шем кажуть: Отой народився був там“.
“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
5 І про Сіон говори́тимуть: „Той і той народився був у ньому, й Сам Всевишній зміцняє його́“!
Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
6 Господь буде лічити у книзі наро́дів: „Оцей народився був там“! (Се́ла)
Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
7 І співають, і грають вони: „У Тобі — всі джере́ла мої!“
Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”

< Псалми 87 >