< Псалми 75 >
1 Для дириґента хору. „Не вигуби!“Псалом Аса́фів. Пісня. Прославляємо, Боже, Тебе, прославляєм, бо близьке́ Твоє Ймення! Оповідають про чу́да Твої.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Salimo la Asafu. Nyimbo. Tikuthokoza Inu Mulungu, tikuthokoza, pakuti dzina lanu lili pafupi nafe, anthutu amafotokoza za ntchito zanu zodabwitsa.
2 „Коли при́йде година озна́чена, то Я буду суди́ти справедливо.
Mumati, “Ine ndimayika nthawi yoyenera, ndine amene ndimaweruza mwachilungamo.
3 Розтопи́лась земля, і всі її ме́шканці, та стовпи́ її змі́цнюю Я. (Се́ла)
Pamene dziko lapansi ndi anthu ake onse anjenjemera, ndine amene ndimagwiriziza mizati yake molimba. (Sela)
4 Я сказав до лихих: Не шалійте, а безбожним: Не підіймайте ви ро́га!
Kwa odzitama ndikuti, ‘Musadzitamenso,’ ndipo kwa oyipa, ‘Musatukulenso nyanga zanu.
5 Не підійма́йте ви рога свого́ догори́, не говоріть твердоши́йно,
Musatukule nyanga zanu motsutsana ndi kumwamba; musayankhule ndi khosi losololoka.’”
6 бо не від сходу, і не від за́ходу, і не від пусти́ні наді́йде пови́щення,
Kugamula milandu sikuchokera kummawa kapena kumadzulo kapena ku chipululu.
7 але́ судить Бог: того Він пони́жує, а того повищує, —
Koma ndi Mulungu amene amaweruza: Iyeyo amatsitsa wina, nakwezanso wina.
8 бо чаша в Господній руці, а шумли́ве вино повне мі́шаного, — і наливає Він з нього, усі ж безза́конні землі виссуть та вип'ють лиш дрі́жджі її!
Mʼdzanja la Yehova muli chikho chodzaza ndi vinyo wochita thovu, wosakanizidwa ndi zokometsera; Iye amamutsanulira pansi ndipo onse oyipa a dziko lapansi amamwa ndi senga zake zonse.
9 А я буду звіща́ти навіки, співатиму Богові Якова,
Kunena za ine, ndidzalengeza izi kwamuyaya; ndidzayimba matamando kwa Mulungu wa Yakobo.
10 відрубаю всі ро́ги безбожних, — роги праведного піднесу́ться!
Ndidzadula nyanga za onse oyipa koma nyanga za olungama zidzakwezedwa.