< Nnwom Mu Dwom 6 >

1 Ɛhe na wo dɔfo no kɔ mmea ahoɔfɛfo mu ahoɔfɛ? Ɛhe na wo dɔfo man fae, na yɛne wo nkɔhwehwɛ no?
Iwe wokongola kuposa akazi onsewa, kodi wokondedwa wakoyo wapita kuti? Kodi wokondedwa wakoyo wakhotera njira iti kuti timufunefune pamodzi ndi iwe?
2 Me dɔfo kɔ ne turo mu, faako a woduadua nnua ahorow, okokyinkyin turo no mu akɔboaboa sukooko ano.
Wachikondi wanga watsikira ku munda kwake, ku timinda ta zokometsera zakudya, akukadyetsa ziweto zake ku minda, ndiponso akuthyola maluwa okongola.
3 Me dɔfo yɛ me de, na me nso meyɛ ne de; okyinkyin sukooko no mu.
Wokondedwa wangayo ndine wake ndipo iyeyo ndi wangawanga; amadyetsa ziweto zake pakati pa maluwa okongola.
4 Me dɔfo, wo ho yɛ fɛ te sɛ Tirsa, wʼahoɔfɛ te sɛ Yerusalem, wusi pi te sɛ asraafo a wɔretu frankaa.
Ndiwe wokongola, bwenzi langa, ngati Tiriza, wokongola kwambiri ngati Yerusalemu, ndiwe woopsa ngati gulu lankhondo lonyamula mbendera.
5 Nhwɛ me saa; wobunkam me so. Wo ti nwi te sɛ mpapokuw a wɔresian afi Gilead.
Usandipenyetsetse; pakuti maso ako amanditenga mtima. Tsitsi lako lili ngati gulu la mbuzi zikutsetsereka kuchokera ku Giliyadi.
6 Wo se te sɛ nguankuw a wɔatwitwa wɔn ho nwi foforo, a wofi aguaree. Baako mpo nyeraa ɛ.
Mano ako ali ngati gulu la nkhosa zimene zikubwera kuchokera kokazisambitsa, iliyonse ili ndi ana amapasa, palibe imene ili yokha.
7 Wʼasontɔre a ɛhyɛ wo nkataanim mu te sɛ ntunkum aduaba fa.
Kukhalira kumbuyo kwa nsalu yako yophimba kumutu, masaya ako ali ngati mabandu a makangadza.
8 Ebia na ɔyerenom yɛ aduosia, mpenanom bɛyɛ aduɔwɔtwe, ne mmabaa dodow a wontumi nkan wɔn;
Ngakhale patakhala akazi a mfumu 60, ndi azikazi 80, ndi anamwali osawerengeka;
9 nanso mʼaborɔnoma a ne ho nni asɛm yɛ sononko; ɔno nko ara ne ne na babea, ɔno na nea ɔwoo no no pɛ nʼasɛm. Mmabaa huu no no, wɔfrɛɛ no nhyira; ahemmea ne mpenanom kamfoo no.
koma nkhunda yanga, wangwiro wanga ndi wosiyana ndi wina aliyense; mwana wamkazi yekhayo wa amayi ake, mwana wapamtima wa amene anamubereka. Anamwali anamuona ndipo anamutcha wodala; akazi a mfumu ndi azikazi anamutamanda.
10 Hena na wapue sɛ ahemadakye yi, ɔyɛ frɔmfrɔm sɛ ɔsram, na ɔhyerɛn sɛ owia, nʼanuonyam te sɛ nsoromma a wɔsa so.
Ndani uyu akuoneka ngati mʼbandakucha, wokongola ngati mwezi, wowala ngati dzuwa, wochititsa mantha ngati gulu la ankhondo mbendera zili mʼmanja?
11 Misian kɔɔ nnuaba pɔw mu hɔ sɛ merekɔhwehwɛ afifide foforo a ɛwɔ obon no mu, sɛ bobe no agu nhwiren, anaasɛ ntunkum no ayɛ frɔmfrɔm.
Ndinatsikira ku munda wa mitengo ya alimondi kukayangʼana zomera zatsopano ku chigwa, kukaona ngati mpesa waphukira kapena ngati makangadza ali ndi maluwa.
12 Mʼani baa me ho so no na mʼadwene de me abesi me nkurɔfo adehye nteaseɛnam so.
Ndisanazindikire kanthu, ndinakhala ngati ndikulota kuti ndili mʼgaleta pambali pa mfumu yanga.
13 San wʼakyi, san wʼakyi, Sulamit babea; San bra, san bra ma yɛnhwɛ wo! Aberante: Adɛn nti na ɛsɛ sɛ mohwɛ Sulamit abeawa sɛnea mohwɛ Mahanaim asaw no?
Bwerera, bwerera iwe namwali wa ku Sulami; bwerera, bwerera kuti ife tidzakupenyetsetse iwe! Mwamuna Chifukwa chiyani mukufuna kudzapenyetsetsa ine mwana wamkazi wa ku Sulami, pamene ndikuvina pakati pa magulu awiri?

< Nnwom Mu Dwom 6 >