< Mmebusɛm 7 >

1 Me ba, fa me nsɛm sie na kora mʼahyɛde wɔ wo mu.
Mwana wanga, mvera mawu anga; usunge bwino malamulo angawa.
2 Di mʼahyɛde so na wubenya nkwa; bɔ me nkyerɛkyerɛ ho ban sɛ nea wodɔ no.
Utsate malamulo anga ndipo udzakhala ndi moyo; samala malangizo angawa monga uchitira ndi maso ako.
3 Kyekyere bɔ wo nsateaa ho; kyerɛw no yiye gu wo koma pon so.
Uchite ngati wawamangirira pa zala zako, ndiponso ngati kuti wawalemba pa mtima pako.
4 Ka kyerɛ nyansa se, “Woyɛ me nuabea,” na frɛ ntease wo busuani;
Nzeru uyiwuze kuti, “Iwe ndiwe mlongo wanga,” ndipo khalidwe lomvetsa bwino zinthu ulitchule kuti, “Bwenzi langa lapamtima.”
5 Wɔbɛtwe wo afi ɔbeawaresɛefo ho, afi ɔbeawarefo huhuni nsɛmmɔdɛ ho.
Zidzakuteteza kwa mkazi wachigololo ndiponso zidzakuthandiza kusamvera mawu oshashalika a mkazi wachilendo.
6 Me fi mfɛnsere ano, mede mʼani faa mfɛnsere mu.
Tsiku lina pa zenera la nyumba yanga ndinasuzumira pa zenera.
7 Mihuu wɔ ntetekwaafo mu, mehyɛɛ mmerante no mu baako nsow, ɔbabun a onni adwene.
Ndinaona pakati pa anthu opusa, pakati pa anyamata, mnyamata wina wopanda nzeru.
8 Na ɔnam borɔn a ɛbɛn ɔbea no fi so a nʼani kyerɛ ɔbea no fi
Iye ankayenda njira yodutsa pafupi ndi nyumba ya mkaziyo, kuyenda molunjika nyumba ya mkaziyo.
9 bere a onwini redwo, na anim rebiribiri no.
Inali nthawi yachisisira madzulo, nthawi ya usiku, kuli mdima.
10 Afei ɔbea bi fi behyiaa no a wasiesie ne ho sɛ oguamanfo a nnaadaa wɔ ne koma mu.
Ndipo mkaziyo anadzakumana naye, atavala ngati munthu wachiwerewere wa mtima wonyenga.
11 (Ɔyɛ hyirenn na hwee mfa ne ho, ɔntena fie koraa;
(Mkaziyo ndi wolongolola ndiponso nkhutukumve, iye ndi wosakhazikika pa khomo.
12 nnɛ wohu no mmɔnten so, ɔkyena na ɔte aguabɔbea, ɔtetɛw wɔ mmantwea mmantwea.)
Mwina umupeza pa msewu, mwina umupeza pa msika, ndipo amadikirira munthu pa mphambano iliyonse).
13 Osoo ne mu few nʼano, wamfɛre, na ɔkae se,
Tsono amagwira mnyamatayo ndi kupsompsona ndi nkhope yake yopanda manyazi amamuwuza kuti,
14 “Mewɔ asomdwoe afɔrebɔde wɔ fie; nnɛ madi me bɔhyɛ so.
“Ndinayenera kupereka nsembe zachiyanjano. Lero ndakwaniritsa malumbiro anga.
15 Enti mebae sɛ merebehyia wo; mehwehwɛɛ wo na mahu wo!
Choncho ndinabwera kudzakumana nawe; ndinkakufunafuna ndipo ndakupeza!
16 Mato me mpa, mede nwera a wɔahyɛ no aduru a efi Misraim.
Pa bedi panga ndayalapo nsalu zosalala zokongola zochokera ku Igupto.
17 Mede nnuhuam apete me mpa so: kurobow, pɛprɛ ne dupapo.
Pa bedi panga ndawazapo zonunkhira za mure, mafuta onunkhira a aloe ndi sinamoni.
18 Bra, ma yɛmfa ɔdɔ mmɔ ɔdɔ mu nkosi anɔpa;
Bwera, tiye tikhale malo amodzi kukondwerera chikondi mpaka mmawa; tiye tisangalatsane mwachikondi!
19 Me kunu nni fie; watu kwan na ɔbɛkyɛ.
Mwamuna wanga kulibe ku nyumbako; wapita ulendo wautali:
20 Ɔde sika a ɛdɔɔso hyɛɛ ne sika kotoku ma na ɔremma kosi ɔsram no kurokumatwa bere mu.”
Anatenga thumba la ndalama ndipo adzabwera ku nyumba mwezi ukakhwima.”
21 Ɔde tɛkrɛmakyene bɔɔ no adafa; ɔde nnaadaa nyaa no ne no dae.
Ndi mawu ake onyengerera amamukakamiza mnyamatayo; amukopa ndi mawu ake oshashalika.
22 Odii nʼakyi prɛko pɛ te sɛ nantwi a ɔrekɔ akumii, anaa ɔwansan a ɔde ne ti rekɔhyɛ hankare fi mu
Nthawi yomweyo chitsiru chimamutsatira mkaziyo ngati ngʼombe yopita kukaphedwa, monga momwe mbawala ikodwera mu msampha,
23 kosi sɛ bɛmma bɛwɔ ne brɛbo mu, te sɛ anomaa a ɔrekɔtɔ anomaa afiri mu na onnim sɛ ɔbɛhwere ne nkwa.
mpaka muvi utalasa chiwindi chake, chimakhala ngati mbalame yothamangira mʼkhwekhwe, osadziwa kuti moyo wake uwonongeka.
24 Na afei, me mma, muntie me; monyɛ aso mma nea meka.
Tsono ana inu, ndimvereni; mvetsetsani zimene ndikunena.
25 Mommma mo koma mpatiri nkɔ no so na momman mmfa nʼakwan so.
Musatengeke mtima ndi njira za mkazi ameneyu; musasochere potsata njira zake.
26 Bebree na wɔnam no so ahwehwe ase; wɔn a wakum wɔn dɔɔso pa ara.
Paja iye anagwetsa anthu ambiri; wapha gulu lalikulu la anthu.
27 Ne fi yɛ ɔda tempɔn a ɛkɔ owu pia mu. (Sheol h7585)
Nyumba yake ndi njira yopita ku manda, yotsikira ku malo a anthu akufa. (Sheol h7585)

< Mmebusɛm 7 >