< Hiob 17 >

1 Me honhom atɔ beraw, me nna so atwa, na ɔda retwɛn me.
“Mtima wanga wasweka, masiku anga atha, manda akundidikira.
2 Ampa ara fɛwdifo atwa me ho ahyia; ɛsɛ sɛ mehwɛ wɔn atutuwpɛ.
Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira; maso anga akupenyetsetsa mdani wanga.
3 “Ao Onyankopɔn, hyɛ me bɔ a wuhia. Hena bio na ɔbɛma me bammɔ?
“Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna. Ndani wina amene adzandiperekera ine chikole?
4 Wɔato wɔn adwene mu a wɔnte asɛm ase; enti woremma wonni nkonim.
Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu; choncho simudzawalola kuti apambane.
5 Sɛ obi sopa ne nnamfonom de gye akatua a, ɛbɛhwere ne mma aniwa.
Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma, ana ake sadzaona mwayi.
6 “Onyankopɔn de me ayɛ asɛm a ɛda obiara ano, obi a wɔte ntasu gu nʼani so.
“Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense, munthu amene anthu amalavulira malovu nkhope yake.
7 Awerɛhow ama mʼani ayɛ siamoo me nipadua nyinaa yɛ sunsuma.
Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni; ndawonda ndi mutu womwe.
8 Ɛyɛ atreneefo nwonwa; wɔn a wodi bem tia wɔn a wonni nyamesu.
Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi; anthu osachimwa akupsera mtima anthu osapembedza Mulungu.
9 Nanso atreneefo bɛkɔ wɔn anim, na wɔn a wɔn nsa ho tew no bɛkɔ so anya ahoɔden.
Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo, ndipo anthu a makhalidwe abwino mphamvu zawo zidzanka zikuchuluka.
10 “Mo nyinaa monsan mmra mmɛsɔ nhwɛ! Na merennya onyansafo wɔ mo mu.
“Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo, sindidzapezapo munthu wanzeru pakati panupo.
11 Me nna atwa mu, me nhyehyɛe apansam. Nanso me koma apɛde
Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka, pamodzinso ndi zokhumba za mtima wanga.
12 ma anadwo dan awia; sum mu koraa no hann bɛn.
Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana, nthawi ya usiku iwo amati ‘kwatsala pangʼono kucha.’
13 Sɛ ofi a mʼani da so nkutoo ne ɔda, sɛ mesɛw me kɛtɛ wɔ sum mu, (Sheol h7585)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
14 sɛ meka kyerɛ porɔwee se, ‘Wo yɛ mʼagya,’ ne osunson se, ‘Me na’ anaa ‘Me nuabea’ a,
ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’ ndiponso kwa mphutsi kuti, ‘ndinu amayi anga’ kapena ‘mlongo wanga,’
15 na afei mʼanidaso wɔ he? Hena na obetumi anya anidaso bi ama me?
tsono chiyembekezo changa chili kuti? Ndani angaone populumukira panga?
16 Ebesian akɔ owu pon ano ana? Yɛn nyinaa besian akɔ mfutuma mu ana?” (Sheol h7585)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)

< Hiob 17 >