< Yeremia 12 >

1 Woyɛ ɔtreneeni bere biara, Awurade, sɛ mede asɛm to wʼanim a. Nso me ne wo bɛkasa afa wʼatɛntrenee ho: Adɛn nti na amumɔyɛfo kwan si wɔn yiye? Adɛn nti na wɔn a wonni gyidi ho dwo wɔn?
Yehova, Inu mumakhala wokhoza nthawi zonse ndikati nditsutsane nanu. Komabe ndikufuna kuyankhula nanu za mlandu wanga. Chifukwa chiyani anthu oyipa zinthu zimawayendera bwino? Chifukwa chiyani anthu achinyengo amakhala pabwino?
2 Woadua wɔn, na wɔagye ntin; wonyinyin na wɔsow aba. Wɔbɔ wo din bere biara nanso wɔn koma mmɛn wo.
Inu munawadzala ndipo anamera mizu; amakula ndi kubereka zipatso. Dzina lanu limakhala pakamwa pawo nthawi zonse, koma mitima yawo imakhala kutali ndi Inu.
3 Nanso wunim me, Awurade; wuhu me, na wosɔ mʼadwene a mewɔ wɔ wo ho no hwɛ. Twe wɔn kɔ sɛ nguan a wɔrekotwitwa wɔn mu! Yi wɔn si nkyɛn ma okumda!
Koma Inu Yehova, ine mumandidziwa; mumandiona ndipo mumayesa zolingalira zanga. Akokeni anthu oyipawo ngati nkhosa zokaphedwa! Ayikeni padera mpaka tsiku loti akaphedwe!
4 Asase no nkyen nkosi da bɛn na prama so sare nguan nkosi da bɛn? Esiane sɛ wɔn a wɔte so no yɛ amumɔyɛfo nti mmoa ne nnomaa a wɔwɔ so awuwu. Na nnipa no da so ka se, “Ɔrenhu nea ɛba yɛn so.”
Kodi dziko lidzakhala likulirabe mpaka liti ndipo udzu mʼmunda uliwonse udzakhalabe ofota mpaka liti? Nyama ndi mbalame kulibiretu chifukwa anthu amene amakhalamo ndi oyipa. Iwo amati: “Yehova sangathe kuona ntchito zathu.”
5 “Sɛ wo ne mmarima atu mmirika ama woabrɛ a, ɛbɛyɛ dɛn na wo ne apɔnkɔ besi mmirikakan? Sɛ wuhintiw wɔ asase petee so a, ɛno de, dɛn na wobɛyɛ wɔ Yordan ho nkyɛkyerɛ mu?
Yehova anayankha kuti, “Ngati kukutopetsa kuthamanga pamodzi ndi anthu nanga ungapikisane bwanji ndi akavalo? Ngati ukupunthwa ndi kugwa pa malo abwino, udzatha bwanji kuthamanga mʼnkhalango za ku Yorodani?
6 Wo nuabarimanom, wʼankasa abusuafo, wɔn mpo ayi wo ama; wɔteɛ mu dennen tia wo. Mfa wo ho nto wɔn so, sɛ mpo wɔka wo ho asɛm pa a.
Ngakhale abale ako ndi anansi akuwukira, onsewo amvana zokuyimba mlandu. Usawakhulupirire, ngakhale ayankhule zabwino ndi iwe.
7 “Megyaw me fi, ato mʼagyapade asaworam; mede nea medɔ no no bɛhyɛ nʼatamfo nsa.
“Ine ndawasiya anthu anga; anthu amene ndinawasankha ndawataya. Ndapereka okondedwa anga mʼmanja mwa adani awo.
8 Mʼagyapade ayɛ me sɛ gyata a ɔwɔ kwae mu. Ɔbobɔ mu gu me so; ɛno nti metan no.
Anthu amene ndinawasankha asanduka ngati mkango wa mʼnkhalango. Akundibangulira mwaukali; nʼchifukwa chake Ine ndikudana nawo.
9 So mʼagyapade nyɛɛ me sɛ anomaa a nkekae sisi ne ho a ɔkyere mmoa na nnomaa foforo a wɔkyere mmoa atwa ne ho ahyia resosɔw no ana? Monkɔboaboa nkekaboa nyinaa ano. Momfa wɔn mmra na wonkum wɔn.
Anthu anga amene ndinawasankha asanduka ngati mbalame yolusa yamawangamawanga imene akabawi ayizinga. Pitani, kasonkhanitseni nyama zakuthengo. Mubwere nazo kuti zidzadye mbalameyo.
10 Nguanhwɛfo bebree bɛsɛe me bobeturo, na wɔatiatia me mfuw so; wɔbɛdan me mfuw fɛɛfɛ no ayɛ no asase hunu a ɛda mpan.
Abusa ambiri anawononga munda wanga wa mpesa, anapondereza munda wanga; munda wanga wabwino uja anawusandutsa chipululu.
11 Ɛbɛyɛ asase a ada mpan a, awo wosee na ɛda hɔ kwa wɔ mʼanim; asase no nyinaa bɛda mpan efisɛ obiara nni hɔ a ɔhwɛ so.
Unawusandutsadi chipululu. Ukanali wokhawokha chomwecho ukundilirira Ine. Dziko lonse lasanduka chipululu chifukwa palibe wolisamalira.
12 Nkoko wosee a ɛwɔ nweatam no nyinaa so no na asɛefo bɛba abegu bebree, Awurade afoa bekunkum wɔn afi asase ano de akosi ano nohɔ; obiara remfa ne ho nni.
Anthu onse owononga abalalikira ku zitunda zonse za mʼchipululu. Yehova watuma ankhondo ake kudzawatha kuyambira kumalire ena a dziko mpaka ku malire enanso a dziko, ndipo palibe amene adzakhale pa mtendere.
13 Wobedua atoko, nso wobetwa nsɔe; wɔbɛbrɛ wɔn ho nanso wɔrennya hwee. Wɔn ani bewu wɔ wɔn nnɔbaetwa ho. Awurade abufuwhyew nti.”
Anthu anafesa tirigu koma anatuta minga; anadzitopetsa kugwira ntchito koma osapeza phindu lililonse. Choncho mudzachita manyazi ndi zokolola zanu chifukwa cha mkwiyo wa Yehova.”
14 Nea Awurade se ni: “Na me yɔnkonom amumɔyɛfo a wɔfa agyapade a, mede maa me nkurɔfo Israelfo no de, metu wɔn afi wɔn nsase so na metu Yudafi afi wɔn mu.
“Anthu oyipa oyandikana ndi anthu anga Aisraeli, akuwalanda Aisraeliwo dziko, cholowa chimene ndinawapatsa. Nʼchifukwa chake ndidzawachotsa mʼdziko limenelo, ndipo ndidzachotsa banja la Yuda pakati pawo.
15 Na sɛ mitu wɔn wie a, mehu wɔn mmɔbɔ bio, na mede wɔn mu biara bɛba nʼagyapade, ne nʼasase so.
Komabe nditawachotsa, ndidzawachitiranso chifundo, ndipo ndidzabwezera aliyense cholowa chake ndi dziko lake.
16 Na sɛ wosua me nkurɔfo akwan yiye na wɔbɔ me din ka ntam se, ‘Nokware sɛ Awurade te ase yi’ a, ɛwɔ mu sɛ mmere bi wɔkyerɛɛ me nkurɔfo ma wɔde Baal kaa ntam de, nanso wɔn ase betim wɔ me nkurɔfo mu.
Ndipo ngati iwo adzaphunzira bwino njira za anthu anga ndi kulumbira mʼdzina langa, namanena kuti, ‘Pali Yehova wamoyo,’ monga iwo anaphunzitsira anthu anga kulumbira mʼdzina la Baala, Ine ndidzawakhazikitsa pakati pa anthu anga.
17 Nanso sɛ ɔman bi antie a, metu nʼase, na masɛe no korakora,” Awurade na ose.
Koma ngati mtundu wina uliwonse sudzamvera, Ine ndidzawuchotsa ndi kuwuwonongeratu,” akutero Yehova.

< Yeremia 12 >