< Habakuk 3 >

1 Saa mpaebɔ yi, Habakuk too no sɛ dwom:
Pemphero la mneneri Habakuku potsata mayimbidwe a Sigionoti.
2 Awurade, mate wo ho nsɛm nyinaa, Na wʼanwonwadwuma a woayɛ no, me ho adwiriw me. Yɛ no foforo wɔ yɛn mmere so. Yɛn mmere yi mu, ma wonhu. Wʼabufuwhyew mu no, kae wo mmɔborɔhunu.
Inu Yehova, ndamva za kutchuka kwanu; Inu Yehova, ntchito zanu zandiopsa. Muzichitenso masiku athu ano, masiku athu ano zidziwike; mu ukali wanu mukumbukire kuchita chifundo.
3 Onyankopɔn fi Teman bae, Ɔkronkronni a ofi Bepɔw Paran so, Nʼanuonyam kata ɔsoro, na nʼayeyi hyɛ asase so ma.
Mulungu anabwera kuchokera ku Temani, Woyerayo kuchokera ku Phiri la Parani. (Sela) Ulemerero wake unaphimba mlengalenga ndipo dziko lapansi linadzaza ndi matamando ake.
4 Ɔhyerɛn sɛ anɔpawia Hann no nsensanee twa yerɛw fi ne nsam, Ɛhɔ na ne tumi ahintaw.
Kuwala kwa ulemerero wake kunali ngati kutuluka kwa dzuwa; kunyezimira kunkatuluka mʼdzanja lake, mʼmene anabisamo mphamvu zake.
5 Ɔyaredɔm di nʼanim kɔ; Na nsanyare di nʼakyi pɛɛ.
Patsogolo pake pankagwa mliri; nthenda yoopsa inkagwa kumbuyo kwake.
6 Sɛ ogyina a, asase wosow. Sɛ ɔhwɛ a, ɔma aman wosow. Tete mmepɔw dwiriwii, na nkoko a efi tete no ka kataa so. Nʼakwan ntwa mu da.
Iye anayimirira ndi kugwedeza dziko lapansi; anayangʼana ndipo mitundu ya anthu inanjenjemera. Mapiri okhazikika anagumuka ndipo zitunda zakalekale zinatitimira. Njira zake ndi zachikhalire.
7 Mihuu Kusanfo ntamadan a atetew ne Midianfo atenae a agyigya.
Ndinaona matenti a ku Kusani ali pa mavuto, mokhala a ku Midiyani muli ululu waukulu.
8 Awurade, wo bo fuw nsubɔnten no? Wʼabufuw no tiaa nsuwansuwa no? Wosɔre tiaa po, bere a wo ne wʼapɔnkɔ ne nkonimdi nteaseɛnam nam no.
Inu Yehova, kodi munakwiyira mitsinje? Kodi munakalipira timitsinje? Kodi munapsera mtima nyanja pamene munakwera pa akavalo anu ndiponso magaleta anu achipulumutso?
9 Wuyii wo tadua, Woma wɔde agyan bebree brɛɛ wo. Wode nsubɔnten paapae asase mu.
Munasolola uta wanu mʼchimake, munayitanitsa mivi yambiri. (Sela) Munagawa dziko lapansi ndi mitsinje;
10 Mmepɔw huu wo, na wɔwosowee Osuhweam bɛsen kɔe. Bun no woroo so, na ehuru baa soro.
mapiri anakuonani ndipo anagwedezeka. Madzi amphamvu anasefukira; nyanja yozama inakokoma ndipo mafunde ake anakwera kwambiri.
11 Owia ne ɔsram gyinagyinaa sorosoro hɔ, bere a wohuu wʼagyan a ɛnenam wim no hann, ne wo peaw a ɛpa yerɛw yerɛw no.
Dzuwa ndi mwezi zinayima chilili mlengalenga, pa kungʼanima kwa mivi yanu yowulukayo, pa kunyezimira kwa mkondo wanu.
12 Wʼabufuwhyew mu no, wonantew twaa asase so na wode abufuw tiatiaa aman no so.
Munayendayenda mʼdziko lapansi muli ndi ukali, ndipo munapondereza mitundu ya anthu muli ndi mkwiyo.
13 Wobaa se worebegye wo nkurɔfo, na woagye nea wɔasra no no nkwa. Wopɛtɛw atirimɔdenfoman no kannifo, wopaa ne ho ntama fi ne ti so kosii ne nan ase.
Munapita kukalanditsa anthu anu, kukapulumutsa wodzozedwa wanu. Munakantha mtsogoleri wa dziko la anthu oyipa, munawononga anthu ake onse. (Sela)
14 Wode nʼankasa peaw hwirew ne ti mu, bere a nʼakofo bɔɔ yerɛdɛ sɛ wɔrebɛhwete yɛn mu. Wɔpɛɛ sɛ wɔbɛtɔre mmɔborɔfo a wɔakɔ agua no ase koraa.
Ndi mkondo wake womwe munalasa mtsogoleri wake pamene ankhondo ake anabwera mwamphamvu kudzatibalalitsa, ankasangalala ngati kuti akudzawononga osauka amene akubisala.
15 Wode wʼapɔnkɔ tiatiaa po no mu, ma asu kɛse no hurui.
Munapondaponda pa nyanja ndi akavalo anu, kuvundula madzi amphamvu.
16 Metee no, me koma tui, nnyigyei no maa mʼano poo biribiri; ɔporɔw hyɛn me nnompe mu, na me nan wosowee. Nanso mɛtɔ me bo ase atwɛn akosi sɛ amanehunu da bɛba ɔman a wɔtow hyɛɛ yɛn so no so.
Ndinamva ndipo mtima wanga unagunda kwambiri, milomo yanga inanjenjemera pakumva phokosolo; mafupa anga anaguluka, ndipo mawondo anga anawombana. Komabe ndikuyembekezera mofatsa, tsiku la masautso limene lidzafike pa mtundu wa anthu umene ukutithira nkhondo.
17 Ɛwɔ mu, borɔdɔma nnua no nguu nhwiren, na aba nso nni bobe no so; ɛwɔ mu, ngodua no adi huammɔ na mfuw no mmɔ aduan. Ɛwɔ mu, nguan biara nni buw no mu, na anantwi nso nni ban no mu.
Ngakhale mtengo wa mkuyu usachite maluwa, ndipo mipesa ikhale yopanda mphesa. Ngakhale mitengo ya olivi isabereke zipatso, ndipo mʼminda musatuluke kanthu. Ngakhale nkhosa ndi ngʼombe zithe mʼkhola,
18 Nanso mʼani begye Awurade mu; me ho bɛsɛpɛw me wɔ Onyankopɔn a ɔyɛ mʼagyenkwa no mu.
komabe ine ndidzakondwera mwa Yehova, ndidzasangalala mwa Mulungu Mpulumutsi wanga.
19 Otumfo Awurade yɛ mʼahoɔden. Ɔma me nan yɛ sɛ ɔforote de, ɔma me nantew sorɔnsorɔmmea. Wɔmfa mpae yi mma nnwonto kwankyerɛfo no. Na wɔnto no wɔ mʼasanku no so.
Ambuye Yehova ndiye mphamvu yanga; amalimbitsa miyendo yanga ngati ya mbawala yayikazi, amandithandiza kukafika pamwamba pa phiri. Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za nsambo.

< Habakuk 3 >