< Mezmurlar 1 >

1 Ne mutlu o insana ki, kötülerin öğüdüyle yürümez, Günahkârların yolunda durmaz, Alaycıların arasında oturmaz.
Wodala munthu amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa, kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa, kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
2 Ancak zevkini RAB'bin Yasası'ndan alır Ve gece gündüz onun üzerinde derin derin düşünür.
Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
3 Böylesi akarsu kıyılarına dikilmiş ağaca benzer, Meyvesini mevsiminde verir, Yaprağı hiç solmaz. Yaptığı her işi başarır.
Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi, umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake ndipo masamba ake safota. Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
4 Kötüler böyle değil, Rüzgarın savurduğu saman çöpüne benzerler.
Sizitero ndi anthu oyipa! Iwo ali ngati mungu umene umawuluzidwa ndi mphepo.
5 Bu yüzden yargılanınca aklanamaz, Doğrular topluluğunda yer bulamaz günahkârlar.
Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo, kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
6 Çünkü RAB doğruların yolunu gözetir, Kötülerin yolu ise ölüme götürür.
Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama, koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.

< Mezmurlar 1 >