< Mezmurlar 48 >

1 İlahi - Korahoğulları'nın mezmuru RAB büyüktür ve yalnız O övülmeye değer Tanrımız'ın kentinde, kutsal dağında.
Nyimbo. Salimo la ana a Kora. Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando mu mzinda wa Mulungu wathu, phiri lake loyera.
2 Yükselir zarafetle, Bütün yeryüzünün sevinci Siyon Dağı, Safon'un doruğu, ulu Kral'ın kenti.
Lokongola mu utali mwake, chimwemwe cha dziko lonse lapansi. Malo aatali kwambiri a Zafoni ndiye Phiri la Ziyoni, mzinda wa Mfumu yayikulu.
3 Tanrı onun kalelerinde Sağlam kule olarak gösterdi kendini.
Mulungu ali mu malinga ake; Iye wadzionetsa yekha kuti ndiye malinga akewo.
4 Krallar toplandı, Birlikte Siyon'un üzerine yürüdüler.
Pamene mafumu anasonkhana pamodzi, pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe,
5 Ama onu görünce şaşkına döndüler, Dehşete düşüp kaçtılar.
iwo anaona mzindawo ndipo anadabwa kwambiri; anathawa ndi mantha aakulu.
6 Doğum sancısı tutan kadın gibi, Bir titreme aldı onları orada.
Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera, ululu wonga wa mkazi woyembekezera pa nthawi yochira.
7 Doğu rüzgarının parçaladığı ticaret gemileri gibi Yok ettin onları.
Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi zitawonongeka ndi mphepo ya kummawa.
8 Her Şeye Egemen RAB'bin kentinde, Tanrımız'ın kentinde, Nasıl duyduksa, öyle gördük. Tanrı onu sonsuza dek güvenlik içinde tutacak. (Sela)
Monga momwe tinamvera, kotero ife tinaona mu mzinda wa Yehova Wamphamvuzonse, mu mzinda wa Mulungu wathu. Mulungu adzawuteteza kwamuyaya.
9 Ey Tanrı, tapınağında, Ne kadar vefalı olduğunu düşünüyoruz.
Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu, ife timalingaliramo zachikondi chanu chosasinthika.
10 Adın gibi, ey Tanrı, övgün de Dünyanın dört bucağına varıyor. Sağ elin zafer dolu.
Monga dzina lanu, Inu Mulungu, matamando anu amafika ku malekezero a dziko lapansi dzanja lanu lamanja ladzaza ndi chilungamo.
11 Sevinsin Siyon Dağı, Coşsun Yahuda kentleri Senin yargılarınla!
Phiri la Ziyoni likukondwera, midzi ya Yuda ndi yosangalala chifukwa cha maweruzo anu.
12 Siyon'un çevresini gezip dolanın, Kulelerini sayın,
Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo, werengani nsanja zake.
13 Surlarına dikkatle bakın, Kalelerini yoklayın ki, Gelecek kuşağa anlatasınız:
Yangʼanitsitsani bwino mipanda yake, penyetsetsani malinga ake, kuti mudzafotokoze za izo ku mʼbado wotsatira.
14 Bu Tanrı sonsuza dek bizim Tanrımız olacak, Bize hep yol gösterecektir.
Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha; Iye adzakhala mtsogoleri wathu mpaka ku mapeto.

< Mezmurlar 48 >