< Mezmurlar 2 >
1 Nedir uluslar arasındaki bu kargaşa, Neden boş düzenler kurar bu halklar?
Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu?
2 Dünyanın kralları saf bağlıyor, Hükümdarlar birleşiyor RAB'be ve meshettiği krala karşı.
Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.
3 “Koparalım onların kayışlarını” diyorlar, “Atalım üzerimizden bağlarını.”
Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”
4 Göklerde oturan Rab gülüyor, Onlarla eğleniyor.
Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo.
5 Sonra öfkeyle uyarıyor onları, Gazabıyla dehşete düşürüyor
Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
6 Ve, “Ben kralımı Kutsal dağım Siyon'a oturttum” diyor.
“Ine ndakhazikitsa mfumu yanga pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
7 RAB'bin bildirisini ilan edeceğim: Bana, “Sen benim oğlumsun” dedi, “Bugün ben sana baba oldum.
Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako.
8 Dile benden, miras olarak sana ulusları, Mülk olarak yeryüzünün dört bucağını vereyim.
Tandipempha, ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako; malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
9 Demir çomakla kıracaksın onları, Çömlek gibi parçalayacaksın.”
Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
10 Ey krallar, akıllı olun! Ey dünya önderleri, ders alın!
Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
11 RAB'be korkuyla hizmet edin, Titreyerek sevinin.
Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
12 Oğulu öpün ki öfkelenmesin, Yoksa izlediğiniz yolda mahvolursunuz. Çünkü öfkesi bir anda alevleniverir. Ne mutlu O'na sığınanlara!
Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye; kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu, pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa. Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.