< Mezmurlar 13 >
1 Müzik şefi için - Davut'un mezmuru Ne zamana dek, ya RAB, Sonsuza dek mi beni unutacaksın? Ne zamana dek yüzünü benden gizleyeceksin?
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale? Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
2 Ne zamana dek içimde tasa, Yüreğimde hep keder olacak? Ne zamana dek düşmanım bana üstün çıkacak?
Ndidzalimbana ndi maganizo anga ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti? Mpaka liti adani anga adzandipambana?
3 Gör halimi, ya RAB, yanıtla Tanrım, Gözlerimi aç, ölüm uykusuna dalmayayım.
Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga. Walitsani maso anga kuti ndingafe;
4 Düşmanlarım, “Onu yendik!” demesin, Sarsıldığımda hasımlarım sevinmesin.
mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,” ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.
5 Ben senin sevgine güveniyorum, Yüreğim kurtarışınla coşsun.
Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika; mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
6 Ezgiler söyleyeceğim sana, ya RAB, Çünkü iyilik ettin bana.
Ine ndidzayimbira Yehova pakuti wandichitira zokoma.