< Mezmurlar 127 >

1 Süleyman'ın hac ilahisi Evi RAB yapmazsa, Yapıcılar boşuna didinir. Kenti RAB korumazsa, Bekçi boşuna bekler.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni. Yehova akapanda kumanga nyumba, omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe. Yehova akapanda kulondera mzinda, mlonda akanangolondera pachabe.
2 Boşuna erken kalkıp Geç yatıyorsunuz. Ey zahmetle kazanılan ekmeği yiyenler, RAB sevdiklerinin rahat uyumasını sağlar.
Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa ndi kusagona msanga madzulo, kuvutikira chakudya choti mudye, pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.
3 Çocuklar RAB'bin verdiği bir armağandır, Rahmin ürünü bir ödüldür.
Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova, ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.
4 Yiğidin elinde nasılsa oklar, Öyledir gençlikte doğan çocuklar.
Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja mwa munthu wankhondo.
5 Ne mutlu ok kılıfı onlarla dolu insana! Kent kapısında hasımlarıyla tartışırken Utanç duymayacaklar.
Wodala munthu amene motengera mivi mwake mwadzaza. Iwo sadzachititsidwa manyazi pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.

< Mezmurlar 127 >