< Mezmurlar 114 >

1 İsrail Mısır'dan çıktığında, Yakup'un soyu yabancı dil konuşan bir halktan ayrıldığında,
Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
2 Yahuda Rab'bin kutsal yeri oldu, İsrail de O'nun krallığı.
Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
3 Deniz olanı görüp geri çekildi, Şeria Irmağı tersine aktı.
Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
4 Dağlar koç gibi, Tepeler kuzu gibi sıçradı.
mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
5 Ey deniz, sana ne oldu da kaçtın? Ey Şeria, neden tersine aktın?
Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
6 Ey dağlar, niçin koç gibi, Ey tepeler, niçin kuzu gibi sıçradınız?
inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
7 Titre, ey yeryüzü, Kayayı havuza, Çakmaktaşını pınara çeviren Rab'bin önünde, Yakup'un Tanrısı'nın huzurunda.
Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
8
amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.

< Mezmurlar 114 >