< Çölde Sayim 7 >

1 Musa konutu bitirdiği gün onu meshetti. Onu ve içindeki bütün eşyaları, sunağı ve bütün takımlarını da meshedip adadı.
Mose atamaliza kuyimika chihema chija, anachidzoza mafuta ndi kuchipatula pamodzi ndi ziwiya zake zonse. Anadzozanso guwa lansembe ndi kulipatula pamodzi ndi ziwiya zake zonse.
2 Sonra İsrail ileri gelenleri, sayılanlardan sorumlu olan aile ve oymak önderleri armağanlar sundular. RAB'be armağan olarak üstü kapalı altı araba ve on iki öküz getirdiler: Her iki önder için bir araba, her önder için bir öküz. Bu armağanları konutun önüne getirdiler.
Kenaka atsogoleri a Aisraeli, akuluakulu a mabanja omwe ankayangʼanira mafuko a anthu omwe anawawerenga aja, anachita chopereka.
3
Anabweretsa zopereka zawo pamaso pa Yehova: ngolo zophimbidwa zisanu ndi imodzi ndiponso ngʼombe zothena khumi ndi ziwiri. Mtsogoleri mmodzi ngʼombe yothena imodzi ndipo atsogoleri awiri ngolo imodzi. Izi anazipereka ku chihema.
4 Sonra RAB Musa'ya, “Bunları Buluşma Çadırı'ndaki hizmetlerde kullanılmak üzere onlardan alıp yapacakları işe göre Levililer'e ver” dedi.
Yehova anawuza Mose kuti,
5
“Ulandire zimenezi kwa iwo kuti zigwire ntchito ku tenti ya msonkhano. Uzipereke kwa Alevi, aliyense monga mwa ntchito yake.”
6 Musa arabaları, öküzleri alıp Levililer'e verdi.
Choncho Mose anatenga ngolo ndi ngʼombe zothenazo nazipereka kwa Alevi.
7 Yapacakları işe göre Gerşonoğulları'na iki arabayla dört öküz,
Anapereka ngolo ziwiri ndi ngʼombe zothena zinayi kwa Ageresoni monga mwantchito yawo
8 Merarioğulları'na da dört arabayla sekiz öküz verdi. Bunlar Kâhin Harun oğlu İtamar'ın sorumluluğu altında yapıldı.
ndiponso anapereka ngolo zinayi ndi ngʼombe zothena zisanu ndi zitatu kwa Amerari molingananso ndi ntchito yawo. Onsewa ankawayangʼanira anali Itamara mwana wa Aaroni wansembe.
9 Kehatoğulları'na ise bir şey vermedi. Çünkü onların görevi kutsal eşyaları omuzlarında taşımaktı.
Koma Mose sanapereke zimenezi kwa Akohati chifukwa zinthu zawo zopatulika zomwe ankayangʼanira zinali zoti azinyamula pa mapewa awo.
10 Meshedilen sunağın adanması için önderler armağanlarını sunağın önüne getirdiler.
Guwa la nsembe litadzozedwa, atsogoleri anabweretsa zopereka zawo zopatulira guwa nazipereka paguwapo.
11 Çünkü RAB Musa'ya, “Sunağın adanması için her gün bir önder kendi armağanını sunacak” demişti.
Pakuti Yehova anawuza Mose kuti, “Tsiku lililonse mtsogoleri mmodzi azibweretsa chopereka chake chopatulira guwa lansembe.”
12 Birinci gün Yahuda oymağından Amminadav oğlu Nahşon armağanlarını sundu.
Amene anabweretsa chopereka chake tsiku loyamba anali Naasoni mwana wa Aminadabu wa fuko la Yuda.
13 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chake chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi, ndi beseni lasiliva limodzi lowazira, lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo wopatulika ndipo zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta ngati chopereka chachakudya;
14 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;
15 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa yayimuna imodzi ndi mwana wankhosa wamwamuna mmodzi wa chaka chimodzi, za nsembe yopsereza;
16 günah sunusu için bir teke;
mbuzi yayimuna imodzi, nsembe ya machimo;
17 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Amminadav oğlu Nahşon'un getirdiği armağanlar bunlardı.
ndi ngʼombe zothena ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa asanu a chaka chimodzi kuti zikhale za nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Naasoni mwana wa Aminadabu.
18 İkinci gün İssakar oymağı önderi Suar oğlu Netanel armağanlarını sundu.
Pa tsiku lachiwiri, Natanieli mwana wa Zuwara, mtsogoleri wa Isakara, anabweretsa chopereka chake.
19 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chomwe anabwera nacho chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi, beseni limodzi lowazira lasiliva lolemera magalamu 800, molingana ndi muyeso wa ku malo opatulika. Mbale zonse zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta monga chopereka cha chakudya.
20 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
Mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110 yodzaza ndi lubani;
21 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa yayimuna imodzi ndi mwana wankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, za nsembe yopsereza:
22 günah sunusu için bir teke;
mbuzi yayimuna imodzi ya nsembe yotetezera machimo;
23 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Suar oğlu Netanel'in getirdiği armağanlar bunlardı.
ndi ngʼombe ziwiri, nkhosa zazimuna ziwiri, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa asanu a chaka chimodzi, nsembe ya chiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Netanieli mwana wa Zuwara.
24 Üçüncü gün Zevulun oymağı önderi Helon oğlu Eliav armağanlarını sundu.
Pa tsiku lachitatu, Eliabu mwana wa Heloni, mtsogoleri wa Azebuloni, anabweretsa chopereka chake.
25 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chake chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka, ndi beseni limodzi lasiliva lowazira lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo opatulika, mbale zonse zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, chopereka cha chakudya;
26 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;
27 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa yayimuna imodzi ndi mwana wankhosa wamwamuna mmodzi wa chaka chimodzi, za nsembe yopsereza;
28 günah sunusu için bir teke;
mbuzi imodzi ya nsembe yopepesera machimo;
29 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Helon oğlu Eliav'ın getirdiği armağanlar bunlardı.
ndi ngʼombe ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Eliabu mwana wa Heloni.
30 Dördüncü gün Ruben oymağı önderi Şedeur oğlu Elisur armağanlarını sundu.
Tsiku lachinayi linali la Elizuri mwana wa Sedeuri, mtsogoleri wa fuko la Rubeni, anabweretsa chopereka chake.
31 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chake chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka, beseni limodzi lowazira lasiliva lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo opatulika; zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, chopereka chachakudya.
32 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
Mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;
33 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa yayimuna imodzi ndi mwana wankhosa wa chaka chimodzi, za nsembe yopsereza;
34 günah sunusu için bir teke;
mbuzi imodzi ya nsembe yopepesera machimo;
35 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Şedeur oğlu Elisur'un getirdiği armağanlar bunlardı.
ndi ngʼombe zazimuna ziwiri, nkhosa zazimuna ziwiri, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Elizuri mwana wa Sedeuri.
36 Beşinci gün Şimon oymağı önderi Surişadday oğlu Şelumiel armağanlarını sundu.
Pa tsiku lachisanu Selumieli mwana wa Zurisadai, mtsogoleri wa fuko la Simeoni, anabweretsa chopereka chake.
37 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chake chinali mbale yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka ndi beseni limodzi lowazira lasiliva lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo opatulika. Zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta monga chopereka chachakudya;
38 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale yagolide imodzi yolemera 110, yodzaza ndi lubani;
39 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa imodzi ndi mwana wankhosa mmodzi wamwamuna wa chaka chimodzi, za nsembe yopsereza;
40 günah sunusu için bir teke;
mbuzi imodzi ya nsembe yopepesera machimo;
41 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Surişadday oğlu Şelumiel'in getirdiği armağanlar bunlardı.
ngʼombe ziwiri, nkhosa zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Selumieli mwana wa Zurisadai.
42 Altıncı gün Gad oymağı önderi Deuel oğlu Elyasaf armağanlarını sundu.
Pa tsiku lachisanu ndi chimodzi, Eliyasafu mwana wa Deuweli, mtsogoleri wa fuko la Gadi, anabweretsa chopereka chake.
43 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chakecho chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka, beseni limodzi lowazira lasiliva lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo opatulika; zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta monga chopereka chachakudya;
44 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;
45 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa yayimuna imodzi ndi mwana wankhosa wamwamuna mmodzi wa chaka chimodzi, chopereka cha nsembe yopsereza:
46 günah sunusu için bir teke;
mbuzi yayimuna imodzi ya nsembe yopepesera machimo;
47 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Deuel oğlu Elyasaf'ın getirdiği armağanlar bunlardı.
ngʼombe zazimuna ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Eliyasafu mwana wa Deuweli.
48 Yedinci gün Efrayim oymağı önderi Ammihut oğlu Elişama armağanlarını sundu.
Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri Elisama mwana wa Amihudi, mtsogoleri wa fuko la Efereimu, anabweretsa chopereka chake.
49 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chakecho chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka, ndi beseni limodzi lowazira lasiliva lolemera magalamu 800, zonsezi monga mwa muyeso wa ku malo opatulika, zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta monga chopereka chachakudya;
50 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;
51 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa imodzi yayimuna ndi mwana wankhosa wamwamuna mmodzi wa chaka chimodzi, nsembe yopsereza;
52 günah sunusu için bir teke;
mbuzi imodzi ya nsembe yopepesera machimo;
53 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Ammihut oğlu Elişama'nın getirdiği armağanlar bunlardı.
ngʼombe ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Elisama mwana wa Amihudi.
54 Sekizinci gün Manaşşe oymağı önderi Pedahsur oğlu Gamliel armağanlarını sundu.
Pa tsiku lachisanu ndi chitatu Gamalieli mwana wa Pedazuri, mtsogoleri wa fuko Manase, anabweretsa chopereka chake.
55 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chakecho chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka, ndi beseni limodzi lowazira lasiliva lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo opatulika; zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta monga chopereka chachakudya;
56 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani,
57 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa yayimuna imodzi ndi mwana wankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, nsembe yopsereza;
58 günah sunusu için bir teke;
mbuzi imodzi ya nsembe yopepesera machimo;
59 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Pedahsur oğlu Gamliel'in getirdiği armağanlar bunlardı.
ngʼombe zazimuna ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Gamalieli mwana wa Pedazuri.
60 Dokuzuncu gün Benyamin oymağı önderi Gidoni oğlu Avidan armağanlarını sundu.
Pa tsiku lachisanu ndi chinayi Abidani mwana wa Gideoni mtsogoleri wa fuko la Benjamini, anabweretsa chopereka chake.
61 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chakecho chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka ndi beseni limodzi lowazira lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo opatulika; zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta monga chopereka cha zakudya;
62 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;
63 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa imodzi yayimuna ndi mwana wankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, nsembe yopsereza;
64 günah sunusu için bir teke;
mbuzi yayimuna imodzi ya nsembe yopepesera machimo;
65 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Gidoni oğlu Avidan'ın getirdiği armağanlar bunlardı.
ngʼombe zazimuna ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu, ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Abidani mwana wa Gideoni.
66 Onuncu gün Dan oymağı önderi Ammişadday oğlu Ahiezer armağanlarını sundu.
Pa tsiku lakhumi Ahiyezeri mwana wa Amisadai, mtsogoleri wa fuko la Dani anabweretsa chopereka chake.
67 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chake chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka, beseni limodzi lowazira lasiliva lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo opatulika, zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta monga chopereka chachakudya;
68 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;
69 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa imodzi yayimuna ndi mwana wankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, nsembe yopsereza;
70 günah sunusu için bir teke;
mbuzi yayimuna imodzi ya nsembe yopepesera machimo;
71 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Ammişadday oğlu Ahiezer'in getirdiği armağanlar bunlardı.
ndi ngʼombe ziwiri zazimuna, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu, ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Ahiyezeri mwana wa Amisadai.
72 On birinci gün Aşer oymağı önderi Okran oğlu Pagiel armağanlarını sundu.
Pa tsiku la khumi ndi chimodzi, Pagieli mwana wa Okirani, mtsogoleri wa fuko la Aseri, anabweretsa chopereka chake.
73 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chakecho chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka, beseni limodzi lowazira lasiliva lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo opatulika; zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta monga chopereka chachakudya;
74 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;
75 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa imodzi yayimuna ndi mwana wankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, za nsembe yopsereza;
76 günah sunusu için bir teke;
mbuzi imodzi yayimuna ya nsembe yopepesera machimo;
77 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Okran oğlu Pagiel'in getirdiği armağanlar bunlardı.
ngʼombe ziwiri zazimuna, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu, ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Pagieli mwana wa Okirani.
78 On ikinci gün Naftali oymağı önderi Enan oğlu Ahira armağanlarını sundu.
Pa tsiku la khumi ndi chimodzi Ahira mwana wa Enani, mtsogoleri wa fuko la Nafutali, anabweretsa chopereka chake.
79 Getirdiği armağanlar şunlardı: 130 kutsal yerin şekeli ağırlığında gümüş bir tabak, yetmiş şekel ağırlığında gümüş bir çanak –ikisi de tahıl sunusu için zeytinyağıyla yoğrulmuş ince un doluydu–
Chopereka chakecho chinali mbale imodzi yasiliva yolemera kilogalamu imodzi ndi theka, beseni limodzi lowazira lasiliva lowazira lolemera magalamu 800, zonse monga mwa muyeso wa ku malo opatulika, zonse ziwiri zinali zodzaza ndi ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta monga chopereka chachakudya;
80 buhur dolu on şekel ağırlığında altın bir tabak;
mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;
81 yakmalık sunu için bir boğa, bir koç, bir yaşında bir erkek kuzu;
mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa imodzi yayimuna ndi mwana wankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, nsembe yopsereza;
82 günah sunusu için bir teke;
mbuzi yayimuna imodzi ya nsembe yopepesera machimo;
83 esenlik kurbanı için iki sığır, beş koç, beş teke, bir yaşında beş kuzu. Enan oğlu Ahira'nın getirdiği armağanlar bunlardı.
ngʼombe zazimuna ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu, ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Ahira mwana wa Enani.
84 Sunak meshedildiğinde İsrail önderlerinin adanması için sunduğu armağanlar şunlardı: On iki gümüş tabak, on iki gümüş çanak, on iki altın tabak;
Zopereka za atsogoleri a Israeli zopatulira guwa lansembe pamene linadzozedwa zinali izi: mbale khumi ndi ziwiri zasiliva, mabeseni owazira asiliva khumi ndi awiri ndi mbale zagolide khumi ndi ziwiri.
85 her gümüş tabağın ağırlığı 130 şekel, her çanağın ağırlığı yetmiş şekeldi. Bütün gümüş eşyaların toplam ağırlığı 2 400 kutsal yerin şekeliydi.
Mbale iliyonse yasiliva inkalemera kilogalamu imodzi ndi theka, ndipo beseni lililonse lowazira linkalemera magalamu 800. Pamodzi, mbale zonse zasiliva zinkalemera makilogalamu 27 monga mwa muyeso wa ku malo opatulika.
86 Buhur dolu on iki altın tabağın her birinin ağırlığı on kutsal yerin şekeliydi. Bütün altın tabakların toplam ağırlığı 120 şekeldi.
Mbale khumi ndi ziwiri zagolide zodzaza ndi lubanizo zinkalemera magalamu 110 iliyonse, monga mwa muyeso wa ku malo opatulika. Pamodzi, mbale zagolide zinkalemera kilogalamu imodzi ndi theka.
87 Yakmalık sunu için tahıl sunularıyla birlikte sunulan hayvanların sayısı on iki boğa, on iki koç, bir yaşında on iki erkek kuzuydu; günah sunusu için de on iki teke sunuldu.
Chiwerengero cha nyama zonse za nsembe yopsereza chinali motere: ngʼombe zazimuna khumi ndi ziwiri, nkhosa zazimuna khumi ndi ziwiri ndi ana ankhosa aamuna khumi ndi awiri a chaka chimodzi pamodzi ndi chopereka chachakudya. Mbuzi zazimuna khumi ndi ziwiri zinali za nsembe yopepesera machimo.
88 Esenlik kurbanı için sunulan hayvanların sayısı yirmi dört sığır, altmış koç, altmış teke, bir yaşında altmış kuzuydu. Sunak meshedildikten sonra, adanması için verilen armağanlar bunlardı.
Chiwerengero cha nyama zonse za nsembe yachiyanjano chinali motere: ngʼombe zothena 24, nkhosa zazimuna 60, mbuzi zazimuna 60 ndi ana ankhosa aamuna a chaka chimodzi 60. Zimenezi ndi zimene zinali zopereka zopatulira guwa lansembe litadzozedwa.
89 Musa RAB'le konuşmak için Buluşma Çadırı'na girince, Levha Sandığı'nın Bağışlanma Kapağı'nın üstündeki iki Keruv arasından kendisine seslenen sesi duydu. RAB Musa'yla bu şekilde konuştu.
Mose atalowa mu tenti ya msonkhano kukayankhula ndi Yehova, anamva mawu kuchokera pakati pa Akerubi awiri amene anali pamwamba pa chivundikiro cha bokosi la umboni. Ndipo anayankhula naye.

< Çölde Sayim 7 >