< Levililer 24 >

1 RAB Musa'ya şöyle dedi:
Yehova anawuza Mose kuti,
2 “İsrail halkına buyruk ver, kandilin sürekli yanıp ışık vermesi için saf sıkma zeytinyağı getirsinler.
“Lamula Aisraeli kuti akupatse mafuta anyale, a olivi wabwino kwambiri kuti nyalezo ziziyaka nthawi zonse.
3 Harun kandilleri benim huzurumda, Buluşma Çadırı'nda, Levha Sandığı'nın önündeki perdenin dışında, akşamdan sabaha kadar sürekli yanar biçimde tutacak. Kuşaklar boyunca sürekli bir kural olacak bu.
Kunja kwa nsalu yotchinga Bokosi la Chipangano, mʼchihema cha msonkhano, Aaroni azionetsetsa kuti nyale ikukhala chiyakire pamaso pa Yehova kuyambira madzulo mpaka mmawa, nthawi zonse. Limeneli ndi lamulo lamuyaya pa mibado yonse.
4 RAB'bin huzurunda saf altın kandillikteki kandiller sürekli yanacaktır.”
Aaroni ayatse nyale zimene zili pa choyikapo nyale chagolide wabwino kwambiri kuti zikhale zoyaka nthawi zonse pamaso pa Yehova.
5 “İnce undan on iki pide pişireceksin. Her biri efanın onda ikisi ağırlığında olacak.
“Mutenge ufa wosalala ndipo muphike makeke khumi ndi awiri ndipo keke iliyonse ikhale ya ufa wa makilogalamu awiri.
6 Bunları RAB'bin huzurunda iki sıra halinde, altışar altışar saf altın masanın üzerine dizeceksin.
Muwayike pa tebulo la golide wabwino kwambiri pamaso pa Yehova mʼmizere iwiri. Mzere uliwonse ukhale wa makeke asanu ndi imodzi.
7 İki sıra ekmeğin yanına anma payı olarak saf günnük koyacaksın. Bu RAB için yakılan sunu olacak ve ekmeğin yerini alacak.
Pa mzere uliwonse muyikepo lubani wafungo lokoma kuti pamodzi ndi bulediyo akhale wachikumbutso cha nsembe yopsereza yopereka kwa Yehova.
8 Bu ekmek, İsrail halkı adına sonsuza dek sürecek bir antlaşma olarak, her Şabat Günü aksatılmadan RAB'bin huzurunda dizilecek.
Sabata ndi sabata nthawi zonse Aaroni aziyika makeke amenewa pamaso pa Yehova mʼmalo mwa Aisraeli onse kuti akhale pangano lamuyaya.
9 Ve Harun'la oğullarına ait olacak. Onu kutsal bir yerde yiyecekler. Çünkü çok kutsaldır. RAB için yakılan sunulardan onların sürekli bir payı olacak.”
Chakudyacho ndi cha Aaroni ndi ana ake ndipo azidyera ku malo wopatulika chifukwa kwa iye chakudyacho ndi chopatulika kwambiri chochokera pa chopereka chopsereza cha Yehova.”
10 İsrailliler arasında annesi İsrailli babası Mısırlı bir adam vardı. Ordugahta onunla bir İsrailli arasında kavga çıktı.
Tsiku lina munthu wina wamwamuna amene amayi ake anali Mwisraeli koma abambo ake anali Mwigupto anapita kwa Aisraeli ndipo anakangana ndi Mwisraeli wina ku msasa.
11 İsrailli kadının oğlu RAB'be sövdü, lanet etti. Onu Musa'ya getirdiler. Annesi Dan oymağından Divri'nin kızı Şelomit'ti.
Munthu uja ananyoza dzina la Yehova ndi kulitemberera. Choncho anabwera naye kwa Mose. Dzina la amayi ake linali Selomiti, mwana wa Dibiri, wa fuko la Dani.
12 Adamı göz altına alıp RAB'bin kararını beklediler.
Anamuyika mʼndende mpaka atadziwa bwino chofuna cha Yehova.
13 RAB Musa'ya şöyle dedi:
Ndipo Yehova anawuza Mose kuti,
14 “Onu ordugahın dışına çıkar. Ettiği laneti duyan herkes elini adamın başına koysun ve bütün topluluk onu taşlasın.
“Pita naye kunja kwa msasa munthu wotembererayo. Onse amene anamumva akutemberera asanjike manja awo pamutu pake ndipo gulu lonse la anthu limugende miyala.
15 İsrail halkına de ki, ‘Kim Tanrısı'na lanet ederse günahının cezasını çekecektir.
Choncho uza Aisraeli kuti, ‘Aliyense wotemberera Mulungu wake alangidwe.
16 RAB'be söven kesinlikle öldürülecektir. Bütün topluluk onu taşlayacak. İster yerli ister yabancı olsun, RAB'be söven herkes öldürülecektir.
Aliyense wonyoza dzina la Yehova, mlendo ngakhale mbadwa, aphedwe. Gulu lonse la anthu limuponye miyala.
17 “‘Adam öldüren kesinlikle öldürülecektir.
“‘Ngati munthu wina aliyense achotsa moyo wa munthu mnzake, munthuyo ayenera kuphedwa.
18 Başkasının hayvanını öldüren, yerine bir hayvan vererek aldığı canın karşılığını canla ödeyecektir.
Aliyense wopha chiweto cha mnzake ayenera kulipira china. Moyo kulipa moyo.
19 Kim komşusunu yaralarsa, kendisine de aynı şey yapılacaktır.
Ngati munthu avulaza mnzake, nayenso amuchite zomwe wachitira mnzakeyo:
20 Kırığa karşılık kırık, göze göz, dişe diş olmak üzere, ona ne yaptıysa kendisine de aynı şey yapılacaktır.
kuthyola fupa kulipira kuthyola fupa, diso kulipira diso, dzino kulipira dzino. Monga momwe anavulazira mnzake, amuvulaze chimodzimodzinso.
21 Hayvan öldüren yerine bir hayvan verecek, adam öldüren öldürülecektir.
Aliyense wopha chiweto cha mnzake, alipire chiweto china, koma aliyense wopha munthu ayenera kuphedwa.
22 Yerli yabancı herkes için tek bir yasanız olacak. Tanrınız RAB benim.’”
Lamulo la mlendo ndi mbadwa ndi limodzi lomweli. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.’”
23 Musa bunları İsrail halkına bildirdikten sonra, halk RAB'be lanet eden adamı ordugahın dışına çıkardı ve taşlayarak öldürdü. Böylece İsrail halkı RAB'bin Musa'ya verdiği buyruğu yerine getirmiş oldu.
Pamenepo Mose anawuza Aisraeli zimenezi, ndipo iwo anatulutsira munthu wotembererayo kunja kwa msasa ndi kumugenda miyala. Aisraeli anachita zimene Yehova analamula Mose.

< Levililer 24 >