< Yeşaya 12 >

1 İsrail halkı o gün, “Ya RAB, sana şükrederiz” diyecek, “Bize öfkelenmiştin ama öfken dindi, Bizi avuttun.
Tsiku limenelo aliyense wa inu adzati: “Ndikukuyamikani, Inu Yehova; chifukwa ngakhale munandipsera mtima, mkwiyo wanu wachoka, ndipo mwanditonthoza.
2 Tanrı kurtuluşumuzdur. O'na güvenecek, yılmayacağız. Çünkü RAB gücümüz ve ezgimizdir. O kurtardı bizi.”
Zoonadi, Mulungu ndiye Mpulumutsi wanga; ndidzamudalira ndipo sindidzachita mantha. Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga; Iye wakhala chipulumutso changa.”
3 Kurtuluş pınarlarından sevinçle su alacaksınız.
Mudzakondwera popeza Yehova ali ngati chitsime cha chipulumutso chanu.
4 O gün diyeceksiniz ki, “RAB'be şükredin, O'nu adıyla çağırın, Halklara duyurun yaptıklarını, Adının yüce olduğunu duyurun!
Tsiku limenelo mudzati: “Yamikani Yehova, tamandani dzina lake; mulengeze ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu, ndipo mulalike kuti dzina lake ndi lopambana.
5 RAB'be ezgiler söyleyin, Çünkü görkemli işler yaptı. Bütün dünya bilsin bunu.
Imbirani Yehova, pakuti wachita ntchito zazikulu; zimenezi zidziwike pa dziko lonse lapansi.
6 Ey Siyon halkı, sesini yükselt, sevinçle haykır! Çünkü aranızda bulunan İsrail'in Kutsalı büyüktür.”
Fuwulani ndi kuyimba mwachimwemwe, inu anthu a ku Ziyoni; pakuti Woyerayo wa Israeli ndi wamkulu pakati panu.”

< Yeşaya 12 >