< Yasa'Nin Tekrari 13 >
1 “Aranızdan bir peygamber ya da düş gören biri çıkarsa, bir belirtiyi ya da şaşılası bir olayı önceden bildirirse,
Ngati mneneri kapena wina aliyense amene amanena zamʼtsogolo mwa maloto atuluka pakati panu, nalengeza za chizindikiro chozizwitsa kapena chodabwitsa,
2 ‘Bilmediğiniz başka ilahlara yönelip tapınalım’ derse, söz ettiği belirti, şaşılası olay gerçekleşse bile,
chinthu nʼkuchitikadi, tsono iyeyo nʼkunena kuti, “Tiyeni titsatire milungu ina, tiyeni tiyipembedze,” (kunena milungu imene simunayidziwe),
3 o peygamberi ya da düş göreni dinlememelisiniz. Tanrınız RAB kendisini bütün yüreğinizle, bütün canınızla sevip sevmediğinizi anlamak için sizi sınamaktadır.
musamumvere mneneriyo kapena wolotayo. Yehova Mulungu wanu afuna akuyeseni kuti aone ngati mumamukonda ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse.
4 Tanrınız RAB'bin ardınca yürüyün, O'ndan korkun. Buyruklarına uyun, O'nun sözüne kulak verin. O'na kulluk edin, O'na bağlı kalın.
Muyenera kutsatira Yehova Mulungu wanu, ndipo ndi Iyeyo amene muyenera kumuopa. Muzisunga malamulo ake ndi kumamumvera, muzimutumikira ndipo kumukangamira Iyeyo.
5 O peygamber ya da düş gören öldürülecek. O, sizi Mısır'dan çıkaran, köle olduğunuz ülkeden kurtaran Tanrınız RAB'be karşı gelmeye kışkırttı. Tanrınız RAB'bin yürümenizi buyurduğu yoldan sizi saptırmaya çalıştı. Aranızdaki kötülüğü ortadan kaldırmalısınız.
Mneneri kapena wolotayo ayenera kuphedwa, popeza analalikira zopandukira Yehova Mulungu wanu, amene anakutulutsani ku Igupto ndi kukupulumutsani ku dziko la ukapolo. Wolalikirayo anafuna kukupatutsani pa njira imene Yehova Mulungu wanu anakulamulirani kuti muyitsatire. Muzichotsa choyipa pakati panu.
6 “Öz kardeşin, oğlun, kızın, sevdiğin karın ya da en yakın dostun seni gizlice ayartmaya çalışır, senin ve atalarının önceden bilmediğiniz, dünyanın bir ucundan öbür ucuna dek uzakta, yakında, çevrenizde yaşayan halkların ilahları için, ‘Haydi gidelim, bu ilahlara tapalım’ derse,
Ngati mʼbale wanu weniweni kapena mwana wanu wamwamuna kapena wamkazi, kapena mkazi wanu wokondedwa, kapena mnzanu wapamtima akukakamizani mwachinsinsi, nʼkumati, “Tiyeni tipite tikapembedze milungu ina” (milungu imene inuyo kapena makolo anu sanayidziwe,
milungu ya anthu okuzungulirani, kaya ndi apafupi kapena akutali, kuchokera kumapeto mpaka kumapeto kwina kwa dziko lapansi),
8 ona uymayacak, onu dinlemeyeceksin. Ona acımayacak, sevecenlik göstermeyecek, onu korumayacaksın.
musamugonjere kapena kumumvera. Musamumvere chisoni. Musamuleke kapena kumutchinjiriza.
9 Onu kesinlikle öldüreceksin. Onu önce sen, sonra bütün halk taşa tutsun.
Mumuphe ndithu. Dzanja lanu likhale loyambirira kumupha, kenaka manja a anthu ena onse.
10 Taşlayarak öldürün onu. Çünkü Mısır'dan, köle olduğunuz ülkeden sizi çıkaran Tanrınız RAB'den sizi saptırmaya çalıştı.
Mumuponye miyala mpaka kumupha, chifukwa anafuna kukupatutsani pa njira ya Yehova Mulungu amene anakutulutsani ku Igupto, dziko la ukapolo.
11 Böylece bütün İsrail bunu duyup korkacak. Bir daha aranızda buna benzer kötü bir şey yapmayacaklar.
Tsono Aisraeli onse adzamva nachita mantha, ndipo palibe mmodzi pakati panu amene adzachitenso choyipa chotere.
12 “Tanrınız RAB'bin yaşamanız için size vereceği kentlerin birinde, içinizden kötü kişiler çıktığını ve, ‘Haydi, bilmediğiniz başka ilahlara tapalım’ diyerek kentlerinde yaşayan halkı saptırdıklarını duyarsanız,
Ngati mumvetsedwa kuti ku umodzi mwa mizinda imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti mukhalemo,
kwapezeka anthu ena oyipa pakati panu ndipo asocheretsa anthu ambiri mʼmizinda yanu, pomanena kuti, “Tiyeni tikapembedze milungu ina” (milungu imene simunayidziwe),
14 araştıracak, inceleyecek, iyice soruşturacaksınız. Duyduklarınız gerçekse ve bu iğrenç olayın aranızda yapıldığı kanıtlanırsa,
mukuyenera kufunsa, kulondola ndi kufufuza bwino nkhaniyo. Ndipo ngati zitatsimikizikadi kuti ndi zoona kuti chinthu chonyansa chotere chachitikadi pakati panu,
15 o kentte yaşayanları kesinlikle kılıçtan geçireceksiniz. Kenti yok edip orada yaşayan bütün halkı ve hayvanları kılıçtan geçireceksiniz.
muyenera kuwapha onse okhala mu mzinda umenewo. Muwonongeretu kwathunthu mzindawo, anthu ake ndi ziweto zake zomwe.
16 Yağmalanan malların tümünü toplayıp meydanın ortasına yığın. Kenti ve malları Tanrınız RAB'be tümüyle yakmalık sunu olarak yakın. Kent sonsuza dek yıkıntı halinde bırakılacak. Yeniden onarılmayacak.
Katundu yense wa anthu mu mzindawo mumuwunjike pamodzi pakatikati pa bwalo losonkhanako ndipo mutenthe mzindawo pamodzi ndi katundu wake yense monga nsembe yathunthu yopsereza ya kwa Yehova Mulungu wanu. Mzinda umenewo ukhale bwinja mpaka muyaya, usadzamangidwenso.
17 Yok edilecek mallardan hiçbir şey almayın. Böylece RAB'bin kızgın öfkesi yatışacak ve RAB atalarınıza içtiği ant uyarınca size acıyacak, sevecenlik gösterecek, sizi çoğaltacaktır.
Musapezeke ndi kanthu kalikonse koyenera kuwonongedwa kuti Yehova abweze mkwiyo wake wochititsa manthawu. Adzakuchitirani chifundo ndi kukumverani chisoni, ndipo adzakuchulukitsani monga analonjeza mwa lumbiro kwa makolo anu,
18 Çünkü Tanrınız RAB'bin sözünü dinleyeceksiniz. Böylece bugün size bildirdiğim buyruklara uyup O'nun gözünde doğru olanı yapmış olacaksınız.”
chifukwa mumamvera Yehova Mulungu wanu, kusunga malamulo ake onse amene ndikukupatsani lero lino ndi kuchita zoyenera pamaso pake.