< Jon 17 >

1 Jisu sum minro kochingbv, nw nyidomookubv kaadungto okv minto, Abu, dw v aapvku. Noogv Kuunyilo nga amina yunglit molaka, vkvlvgavbolo Kuunyilo ngvka noogv amina kaiyachok mola jidukubv.
Yesu atatha kunena izi, anayangʼana kumwamba ndipo anapemphera: “Atate, nthawi yafika. Lemekezani Mwana wanu, kuti Mwana wanuyo akulemekezeni Inu.
2 No nyiamookua rigv dubv tojupkunam ha ninyia jito, vkvlvgavbolo nw noogv jinam a bunua turbwng nvnga jidubv. (aiōnios g166)
Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. (aiōnios g166)
3 Okv turbwngnv singnam manv nam jvjvrungnv Pwknvyarnv akin vla chinam, okv Jisunyi no vngmu kunamv vla chinam. (aiōnios g166)
Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. (aiōnios g166)
4 Ngo nyiamooku so noogv amin kai nama kaatam pvkunv; noogv ritokv vla ridung jinama ngo rinya pvkunv.
Ine ndabweretsa ulemerero wanu pa dziko pamene ndamaliza ntchito imene munandipatsa kuti ndi igwire.
5 Abu! Nyia mooku ha pwklin yarlin madvbv noogv ngam amin kai dubv jinam aingbv. Vjakka no gv nvchilo ngam amin kai dubv jilabvka.
Ndipo tsopano, Atate, ndilemekezeni Ine pamaso panu ndi ulemerero uja umene ndinali nawo kwa Inu dziko lapansi lisanayambe.
6 Nyia mooku so noogv ngam jinam vdwa noogv amina ngo bunua chimupvnv. Bunu no gvngvku okv no bunua ngam jito. Bunu noogv gamchar vdwa tvvpvripvku,
“Ine ndawadziwitsa za Inu anthu amene munandipatsa mʼdziko lapansi. Iwo anali anu. Inu munawapereka kwa Ine ndipo amvera mawu anu.
7 okv vjak bunu chimpvku noogv ngam ogumvnwng jinam vdwa no gvlokv aanv ngv vla.
Tsopano akudziwa kuti zonse zimene munandipatsa nʼzochokera kwa Inu.
8 Ngo noogv jinam doin ha bunua jipvkunv, okv bunu larwksupvku; bunu ngam noogv lokv jvjvbv aanv ngv vla chindu, okv ngam no vngmu pvnv vla bunu mvnjwngdu.
Pakuti Ine ndiwapatsa mawu amene Inu munandipatsa ndipo awalandira. Iwo akudziwa ndithu kuti Ine ndinachokera kwa Inu, ndipo akukhulupirira kuti Inu ndiye amene munandituma Ine.
9 “Ngo bunugv lvgabv kumdunv. Ngo nyiamooku gv lvgabv kumma vbvritola noogv ngam jinam vdwgv lvgabv, bunu no gvbv ripvku.
Ine ndikuwapempherera. Ine sindikupempherera dziko lapansi, koma anthu amene Inu mwandipatsa, pakuti ndi anu.
10 Ngoogvlo ogugo doopvdw mvnwngngv no gvngv, okv noogv ogu mvnwngngv ngokvku; okv ngoogv amin kai nama bunugv lokv kaatam pvnv.
Zonse zimene Ine ndili nazo ndi zanu, ndipo zonse zimene Inu muli nazo ndi zanga. Choncho Ine ndalemekezedwa mwa iwowo.
11 Okv vjak ngo no gvlo chaarikunv; ngo nyiamooku so doobwng kumare, vbvritola bunu nyiamooku si doopv. Darwknv Abu! Noogv amin jwkrw lokv bunua alv dubv toryagaya laka, noogv nga amin jinam a vkvlvgavbolo bunuv akin gubv ridu kubv no la ngo oguaingbv akinpvdw vkv aingbv.
Ine sindikukhalanso mʼdziko lapansi nthawi yayitali, koma iwo akanali mʼdziko lapansi. Ine ndikubwera kwa Inu. Atate Woyera, atetezeni ndi mphamvu za dzina lanu. Dzina limene munandipatsa Ine, kuti iwo akhale amodzi monga Ife tili amodzi.
12 Bunua ngoogv lvkobv doorilo, no gv ngam amin jinam, ho gv jinam amin jwkrw lokv ngo bunua turlingalin pvkunv, Darwknv kitap lokv minam gaam hv rilin kunam lvgabv nyidum akin go ngerung jinv nga mimabv ngo bunugv lokv akin goka ngemu mato.
Pamene ndinali nawo, ndinawateteza ndi kuwasunga mosamala mʼdzina limene munandipatsa. Palibe ndi mmodzi yemwe amene anatayika kupatula yekhayo amene anayenera kuwonongeka kuti malemba akwaniritsidwe.
13 Okv vjak ngo no gvlo aariku, okv ngo nyiamooku soogv ogu ogu vdwa mindunv vkvlvga bunu gvlo ngoogv mvngpuv bunugv haapok vdwlo kaibv doolwk modubv.
“Tsopano ndikubwera kwa Inu. Ndikunena izi ndikanali mʼdziko lapansi, kuti iwo akhale ndi muyeso wodzaza wachimwemwe changa mʼkati mwawo.
14 Ngo bunua noogv doin a jipvnv, okv nyiamookuv bunua kaanwng mado, ogulvgavbolo bunu nyiamooku gvngv kuma, ngoogv nyiamooku gvngv manam apiabv.
Ine ndawapatsa mawu anu ndipo dziko lapansi likudana nawo, pakuti sali a dziko lapansi monga Ine sindilinso wa dziko lapansi.
15 Ngo bunua nyiamooku so doonv nga naarotvka vla mima, vbvritola bunua Alvmanv loka toryagaya laka vla mindunv.
Sindikupempha kuti muwachotse mʼdziko lapansi koma kuti muwateteze kwa woyipayo.
16 Ngo gv nyiamooku gvngv manam apiabv bunu nyiamooku gvngv kuma.
Iwo si a dziko lapansi, monga Ine sindilinso wa dziko lapansi.
17 Noogv gaam v jvjvrungnv; jvjvnv gaam lokv no bunua no gvbv jvjv dukubv mvsulaka.
Ayeretseni ndi choonadi chanu. Mawu anu ndiye choonadi.
18 No oguaingbv ngam nyiamooku so vngmupvdw, vkv aingbv ngo bunua nyiamooku so vngmupvnv.
Monga Inu munandituma Ine mʼdziko lapansi, Inenso ndikuwatuma mʼdziko lapansi.
19 Okv ngo bunugv lvgabv ngo atuv no gvlo tolwk sudunv, ho apiabv bunuka no gvlo jvjvbv tolwk sidukubv.”
Chifukwa cha iwowa Ine ndikudziyeretsa, kuti iwo ayeretsedwenso kwenikweni.
20 “Ngo bunu mvngchik lvgabv kumma, vbvritola bunugv doin lokv nga mvngjwngnv vdwgv lvgabvka kumdunv.
“Ine sindikupempherera iwo okhawa, komanso amene adzandikhulupirira chifukwa cha uthenga wawo.
21 Bunu mvnwngnga akin molaka vla ngo kumdunv. Abu! no ngoogvlo okv ngo no gvlo vkv aingbv bunuaka ngonu gvlo akin motoka, okv nyiamooku so gv nyi vdwv no kunyi nga vngmunv vla chindubv.
Ndikuwapempherera kuti onsewa akhale amodzi. Monga Inu Atate muli mwa Ine ndi Ine mwa Inu, iwonso akhale mwa Ife kuti dziko lapansi likhulupirire kuti Inu munandituma Ine.
22 No okv ngo oguaingbv akinpvdw, vkv aingbv bunuaka akin modubv vla, no gv jinam yunglit nama ngo bunua jipvnv.
Ine ndawapatsa ulemerero umene munandipatsa Ine, kuti akhale amodzi monga Ife tili amodzi.
23 Ngo bunu gvlo okv no ngoogvlo, vkvlvgavbolo bunu mvnwngngv akin dukubv, nyiamookuv no ngam vngmunv vla chinam lvgabv okv no gv ngam paknam apiabv bunua no pakdu kubv.”
Ine ndikhale mwa iwo ndipo Inu mwa Ine kuti umodzi wawo ukhale wangwiro. Choncho dziko lapansi lidzadziwa kuti Inu munandituma Ine ndipo Inu mwawakonda iwowa monga momwe Inu munandikondera Ine.
24 “Abu no bunuam ngam jito, okv ngo ogolo dooredw bunuaka ngoogvlo doomu nvpv mvngdu, noogv nga yunglit dubv jinama ngooka bunua ngoogv yunglit nama kaatam dukubv ogulvgavbolo nyiamookua pwklinyarlin madvbv no ngam pakpvnv.
“Atate, Ine ndikufuna kuti anthu amene mwandipatsa Ine adzakhale ndi Ine kumene kuli Ine, ndi kuona ulemerero wanga, ulemerero umene munandipatsa chifukwa Inu munandikonda dziko lapansi lisanalengedwe.
25 Daadwvrwnv Abu! Nyia mooku v nam chima vbvritola ngo nam chindu, okv si bunu no nga vngmunv vla chindu.
“Atate wolungama, ngakhale kuti dziko lapansi silikudziwani Inu, Ine ndimakudziwani, ndipo iwo amadziwa kuti Inu munandituma Ine.
26 Ngo nam bunua chimu dukubv mvpvnv, okv ngo vbvdvdvbv ribwngre, vkvlvgabv no gv ngam paknamv bunu gvlo doolwk dukubv.”
Ine ndawadziwitsa dzina lanu, ndipo ndidzapitiriza kuwadziwitsa dzina lanulo, kuti chikondi chomwe munandikonda nacho chikhale mwa iwo, ndipo Ine mwa iwo.”

< Jon 17 >