< Psaltaren 125 >
1 En vallfartssång. De som förtrösta på HERREN, de likna Sions berg, som icke vacklar, utan förbliver evinnerligen.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni, limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
2 Jerusalem omhägnas av berg, och HERREN omhägnar sitt folk, ifrån nu och till evig tid.
Monga mapiri azungulira Yerusalemu, momwemonso Yehova azungulira anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya.
3 Ty ogudaktighetens spira skall icke förbliva över de rättfärdigas arvslott, på det att de rättfärdiga ej må uträcka sina händer till orättfärdighet.
Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama, kuti anthu olungamawo angachite nawonso zoyipa.
4 Gör gott, o HERRE, mot de goda och mot dem som hava redliga hjärtan.
Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino, amene ndi olungama mtima
5 Men dem som vika av på vrånga vägar, dem rycke HERREN bort tillika med ogärningsmännen. Frid vare över Israel!
Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa. Mtendere ukhale pa Israeli.