< Jeremia 6 >

1 Bärgen edert gods ut ur Jerusalem, I Benjamins barn, stöten i basun i Tekoa, och resen upp ett högt baner ovanför Bet-Hackerem; ty en olycka hotar från norr, med stor förstöring.
“Thawani, inu anthu a ku Benjamini! Tulukani mu Yerusalemu! Lizani lipenga ku Tekowa! Kwezani mbendera ku Beti-Hakeremu! Pakuti tsoka lalikulu likubwera kuchokera kumpoto, ndipo chiwonongekocho nʼchachikulu.
2 Hon som är så fager och förklemad, dottern Sion, henne skall jag förgöra.
Kodi mzinda wa Ziyoni suli ngati msipu wokongola kwambiri, kumene abusa amafikako ndi ziweto zawo?
3 Herdar skola komma över henne med sina hjordar; de skola slå upp sina tält runt omkring henne, avbeta var och en sitt stycke.
Abusa ndi nkhosa zawo adzabwera kudzalimbana nawo; adzamanga matenti awo mowuzinga, ndipo aliyense adzakhazika anthu ake pamalo pake.”
4 Ja, invigen eder till strid mot henne. »Upp, låt oss draga åstad, medan middagsljuset varar! Ack att dagen redan lider till ända! Ack att aftonens skuggor förlängas!
Adzanena kuti, “Konzekani kuwuthira nkhondo mzindawo! Nyamukani, kuti tiwuthire nkhondo mzindawu masana ano. Koma tili ndi tsoka, dzuwa lapendeka, ndipo zithunzithunzi za kumadzulo zikunka zitalika.
5 Välan, så låt oss draga ditupp om natten och förstöra hennes palatser.»
Tsono nyamukani kuti tiwuthire nkhondo mzindawu usiku uno ndi kuwononga malinga ake!”
6 Ty så säger HERREN Sebaot: Fällen träd och kasten upp vallar emot Jerusalem. Hon är staden som skall hemsökas, hon som i sig har idel förtryck
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Dulani mitengo ndipo mumange mitumbira yankhondo kulimbana ndi Yerusalemu. Mzinda umenewu uyenera kulangidwa; wadzaza ndi kuponderezana.
7 Likasom en brunn låter vatten välla fram, så låter hon ondska framvälla. Våld och förödelse hör man där, sår och slag äro beständigt inför min åsyn.
Monga momwe chitsime chimatulutsira madzi ndi mmenenso Yerusalemu amatulutsira zoyipa zake. Chiwawa ndi chiwonongeko ndi zomwe zimamveka mu mzindamo; nthenda yake ndi mabala ake ndimaziona nthawi zonse.
8 Låt varna dig, Jerusalem, så att min själ ej vänder sig ifrån dig, så att jag icke gör dig till en ödemark, till ett obebott land.
Iwe Yerusalemu, tengapo phunziro, kuopa kuti chikondi changa pa iwe chingakuchokere ndi kusandutsa dziko lako kukhala bwinja mopanda munthu wokhalamo.”
9 Så säger HERREN Sebaot: En efterskörd, likasom på ett vinträd, skall man hålla på kvarlevan av Israel. Räck ut din hand åter och åter, såsom när man plockar av druvor från rankorna.
Yehova Wamphamvuzonse anandiwuza kuti, “Adani adzawakunkha ndithu anthu otsala a Israeli, monga momwe amachitira populula mphesa. Tsono iwe yesetsa kupulumutsa amene ungathe monga mmene amachitira munthu wokolola mphesa.”
10 Men inför vem skall jag tala och betyga för att bliva hörd? Se, deras öron äro oomskurna, så att de icke kunna höra. Ja, HERRENS ord har blivit till smälek bland dem; de hava intet behag därtill.
Kodi ndiyankhule ndi yani ndi kumuchenjeza? Ndinene mawu ochenjeza kwa yani kuti amve? Makutu awo ndi otsekeka kotero kuti sangathe kumva. Mawu a Yehova ndi onyansa kwa iwo; sasangalatsidwa nawo.
11 Därför är jag uppfylld av HERRENS vrede, jag förmår icke hålla den inne. Utgjut den över barnen på gatan och över alla de unga männens samkväm; ja, både man och kvinna skola drabbas därav, jämväl den gamle och den som har fyllt sina dagars mått.
Koma ine ndadzazidwa ndi mkwiyo wa Yehova, ndipo ndatopa ndi kusunga mkwiyo wa Yehova. Yehova anandiwuza kuti, “Tsono ndidzawutulutsira mkwiyo umenewu pa ana oyenda mʼmisewu ndi pa achinyamata amene asonkhana pamodzi; pakutinso mwamuna ndi mkazi wake adzatengedwa, pamodzi ndi okalamba amene ali ndi zaka zochuluka.
12 Och deras hus skola gå över i främmandes ägo så ock deras åkrar och deras hustrur, ty jag vill uträcka min hand mot landets inbyggare, säger HERREN.
Nyumba zawo adzazipereka kwa ena, pamodzi ndi minda yawo ndi akazi awo. Ndidzatambasula dzanja langa kukantha anthu okhala mʼdzikomo,” akutero Yehova.
13 Ty alla, både små och stora, söka där orätt vinning, och både profeter och präster fara allasammans med lögn,
“Kuyambira wamngʼono mpaka wamkulu, onse ali ndi dyera lofuna kupeza phindu mwa kuba; aneneri pamodzi ndi ansembe omwe, onse amachita zachinyengo.
14 de taga det lätt med helandet av mitt folks skada; de säga: »Allt står väl till, allt står väl till», och dock står icke allt väl till.
Amapoletsa zilonda za anthu anga pamwamba pokha. Iwo amanena kuti, ‘Mtendere, mtendere,’ pamene palibe mtendere.
15 De skola komma på skam, ty de övade styggelse. Likväl känna de alls icke någon skam och veta icke av någon blygsel. Därför skola de falla bland de andra; när min hemsökelse träffar dem, skola de komma på fall, säger HERREN,
Kodi amachita manyazi akamachita zonyansazo? Ayi, sachita manyazi ndi pangʼono pomwe; sadziwa ndi kugwetsa nkhope komwe. Choncho iwo adzagwera pakati pa anzawo amene agwa kale; adzagwa pansi tsiku limene ndidzawalange,” akutero Yehova.
16 Så sade HERREN: »Ställen eder vid vägarna och sen till, och frågen efter forntidens stigar, frågen vilken väg som är den goda vägen, och vandren på den, så skolen I finna ro för edra själar.» Men de svarade: »Vi vilja icke vandra på den.»
Yehova akuti, “Imani pa mphambano ndipo mupenye; kumeneko ndiye kuli njira zakale, funsani kumene kuli njira yabwino. Yendani mʼmenemo, ndipo mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu. Koma inu munati, ‘Ife sitidzayenda njira imeneyo.’
17 Och när jag då satte väktare över eder och sade: »Akten på basunens ljud», svarade de: »Vi vilja icke akta därpå.»
Ine ndinakupatsani alonda oti akuyangʼanireni ndipo ndinati, ‘Imvani kulira kwa lipenga!’ koma inu munati, ‘Sitidzamvera.’
18 Hören därför, I hednafolk, och märk, du menighet, vad som sker bland dem.
Nʼchifukwa chake imvani, inu anthu a mitundu ina; yangʼanitsitsani, inu amene mwasonkhana pano, chimene chidzawachitikire anthuwo.
19 Ja hör, du jord: Se, jag skall låta olycka komma över detta folk, såsom en frukt av deras anslag, eftersom de icke akta på mina ord, utan förkasta min lag.
Imvani, inu anthu okhala pa dziko lapansi, ndikubweretsa masautso pa anthu awa. Zimenezi ndi mphotho ya ntchito zawo. Iwowa sanamvere mawu anga ndipo anakana lamulo langa.
20 Vad frågar jag efter rökelse, komme den ock från Saba, eller efter bästa kalmus ifrån fjärran land? Edra brännoffer täckas mig icke, och edra slaktoffer behaga mig icke.
Kodi pali phindu lanji ngakhale mubwere ndi lubani kuchokera ku Seba, kapena zonunkhira zina kuchokera ku dziko lakutali? Nsembe zanu zopsereza Ine sindidzalandira; nsembe zanu sizindikondweretsa.”
21 Därför säger HERREN så: Se, jag skall lägga stötestenar för detta folk; och genom dem skola både fader och söner komma på fall, den ene borgaren skall förgås med den andre.
Choncho Yehova akuti, “Ndidzayika zokhumudwitsa pamaso pa anthu awa. Abambo ndi ana awo aamuna onse adzapunthwa ndi kugwa; anansi awo ndi abwenzi awo adzawonongeka.”
22 Så säger HERREN: Se, ett folk kommer från nordlandet, ett stort folk reser sig vid jordens yttersta ända.
Yehova akunena kuti, “Taonani, gulu lankhondo likubwera kuchokera kumpoto; mtundu wa anthu amphamvu wanyamuka kuchokera kumathero a dziko lapansi.
23 De föra båge och lans, de äro grymma och utan förbarmande. Dånet av dem är såsom havets brus, och på sina hästar rida de fram, rustade såsom kämpar till strid, mot dig, du dotter Sion.
Atenga mauta ndi mikondo; ndi anthu ankhanza ndi opanda chifundo. Phokoso lawo lili ngati mkokomo wa nyanja. Akwera pa akavalo awo ndipo akonzekera ngati anthu ankhondo, kudzakuthirani nkhondo anthu a ku Ziyoni.”
24 När vi höra ryktet om dem, sjunka våra händer ned, ängslan griper oss, ångest lik en barnaföderskas.
A ku Ziyoni akuti “Ife tamva mbiri yawo, ndipo manja anthu alefukiratu. Nkhawa yatigwira, ndipo tikumva ululu ngati mayi pa nthawi yake yochira.
25 Gå icke ut på marken, och vandra ej på vägen, ty fienden bär svärd; skräck från alla sidor!
Musapite ku minda kapena kuyenda mʼmisewu, pakuti mdani ali ndi lupanga, ndipo ponseponse anthu akuchita mantha.
26 Du dotter mitt folk, höll dig i sorgdräkt, vältra dig i aska, höj sorgelåt likasom efter ende sonen, och håll bitter dödsklagan; ty plötsligt kommer förhärjaren över oss.
Inu anthu anga, valani ziguduli ndipo gubudukani pa phulusa; lirani mwamphamvu ngati munthu wolirira mwana wake mmodzi yekha, pakuti mwadzidzidzi wowonongayo adzabwera kudzatipha.
27 Jag har satt dig till en proberare i mitt folk -- såväl som till ett fäste -- på det att du må lära känna och pröva deras väg.
“Iwe Yeremiya, ndakuyika kuti ukhale choyesera zitsulo. Uwayese anthu anga monga ungayesere chitsulo kuti uwone makhalidwe awo.
28 De äro allasammans avfälliga och gensträviga, de gå med förtal, de äro koppar och järn, allasammans äro de fördärvliga människor.
Onsewo ali ndi khalidwe lokanika ndi lowukira ndipo akunka nanena zamiseche. Iwo ndi olimba ngati mkuwa ndi chitsulo. Onse amangochita zoyipa zokhazokha.
29 Blåsbälgen pustar, men ur elden kommer allenast bly fram; allt luttrande är förgäves, slagget bliver ändå icke frånskilt.
Moto mu mvukuto ukuyaka kwambiri; mtovu watha kusungunuka ndi moto. Koma ntchito yosungunulayo sikupindula chifukwa zoyipa sizikuchokapo.
30 »Ett silver som må kastas bort», så kan man kalla dem, ty HERREN har förkastat dem.
Iwo ali ngati siliva wotayidwa, chifukwa Yehova wawakana.”

< Jeremia 6 >