< Nehemja 10 >
1 Men de som beseglade det, voro desse: Nehemia Thirsatha, Hachalia son, och Zedekia,
Amene anasindikiza chidindo anali awa: Nehemiya, bwanamkubwa uja, mwana wa Hakaliya. Zedekiya,
2 Seraja, Asaria, Jeremia,
Seraya, Azariya, Yeremiya
3 Pashur, Amaria, Malchija,
Pasuri, Amariya, Malikiya,
4 Hattus, Sebanja, Malluch,
Hatusi, Sebaniya, Maluki,
5 Harim, Meremoth, Obadja,
Harimu, Meremoti, Obadiya,
6 Daniel, Ginnethon, Baruch,
Danieli, Ginetoni, Baruki,
7 Mesullam, Abia, Mijamin,
Mesulamu, Abiya, Miyamini
8 Maasia, Bilgai, och Semaja: De voro Presterna.
Maziya, Biligai ndi Semaya Awa anali ansembe.
9 Men Leviterna voro: Jesua, Asanja son, Binnui af Henadads barnom, Kadmiel;
Alevi anali awa: Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa fuko la Henadadi, Kadimieli,
10 Och deras bröder, Sebanja, Hodija, Kelita, Pelaja, Hanan,
ndi abale awo awa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,
11 Micha, Rehop, Hasabia,
Mika, Rehobu, Hasabiya,
12 Saccur, Serebia, Sebanja,
Zakuri, Serebiya, Sebaniya,
13 Hodija, Bani och Beninu.
Hodiya, Bani ndi Beninu.
14 Hufvuden i folken voro: Paros, PahathMoab, Elam, Sattu, Bani,
Atsogoleri a anthu anali awa: Parosi, Pahati-Mowabu, Elamu, Zatu, Bani,
19 Hariph, Anathoth, Nebai,
Harifu, Anatoti, Nebayi,
20 Magpias, Mesullam, Hesir,
Magipiyasi, Mesulamu, Heziri
21 Mesesabeel, Zadok, Jaddua,
Mesezabeli, Zadoki, Yaduwa
22 Pelatja, Hanan, Anaja,
Pelatiya, Hanani, Ananiya,
23 Hosea, Hanania, Hasub,
Hoseya, Hananiya, Hasubu
24 Hallohes, Pilha, Sobek,
Halohesi, Piliha, Sobeki,
25 Rehum, Hasabna, Maaseja,
Rehumu, Hasabiya, Maaseya,
27 Malluch, Harim och Baana.
Maluki, Harimu ndi Baana.
28 Och det andra folket, Presterna, Leviterna, dörravaktarena, sångarena, Nethinim, och alle de som hade söndrat sig ifrå folken i landen, intill Guds lag, med sina hustrur, söner och döttrar, alle de som det kunde förstå;
Ife otsalafe, ndiye kuti ansembe, Alevi, alonda a ku Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu, onse amene anadzipatula pakati pa anthu a mitundu ina kuti atsate malamulo a Yehova, pamodzi ndi akazi athu, ana athu ndi onse amene ali ndi nzeru,
29 Och deras mägtige, togo sig det till för sina bröder, och de kommo till att svärja och förpligta sig med ed, till att vandra i Guds lag, som igenom Guds tjenare Mose gifven är, att de hålla och göra ville efter all Herrans vår Guds bud, rätter och seder;
tikuphatikana ndi abale athu wolemekezeka, ndipo tikulonjeza molumbira kuti tidzayenda motsata malamulo a Mulungu amene anapereka kudzera mwa Mose mtumiki wa Mulungu. Tilonjeza kumvera ndi kutsata bwino mawu onse, miyambo yonse ndi malangizo onse a Yehova. Yehova atilange ngati sitidzachita zimenezi.
30 Och att vi icke skulle gifva folken i landena våra döttrar; ej heller vårom sönom taga deras döttrar.
“Ife tikulonjeza kuti sitidzapereka ana athu aakazi kuti akwatiwe ndi amuna a mayiko ena kapena kutenga ana awo aakazi kuti akwatiwe ndi ana athu aamuna.
31 Desslikes, när folket i landet förer om Sabbathsdagen någon varo och allahanda spisning, till att sälja, att vi icke ville taga det af dem om Sabbathen och helgedagar; och att vi i sjunde årena ville göra förlösning på allahanda tunga;
“Ngati anthu a mitundu ina abwera ndi zinthu za malonda, monga tirigu, kudzagulitsa pa tsiku la Sabata, sitidzawagula pa tsiku la Sabata kapena pa tsiku lina lililonse loyera. Pa chaka chilichonse cha chisanu ndi chiwiri tidzagoneka munda wosawulima ndipo tidzafafaniza ngongole zonse.
32 Och lägga ett bud uppå oss, att vi årliga gifva skulle en tridiung af en sikel silfver, till tjensten i vår Guds hus;
“Tikulonjezanso molumbira kuti chaka ndi chaka tizipereka magalamu anayi a siliva kuti zithandize ntchito ya ku Nyumba ya Mulungu wathu.
33 Nämliga till skådobröd, till dagligit spisoffer, till dagligit bränneoffer, på Sabbaths, nymånads och högtidsdagom, och till det helgada, och till syndoffer, der Israel skulle med försonad varda, och till all verk i vår Guds hus.
Ndalamayi izithandiza kulipirira buledi wa pa tebulo, chopereka cha chakudya cha nthawi zonse, zopereka zopsereza za nthawi zonse, zopereka za pa tsiku la Sabata, za pachikondwerero cha Mwezi Watsopano, za pa masiku a chikondwerero osankhika, zopereka za zinthu zopatulika, zopereka za nsembe yopepesera machimo a Aisraeli ndi ntchito ina iliyonse ya ku Nyumba ya Mulungu.
34 Och vi kastade lott emellan Presterna, Leviterna och folket, om vedoffer, det man till vår Guds hus årliga framföra skulle, efter våra fäders hus, på bestämd tid, att bränna på Herrans vår Guds altare, såsom det i lagen skrifvet är;
“Ife ansembe, Alevi ndi anthu onse, tachita maere kuti tidziwe pamene banja lathu lililonse lidzabweretsa ku nyumba ya Mulungu wathu pa nthawi yoyikika ya chaka zopereka za nkhuni zoyaka pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wathu, monga momwe zinalembedwera mʼMalamulo.”
35 Och till att årliga frambära förstlingen af vårt land, och förstlingen af allo frukt, af all trä till Herrans hus;
“Tilonjezanso kuti tidzabwera ndi zipatso zoyamba kucha za mʼminda yathu ndi zipatso zoyamba kucha za mtengo uliwonse wa zipatso chaka ndi chaka kuti tidzapereke ku Nyumba ya Mulungu wathu.”
36 Och förstlingen af våra söner, och af vår boskap, såsom det i lagen skrifvet står; och förstlingen af vårt fä, och af vår får, att vi allt detta skulle hafva in uti vår Guds hus till Presterna, som i vår Guds hus tjena;
“Tidzabweranso nawo ku Nyumba ya Mulungu, kwa ansembe amene amatumikira ku Nyumba ya Mulungu ana athu aamuna oyamba kubadwa ndi ana angʼombe oyamba kubadwa monga zalembedwera mu Malamulo. Tidzaperekanso ana oyamba kubadwa a ziweto zathu ndi ana ankhosa oyamba kubadwa.”
37 Och att vi ville frambära förstlingen af vår deg, och vårt häfoffer, och frukt af allahanda trä, vin och oljo, till Presterna, i kistorna vid vår Guds hus; och vårt lands tiond till Leviterna, så att Leviterna skulle hafva tionden i alla städer, der vårt åkerverk är.
“Ndiponso ku zipinda za Nyumba ya Mulungu wathu, kwa ansembe tidzaperekanso mtanda wathu wa buledi wa ufa ndi mphatso zina monga zipatso za mtengo uliwonse, vinyo ndi mafuta. Tidzaperekanso kwa alevi chakhumi cha mbewu zathu pakuti alevi ndiwo amasonkhanitsa chakhumi mʼmidzi yathu yonse.
38 Och Presten Aarons son skall ock del hafva af Leviternas tiond, med Leviterna; så att Leviterna skola bära tionden af sine tiond upp till vår Guds hus, i kistorna, uti skatthuset.
Wansembe, mdzukulu wa Aaroni azikhala pamodzi ndi Alevi pamene akulandira chakhumi. Ndipo Alevi azibwera ndi chakhumicho ku nyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda zosungiramo chuma.”
39 Ty Israels barn, och Levi barn, skola bära häfoffret af säd, vin och oljo, upp i kistorna. Dersammastäds äro helgedomens kärile, och Presterna, som der tjena, och dörravaktare, och sångare; att vi vår Guds hus icke öfvergifve.
Choncho Israeli, kuphatikiza zidzukulu za Alevi, azipititsa zopereka za tirigu, vinyo ndi mafuta ku zipinda zosungiramo katundu wopatulika, komanso kokhala ansembe amene akutumikira pamodzi ndi alonda a ku Nyumba ya Mulungu ndi anthu oyimba nyimbo. “Kwambiri ife sitidzaleka kusamala Nyumba ya Mulungu.”