< Josua 4 >

1 Och Herren sade till Josua:
Anthu onse atatha kuwoloka Yorodani, Yehova anati kwa Yoswa,
2 Tager eder tolf män, utaf hvart slägtet en;
“Sankha amuna khumi ndi awiri, mmodzi pa fuko lililonse.
3 Och bjuder dem, och säger: Lyfter upp utur Jordan tolf stenar, af det rummet der Presternas fötter stilla stå, och hafver dem öfver med eder, att I lefven dem i lägrena, der I eder i denna nattene lägren.
Tsono uwalamule kuti, ‘Tengani miyala khumi ndi iwiri pakati penipeni pa mtsinje wa Yorodani, pamalo pamene ansembe anayimirirapo. Miyalayo muwoloke nayo ndi kudzayitula pamalo pamene mukagone usiku uno.’”
4 Då kallade Josua tolf män, som tillskickade voro af Israels barn, utaf hvart slägte en;
Choncho Yoswa anayitana amuna khumi ndi awiri amene anawasankha aja kuchokera pakati pa Aisraeli, mmodzi pa fuko lililonse,
5 Och sade till dem: Går fram för Herrans edars Guds ark midt i Jordan, och hvar lyfte en sten på sina axlar, efter talet af Israels barnas slägter;
ndipo anawawuza kuti, “Lowani pakati pa mtsinje wa Yorodani, patsogolo pa Bokosi la Yehova Mulungu wanu. Ndipo aliyense wa inu atenge mwala pa phewa lake, monga mwa chiwerengero cha mafuko a Aisraeli,
6 Att de skola vara ett tecken ibland eder, när edor barn i framtiden fråga sina fäder, och säga: Hvad göra desse stenarna här?
kuti ikhale chizindikiro kwa inu. Mʼtsogolo muno ana anu akamadzakufunsani kuti, ‘Kodi miyala iyi ikutanthauza chiyani?’
7 Att I då mågen säga dem, huru Jordans vatten sig åtskiljde för Herrans förbunds ark, då han gick genom Jordan; så att desse stenarna skola vara Israels barnom till en evig åminnelse.
Muzidzawawuza kuti, ‘Madzi a Yorodani analeka kuyenda pamene Bokosi la Chipangano la Yehova linkawoloka mtsinjewo. Miyala iyi idzakhala chikumbutso kwa anthu a Israeli kwa muyaya.’”
8 Då gjorde Israels barn såsom Josua böd dem; och båro tolf stenar midt utur Jordan, såsom Herren hade sagt Josua, efter talet af Israels barnas slägte; och båro dem med sig till det rummet, der de lägrade sig, och der lade de dem.
Aisraeli anachitadi monga Yoswa anawalamulira. Iwo ananyamula miyala khumi ndi iwiri kuchokera pakati pa Yorodani, fuko lililonse la Israeli mwala wake, monga Yehova analamulira Yoswa. Miyalayo anapita nayo ku misasa yawo nakayikhazika kumeneko.
9 Och Josua reste upp tolf stenar midt i Jordan, der Presternas fötter ståndit hade, som förbundsens ark båro, och de äro der ännu intill denna dag.
Yoswa anayimika miyala khumi ndi iwiri imene inali pakati pa Yorodani pamalo pamene ansembe onyamula Bokosi la Chipangano anayimapo. Ndipo miyalayo ili pamalo pomwepo mpaka lero lino.
10 Ty Presterna, som arken båro, stodo midt i Jordan, tilldess allt bestäldt vardt, som Herren böd Josua säga folkena, och Mose Josua budit hade; och folket skyndade sig, och gick öfver.
Ansembe onyamula Bokosi lija anayimirirabe pakati pa Yorodani mpaka zonse zimene Yehova analamulira Yoswa kuti awuze anthu zinatha. Zimenezi zinali monga momwe Mose anamufotokozera Yoswa. Tsono anthu anawoloka mtsinjewo mofulumira.
11 Då nu folket allt öfvergånget var, så gick ock Herrans ark öfver, och Presterna för folket.
Anthu atatha kuwoloka, ansembe anatsogolera anthuwo atanyamula Bokosi la Yehova.
12 Och de Rubeniter, och de Gaditer, och den halfva Manasse slägt, gingo väpnade för Israels barnom, såsom Mose dem sagt hade;
Anthu a fuko la Rubeni, Gadi ndi theka la fuko la Manase anawoloka patsogolo pa Aisraeli ali ndi zida, monga momwe Mose anawalamulira.
13 Vid fyratiotusend väpnade till härs gingo för Herranom till strids på Jericho mark.
Asilikali pafupifupi 40,000 anawoloka napita kukayima mʼchigwa cha Yeriko kukonzekera nkhondo.
14 På den dagen gjorde Herren Josua stor för hela Israel; och de fruktade honom, såsom de fruktade Mose, medan han lefde.
Zimene Yehova anachita tsiku limeneli zinapatsa anthu mtima wolemekeza Yoswa. Ndipo anamulemekeza masiku onse a moyo wake, monga momwe analemekezera Mose.
15 Och Herren sade till Josua:
Kenaka Yehova anati kwa Yoswa,
16 Bjud Presterna, som bära vittnesbördsens ark, att de träda upp utur Jordan.
“Lamula ansembe onyamula Bokosi la Chipanganowo kuti atuluke mu Yorodani.”
17 Alltså böd Josua Prestomen, och sade: Stiger upp utur Jordan.
Choncho Yoswa anawalamuladi ansembe aja kuti atuluke mu Yorodani muja.
18 Och då Presterna, som Herrans förbunds ark båro, stego upp utur Jordan, och trädde med deras fotbjelle på torra landet, kom Jordans vatten återigen i sin stad, och flöt såsom tillförene till alla sina brädder.
Ansembe onyamula Bokosi la Chipangano la Yehova aja atangotuluka mu mtsinje muja nʼkuponda powuma, madzi a mu Yorodani anayambanso kuyenda ngati poyamba mpaka kumasefukira.
19 Och det var den tionde dagen i den första månadenom, då folket uppsteg utur Jordan, och lägrade sig i Gilgal, östan för Jericho.
Aisraeli anawoloka Yorodani tsiku lakhumi la mwezi woyamba ndipo anakamanga misasa yawo ku Giligala mbali ya kummawa kwa Yeriko.
20 Och de tolf stenar, som de utur Jordan tagit hade, reste Josua upp i Gilgal;
Ku Giligala, Yoswa anayimikako miyala khumi ndi iwiri imene anayitenga mu Yorodani ija.
21 Och sade till Israels barn: När nu i framtiden edor barn fråga sina fäder, och säga: Hvad skola desse stenarna?
Ndipo iye anati kwa Aisraeli, “Mʼtsogolo muno pamene adzukulu anu adzafunsa makolo awo kuti, ‘Kodi miyala iyi ikutanthauza chiyani?’
22 Så skolen I undervisa dem, och säga: Israel gick torr igenom Jordan,
Muzidzawawuza kuti, ‘Aisraeli anawoloka Yorodani pansi pali powuma.’
23 Då Herren edar Gud förtorkade Jordans vatten för eder, så länge I gingen deröfver, lika som Herren edar Gud gjorde i röda hafvet, hvilket han torrt gjorde för oss, så att vi ginge derigenom;
Pakuti Yehova Mulungu wanu ndiye anawumitsa Yorodani pamaso panu mpaka inu mutawoloka. Yehova Mulungu wanu anaphwetsa madzi a Yorodani monga mmene anachitira ndi Nyanja Yofiira mpaka ife tinawoloka powuma.
24 På det all folk på jordene skola känna Herrans hand, huru mägtig hon är; och att I skolen frukta Herran edar Gud alltid.
Iye anachita zimenezi kuti anthu onse pa dziko lapansi adziwe kuti dzanja la Yehova ndi lamphamvu, ndi kuti inu muziopa Yehova Mulungu wanu masiku onse.”

< Josua 4 >