< Job 34 >

1 Och Elihu svarade, och sade:
Pamenepo Elihu anapitiriza kuyankhula kuti,
2 Hörer, I vise, mitt tal, och I förståndige, akter på mig;
“Imvani mawu anga, inu anthu anzeru; tcherani khutu inu anthu ophunzira.
3 Ty örat pröfvar talet, och munnen smakar maten.
Pakuti khutu limayesa mawu monga momwe mʼkamwa mumalawira chakudya.
4 Låt oss utvälja en dom, att vi måge emellan oss känna hvad godt är.
Tsono tiyeni tizindikire chomwe chili choyenera; tiphunzire pamodzi chomwe chili chabwino.
5 Ty Job hafver sagt: Jag är rättfärdig, och Gud hafver förvägrat mig min rätt.
“Yobu akunena kuti, ‘Ndine wosalakwa, koma Mulungu akukana kundiweruza molungama.
6 Jag måste ljuga, om jag än rätt hade; jag varder plågad af min skott, om jag än det intet förskyllat hade.
Ngakhale ndine wolungama mtima, akundiyesa wabodza; ngakhale ndine wosachimwa, mivi yake ikundichititsa mabala osachiritsidwa.’
7 Ho är en sådana, som Job; som gabberi dricker såsom vatten,
Kodi munthu wofanana ndi Yobu ndani, amene amayankhula zamwano ngati akumwa madzi?
8 Och går på vägenom med illgerningsmän, så att han vandrar med ogudaktiga män?
Iye amayenda ndi anthu ochita zoyipa; amayanjana ndi anthu oyipa mtima.
9 Ty han hafver sagt: Om än någor rätt färdig vore, så gäller han dock intet när Gudi.
Paja iye amanena kuti, ‘Munthu sapindula kanthu poyesetsa kukondweretsa Mulungu.’
10 Hörer mig, I vise män: Bort det, att Gud skulle vara ogudaktig, och den Allsmägtige orättvis;
“Tsono mverani ine, inu anthu anzeru zomvetsa zinthu. Mulungu sangachite choyipa ndi pangʼono pomwe, Wamphamvuzonse sangathe kuchita cholakwa.
11 Utan han lönar menniskone, efter som hon hafver förtjent; och drabbar uppå hvar och en efter hans gerningar.
Iye amamubwezera munthu molingana ndi ntchito zake; Mulungu amabweretsa pa munthu molingana ndi zomwe amachita.
12 Utan tvifvel, Gud fördömer ingen med orätt, och den Allsmägtige böjer icke rätten.
Nʼchosayembekezeka kuti Mulungu achite cholakwa, kuti Wamphamvuzonse apotoze chilungamo.
13 Ho hafver skickat det uppå jordene är, och ho hafver satt hela jordenes krets?
Kodi anapatsa Mulungu udindo wolamulira dziko lapansi ndani? Ndani anayika Mulungu kuti azilamulira dziko lonse?
14 Om han det toge sig före, kunde han allas anda och lif till sig samla;
Mulungu akanakhala ndi maganizo oti achotse mzimu wake ndi mpweya wake,
15 Allt kött vorde tillhopa förgåendes, och menniskan vorde åter till asko igen.
zamoyo zonse zikanawonongekeratu ndipo munthu akanabwerera ku fumbi.
16 Hafver du förstånd, så hör detta, och gif akt på mins tals röst.
“Ngati ndinu omvetsa zinthu, imvani izi; mvetserani zimene ndikunena.
17 Skulle någon fördenskull tvinga rätten, att han hatar honom? Och derföre att du stolt äst, skulle du fördenskull fördöma den rättfärdiga?
Kodi Mulungu wodana ndi chilungamo angathe kukhala wolamulira? Kodi iwe ungathe kuweruza Wolungama ndi Wamphamvuyo?
18 Skulle någor säga till Konungen: Du Belial? och till Förstarna: I ogudaktige?
Kodi si Iye amene amanena kwa mafumu kuti, ‘Ndinu opanda pake,’ ndipo amawuza anthu otchuka, ‘Ndinu oyipa,’
19 Den dock icke ser på Förstarnas person, och känner icke mer den härliga än den fattiga; förty de äro alle hans handaverk.
Iye sakondera akalonga ndipo salemekeza anthu olemera kupambana osauka, pakuti onsewa ndi ntchito ya manja ake?
20 Med hast måste menniskorna dö, och om midnattstid förskräckas och förgås; de mägtige varda kraftlöse borttagne.
Iwo amafa mwadzidzidzi, pakati pa usiku; anthu amachita mantha ndipo amamwalira; munthu wamphamvu amachotsedwa popanda dzanja la munthu.
21 Ty hans ögon se uppå hvars och ens vägar, och han skådar alla deras gånger.
“Maso a Mulungu amapenya njira za munthu; amaona mayendedwe ake onse.
22 Intet mörker eller skygd är, att ogerningsmän måga sig der fördölja;
Palibe malo obisika kapena a mdima wandiweyani kumene anthu ochita zoyipa angabisaleko.
23 Ty det varder ingom tillstadt, att han kommer med Gud till rätta.
Mulungu sasowa kuti apitirizebe kufufuza munthu, kuti abwere pamaso pake kudzaweruzidwa.
24 Han förgör många stolta, som icke stå till att räkna; och sätter andra i deras stad;
Popanda kufufuza, Iye amawononga anthu amphamvu ndipo mʼmalo mwawo amayikamo ena.
25 Derföre, att han känner deras gerningar; och omstörter dem om nattena, att de skola sönderkrossade varda.
Pakuti Iyeyo amadziwa bwino ntchito zawo amawagubuduza usiku ndipo amatswanyika.
26 Han kastar de ogudaktiga uti en hop, der man gerna ser det;
Iye amawalanga chifukwa cha kuyipa kwawo, pamalo pamene aliyense akuwaona;
27 Derföre, att de icke hafva följt honom efter, och förstodo ingen af hans vägar;
Chifukwa anasiya kumutsata ndipo sasamaliranso njira zake zonse.
28 Att de fattigas rop skulle komma inför honom, och han dens eländas rop höra måtte.
Anachititsa amphawi kuti kulira kwawo kufike pamaso pake, kotero Iyeyo anamva kulira kwa amphawiwo.
29 Om han frid gifver, ho vill fördöma? Och om han förskyler anletet, ho vill se uppå honom ibland folken och menniskorna?
Koma ngati Mulungu akhala chete, ndani angamunene kuti walakwa? Akabisa nkhope yake, ndani angathe kumupenyabe? Komatu ndiye amene amayangʼana za munthu komanso mtundu wa anthu,
30 Så låter han nu en skrymtare regera, till att plåga folket.
kuti asalamuliridwe ndi anthu osapembedza, kuti asatchere anthu misampha.
31 För Guds skull vill jag lida talet, och icke förmenat.
“Mwina munthu atanena kwa Mulungu kuti, ‘Ndine wolakwa koma sindidzachimwanso,
32 Hafver jag icke drabbat rätt, lär du mig bättre; hafver jag orätt handlat, vill jag icke göra så mer.
ndiphunzitseni zimene sindikuziona ngati ndachita choyipa, sindidzachitanso.’
33 Man vänter nu svar af dig; ty du förkastar all ting, och du hafver begynt det, och icke jag. Vetst du nu något, så tala.
Kodi Mulungu akuweruzeni potsata mmene inuyo mukuganizira, pamene inu mukukana kulapa? Chisankho nʼchanu, osati changa; tsono ndiwuzeni zomwe mukudziwa.
34 Visa män låter jag väl tala, och en vis man hörer mig.
“Anthu omvetsa zinthu adzakambirana, anthu anzeru amene akundimva adzandiwuza kuti,
35 Men Job talar ovisliga, och hans ord äro icke vis.
‘Yobu akuyankhula mopanda nzeru; mawu ake ndi opanda fundo.’
36 Min Fader, låt Job försökt varda allt intill ändan, derföre att han vänder sig till orättfärdiga menniskor.
Aa, kunali bwino Yobu akanayesedwa mpaka kumapeto chifukwa choyankha ngati munthu woyipa!
37 Han hafver utöfver sina synd ännu dertill hädat; derföre låt honom inför oss slagen varda; och träte sedan med sinom ordom inför Gud.
Pa tchimo lake amawonjezerapo kuwukira; amawomba mʼmanja mwake monyoza pakati pathu, ndipo amachulukitsa mawu otsutsana ndi Mulungu.”

< Job 34 >