< Jesaja 65 >

1 Jag varder sökt af dem som intet efter mig frågade; jag varder funnen af dem som intet sökte mig; och till Hedningarna, som mitt Namn intet åkallade, säger jag: Här är jag, här är jag.
“Ndinali wokonzeka kumva mapemphero a amene sankandipempha kanthu; ndipo ndinalola kuti anthu amene ankandifunafuna kuti andipeze. Kwa mtundu wa anthu umene sunkapempha chithandizo kwa Ine, ndinati, ‘Ine ndili pano, Ine ndili pano.’
2 Ty jag uträcker mina händer hela dagen till ett ohörsamt folk, som efter sina tankar vandrar på den väg, som intet god är.
Tsiku lonse ndatambasulira manja anga anthu owukira aja, amene amachita zoyipa, natsatira zokhumba zawo.
3 Ett folk, som mig förtörnar, är alltid för mitt ansigte; offrar i örtagårdom, och röker på tegelstenar;
Ndatambasulira manja anga anthu aja amene nthawi zonse amandikwiyitsa mopanda manyazi. Iwo amapereka nsembe mʼminda ndi kufukiza lubani pa maguwa ansembe a njerwa.
4 Bor ibland grifter, och håller sig uti kulor; äta svinakött, och hafva förbudet såd uti deras grytor;
Amakatandala ku manda ndipo amakachezera usiku wonse kumalo obisika. Amadya nyama ya nkhumba, ndipo mʼmiphika mwawo muli msunzi wa nyama yodetsedwa.
5 Och säga: Blif hemma, och kom intet vid mig; ty jag skall helga dig. Desse skola varda en rök i mine vrede, en eld, som brinner hela dagen.
Amawuza ena kuti, ‘Khala patali usandiyandikire, chifukwa ungatengere kupatulika kwanga!’ Ukali wanga pa anthu otere uli ngati utsi mphuno zanga, ngati moto umene umayaka tsiku lonse.
6 Si, det står skrifvet för mig: Jag vill icke tiga, utan betala; ja, jag vill betala dem i deras sköt;
“Taonani, ndatsimikiza kale mlandu ndi chilango chawo; sindidzakhala chete koma ndidzawalanga kwathunthu chifukwa cha machimo awo
7 Både deras missgerningar, och deras fäders missgerningar tillsammans, säger Herren; de som på bergen rökt, och mig på högarna försmädat hafva; jag skall mäta dem deras förra väsende uti deras sköt.
ndi a makolo awo,” akutero Yehova. “Chifukwa anapereka nsembe zopsereza pa mapiri ndi kundinyoza Ine pa zitunda zawo, Ine ndidzawalanga kwathunthu potsata zimene anachita kale.”
8 Så säger Herren: Likasom då man must finner uti vindrufvone, och säger: Förderfva det icke, ty der är en välsignelse uti; alltså vill jag för mina tjenares skull göra, att jag icke förderfvar det allt;
Yehova akuti, “Pamene madzi akanapezeka mu phava la mphesa ndipo anthu amati, ‘Musawononge phavalo, popeza madzi ena abwino akanalimobe mʼphavalo,’ Inenso chifukwa cha mtumiki wanga; sindidzawononga onse.
9 Utan vill låta växa utaf Jacob säd, och af Juda den som mitt berg besitta skall; ty mine utkorade skola besitta det, och mine tjenare skola der bo.
Ndidzatulutsa zidzukulu mʼbanja la Yakobo, ndipo a banja la Yuda adzalandira mapiri anga ngati cholowa chawo. Anthu anga osankhidwa adzalandira zimenezi, ndipo atumiki anga adzakhala kumeneko.
10 Och Saron skall vara ett hus för hjordar, och Achors dal skall ett fälägre varda, mino folke som mig söka.
Chigwa cha Saroni chidzakhala kodyetserako nkhosa, ndipo chigwa cha Akori chidzakhala malo opumirako ngʼombe kwa anthu anga ondifunafuna Ine.
11 Men I som Herran förlåten, och mitt helga berg förgäten, och uppresen till Gad ett bord, och skänken fullt in af drickoffer för Meni;
“Koma inu amene mumasiya Yehova ndi kuyiwala phiri langa lopatulika, amene munamukonzera Gadi chakudya ndi kuthirira Meni chakumwa,
12 Nu väl, jag vill uträkna eder till svärd, så att I alla måsten bocka eder till slagtning; derföre, att jag kallade, och I svaraden intet; jag talade, och I hörden intet, utan gjorden det mig misstyckte, och utvalden det mig intet täckt var.
ndidzakuperekani ku lupanga ngati nsembe, ndipo nonse mudzaphedwa; chifukwa simunayankhe pamene ndinakuyitanani, ndinayankhula koma simunamvere. Munachita zoyipa pamaso panga ndipo munasankha kuchita zoyipa zomwe sindikondwera nazo.”
13 Derföre säger Herren Herren alltså: Si, mine tjenare skola äta; men I skolen hungra; Si, mine tjenare skola dricka, men I skolen törsta; si, mine tjenare skola glade vara, men I skolen till skam varda;
Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti, “Atumiki anga adzadya, koma inu mudzakhala ndi njala; atumiki anga adzamwa, koma inu mudzakhala ndi ludzu; atumiki anga adzakondwa, koma inu mudzakhala ndi manyazi.
14 Si, mine tjenare skola fröjda sig för godt mods skull; men I skolen för hjertans sorgs skull ropa, och för jämmer gråta;
Atumiki anga adzayimba mosangalala, koma inu mudzalira kwambiri chifukwa chovutika mu mtima ndipo mudzalira mofuwula chifukwa mudzamva kuwawa mu mtima.
15 Och skolen låta edor namn minom utkoradom till ett svärjande: och Herren Herren skall döda dig, och nämna sina tjenare med ett annat namn;
Anthu anga osankhidwa adzatchula dzina lanu potemberera. Ambuye Yehova adzakuphani, koma atumiki ake adzawapatsa dzina lina.
16 Så att den som sig välsignar på jordene, han skall välsigna sig uti den rätta Guden; och den som svär på jordene, han skall svärja vid den rätta Guden; ty de förra bedröfvelser äro förgätne, och äro förskyld för min ögon.
Aliyense wopempha dalitso mʼdzikomo adzachita zimenezo kwa Mulungu woona; ndipo aliyense wochita malumbiro mʼdzikomo adzalumbira mwa Mulungu woona. Pakuti mavuto akale adzayiwalika ndipo adzachotsedwa pamaso panga.
17 Ty si, jag vill skapa en ny himmel, och ena nya jord; så att man intet mer skall komma den förra, ihåg, eller lägga dem på hjertat;
“Taonani, ndikulenga mlengalenga mwatsopano ndi dziko lapansi latsopano. Zinthu zakale sizidzakumbukika, zidzayiwalika kotheratu.
18 Utan de skola fröjda sig evinnerliga, och glade vara öfver det som jag skapar; ty si, jag vill skapa Jerusalem till fröjd, och dess folk till glädje.
Koma inu mukhale osangalala ndi okondwa mpaka muyaya chifukwa cha zimene ndikulenga, pakuti ndikulenga Yerusalemu kukhala malo wosangalatsa ndipo anthu ake adzakhala achimwemwe.
19 Och jag vill glad vara öfver Jerusalem, och fröjda mig öfver mitt folk; och gråtoröst eller klagoröst skall icke mer derinne hörd varda.
Ine ndidzakondwa chifuwa cha Yerusalemu ndipo ndidzasangalala chifukwa cha anthu anga. Kumeneko sikudzamvekanso kulira ndi mfuwu wodandaula.
20 Der skola icke mer vara barn, som icke räcka till deras dagar, eller gamle som deras år icke uppfylla; utan hundradeåra barn skola dö, och de hundradeåra syndare skola förbannade varda.
“Ana sadzafa ali akhanda ndipo nkhalamba zonse zidzakwaniritsa zaka zawo zonse. Wamngʼono mwa iwo adzafa ali ndi zaka 100. Amene adzalephere kufika zaka 100 adzatengedwa kukhala wotembereredwa.
21 De skola bygga hus, och bo deruti; de skola plantera vingårdar, och äta fruktena af dem.
Anthu adzamanga nyumba ndi kukhalamo, adzadzala mpesa ndipo adzadya zipatso zake.
22 De skola icke bygga, att en annar bor deruti, och icke plantera, att en annar äter; ty mins folks dagar skola vara såsom ett träs dagar, och deras händers verk skall föråldras när mina utkorade.
Sadzamanganso nyumba anthu ena nʼkukhalamo, kapena kudzala ndi ena nʼkudya. Pakuti anthu anga adzakhala ndi moyo wautali ngati mitengo. Osankhidwa anga adzakondwera ndi ntchito ya manja awo nthawi yayitali.
23 De skola icke arbeta fåfängt, eller föda otidiga födslo; ty de äro Herrans välsignadas säd, och deras efterkommande med dem.
Sadzagwira ntchito pachabe kapena kubereka ana kuti aone tsoka; chifukwa adzakhala anthu odalitsidwa ndi Yehova, iwowo pamodzi ndi adzukulu awo omwe.
24 Och skall ske, att förr än de ropa, vill jag svara; medan de ännu tala, vill jag höra.
Ndidzawayankha ngakhale asanathe nʼkupempha komwe. Pamene akuyankhula kumene Ine ndidzakhala nditamva kale.
25 Ulfven och lambet skola gå i bet tillsamman; lejonet skall äta strå, såsom ett nöt, och ormen skall äta jord; de skola ingen skada eller förderf göra på hela mitt helga berg, säger Herren.
Mʼmbulu ndi mwana wankhosa wamkazi zidzadyera pamodzi. Mkango udzadya udzu monga ngʼombe, koma fumbi ndiye chidzakhale chakudya cha njoka. Pa phiri langa lopatulika sipadzakhala chinthu chopweteka kapena chowononga,” akutero Yehova.

< Jesaja 65 >