< 1 Krönikeboken 9 >

1 Och hele Israel vardt räknad, och si, de äro uppskrifne i Israels och Juda Konungars bok, och nu bortförde till Babel för sina missgerningars skull;
Aisraeli onse analembedwa potsata mibado yawo mʼbuku la mafumu a Aisraeli. Anthu a ku Yuda anatengedwa kunka ku ukapolo ku Babuloni chifukwa cha kusakhulupirika kwawo.
2 De som tillförene bodde på sina ägor och städer, nämliga Israel, Prester, Leviter och de Nethinim.
Tsono anthu oyamba kukhala mʼmadera awo anali Aisraeli wamba, ansembe, Alevi ndi otumikira ku Nyumba ya Yehova.
3 Men i Jerusalem bodde någre af Juda barn, någre af BenJamins barn, någre af Ephraims och Manasse barn;
Anthu a ku Yuda, Benjamini ndi Efereimu ndiponso Manase amene anakhala mu Yerusalemu anali awa:
4 Nämliga utaf Perez barn, Juda sons, var Athai, Ammihuds son, Omri sons, Imri sons, Bani sons;
Utai mwana wa Amihudi, mwana wa Omuri, mwana wa Imuri, mwana wa Bani, chidzukulu cha Perezi mwana wa Yuda.
5 Men af Siloni, Asaja förste sonen, och hans andre söner.
A banja la Siloni: Asaya mwana wake woyamba pamodzi ndi ana ake.
6 Af Serahs barn, Jeguel och deras bröder, sexhundrad och niotio.
A banja la Zera: Yeueli. Anthu ochokera ku Yuda analipo 690.
7 Af BenJamins barn, Sallu, Mesullams son, Hodavia sons, Hassenua sons,
A fuko la Benjamini: Salu mwana wa Mesulamu, mwana wa Hodaviya, mwana wa Hasenuya;
8 Och Jibneja, Jerohams son. Och Ela, Ussi son, Michri sons, och Mesullam, Sephatia son, Reguels sons, Jibneja sons;
Ibineya mwana wa Yerohamu; Ela mwana wa Uzi, mwana wa Mikiri; ndi Mesulamu mwana wa Sefatiya, mwana wa Reueli mwana wa Ibiniya.
9 Dertill deras bröder uti deras ätter, niohundrad och sex och femtio. Alle desse männerna voro höfvitsmän för fäderna uti deras fäders hus.
Anthu ochokera ku Benjamini monga analembedwera mwa mibado yawo, analipo 956. Anthu onsewa anali atsogoleri a mabanja awo.
10 Af Presterna, Jedaja, Jojarib, Jachin;
Ansembe: Yedaya, Yehoyaribu; Yakini;
11 Och Asaria, Hilkia son, Mesullams sons, Zadoks sons, Merajoths sons, Ahitobs sons, en Förste i Guds hus;
Azariya mwana wa Hilikiya, mwana wa Mesulamu, mwana wa Zadoki mwana wa Merayoti, mwana wa Ahitubi, wamkulu woyangʼanira Nyumba ya Mulungu;
12 Och Adaja, Jerohams son, Pashurs sons, Malchia sons; och Masai, Adiels son, Jahsera sons, Mesullams sons, Mesillemiths sons, Immers sons;
Adaya mwana wa Yerohamu, mwana wa Pasi-Huri, mwana wa Malikiya; ndi Maasai mwana wa Adieli, mwana wa Yahizera, mwana wa Mesulamu, mwana wa Mesilemoti, mwana wa Imeri.
13 Dertill deras bröder höfvitsmän i deras fäders huse, tusende sjuhundrad och sextio starke män, till att beställa hvad ämbetet tillhörde i Guds hus.
Ansembe amene anali atsogoleri a mabanja awo analipo 1,760. Anali anthu amphamvu ndi odziwa kutumikira mʼnyumba ya Mulungu.
14 Men af Leviterna, af Merari barnom, Semaja, Hasubs son, Asrikams sons, Hasabia sons,
Alevi: Semaya mwana wa Hasubu, mwana wa Azirikamu, mwana wa Hasabiya, wa mʼbanja la Merari;
15 Och Bakbakkar, den timbermannen, och Galal; och Matthania, Micha son, Sichri sons, Assaphs sons,
Bakibakara, Heresi, Galali ndi Mataniya mwana wa Mika, mwana wa Zikiri, mwana wa Asafu;
16 Och Obadja, Semaja son, Galals sons, Jeduthuns sons, och Berechia, Asa son, Elkana sons, den som uti de Netophathiters byar bodde.
Obadiya mwana wa Semaya mwana wa Galali, mwana wa Yedutuni ndi Berekiya mwana wa Asa, mwana wa Elikana, amene ankakhala ku midzi ya Anetofati.
17 Dörravaktarena voro: Sallum, Akkub, Talmon, Ahiman, med deras bröder; och Sallum, öfversten.
Alonda a pa makomo: Salumu, Akubu, Talimoni, Ahimani ndi abale awo. Mtsogoleri wawo anali Salumu.
18 Ty härtill hade vaktat för Konungsporten östantill Levi barn, i lägre,
Amenewa amakhala pa chipata cha mfumu kummawa mpaka lero lino. Alonda a gulu la Alevi anali awa:
19 Sallum, Kore son, Ebiasaphs sons, Korahs sons, och hans bröder utu hans faders hus, de Korhiter, vid ämbetets sysslo, att de vaktade vid tabernaklets dörrar, och deras fader i Herrans lägre, att de skulle vakta på ingången.
Salumu mwana wa Kore, mwana wa Ebiyasafu, mwana wa Kora, pamodzi ndi abale ake a ku banja la makolo ake, Akora aja ankanyangʼanira khomo la Tenti monga ankachitira abambo awo polondera khomo la malo okhalapo Yehova.
20 Men Pinehas, Eleazars son, var Försten öfver dem, derföre att Herren hade tillförene varit med honom.
Masiku oyamba Finehasi mwana wa Eliezara anali woyangʼanira alonda apakhomo ndipo Yehova anali naye.
21 Zacharia, Meselemia son, var väktare vid vittnesbördsens tabernakels dörr.
Zekariya mwana wa Meselemiya anali mlonda woyangʼanira pa chipata cha tenti ya msonkhano.
22 Alle desse voro utvalde till väktare vid dörrarna, tuhundrad och tolf. De voro räknade i deras byar. Och David och Samuel Siaren stiktade dem genom deras tro;
Onse amene anasankhidwa kukhala alonda pa khonde analipo 212. Iwo analembedwa mwa mibado yawo ku midzi yawo. Davide ndi mneneri Samueli ndiwo anawayika mʼmalo awo antchito chifukwa cha kukhulupirika kwawo.
23 Att de och deras barn skulle taga vara på Herrans hus, nämliga på tabernaklets hus, att de det vakta skulle.
Iwo ndi zidzukulu zawo anali oyangʼanira zipata za nyumba ya Yehova imene imatchedwa Tenti.
24 De samme dörravaktare voro ställde på fyra sidor, östan, vestan, norr, söder.
Alonda apakhomowa anali mbali zonse zinayi: kummawa, kumadzulo, kumpoto ndi kummwera.
25 Men deras bröder voro i sina byar, så att de ju inkommo på sjunde dagen, till att alltid vara när dem.
Abale awo a ku midzi yawo amabwera nthawi ndi nthawi kudzagwira ntchito yawo kwa masiku asanu ndi awiri.
26 Förty Leviterna voro dessom fyra öfversta dörravaktaromen betrodde, och de voro öfver kistorna och skatten i Guds hus;
Koma atsogoleri akuluakulu anayi a alonda, amene anali Alevi, anapatsidwa udindo woyangʼanira zipinda ndi chuma cha nyumba ya Mulungu.
27 Och blefvo de öfver nattena omkring Guds hus; ty dem hörde vakten till, att de skulle upplåta hvar morgon.
Iwo amakhala usiku wonse atayima mozungulira Nyumba ya Mulungu, chifukwa anayenera kuyilondera. Ndipo anali ndi kiyi wotsekulira mmawa uliwonse.
28 Och somlige af dem voro öfver ämbetstygen; förty de båro dem tald ut och in.
Ena amayangʼanira zipangizo zimene amagwiritsa ntchito pa ntchito mʼNyumba ya Mulungu. Iwo amaziwerenga zikamalowetsedwa ndi potulutsidwa.
29 Och somlige af dem voro beställde öfver kärilen, och öfver all helig redskap; öfver semlomjöl, öfver vin, öfver oljo, öfver rökelse, öfver rökverk.
Ena anapatsidwa udindo wosamalira zipangizo ndi zinthu zina zonse za ku malo opatulika, pamodzi ndi ufa, vinyo, mafuta, lubani ndi zonunkhira.
30 Men Presternas barn gjorde somlige rökverk.
Koma ansembe ena amasakaniza zonunkhirazo.
31 Mattithia utaf Leviterna, dem första Sallums sone, den Korhitens, voro betrodda pannorna.
Mlevi wotchedwa Matitiya mwana woyamba wa Salumu wa mʼbanja la Kora, anapatsidwa udindo woyangʼanira zophikidwa mʼziwaya.
32 Utaf de Kehathiter deras bröder, voro till att bereda skådobröden, så att de tillredde dem på hvar Sabbathsdag.
Abale ake ena a mʼbanja la Akohati amaphika buledi wa pa Sabata lililonse amene amayikidwa pa tebulo.
33 Desse äro de sångare, höfvitsmän ibland Leviternas fäder, öfver kistorna skickade; förty dag och natt voro de der öfver i sysslomen.
Atsogoleri a mabanja a Alevi, amene anali ndi luso loyimba, amakhala mʼzipinda za Nyumba ya Mulungu ndipo samagwira ntchito zina chifukwa ankatumikira usana ndi usiku.
34 Desse äro höfvitsmän förfäderna ibland Leviterna uti deras ätter; och bodde i Jerusalem.
Onsewa anali atsogoleri a mabanja a Alevi, akuluakulu monga analembedwera pa mibado yawo, ndipo ankakhala mu Yerusalemu.
35 I Gibeon bodde Jegiel, Gibeons fader; hans hustru het Maacha;
Yeiyeli abambo a Gibiyoni ankakhala ku Gibiyoni. Dzina la akazi awo linali Maaka,
36 Och hans förste son Abdon, Zur, Kis, Baal, Ner, Nadab,
ndipo mwana wawo woyamba kubadwa anali Abidoni, motsatana ndi Zuri, Kisi, Baala, Neri, Nadabu,
37 Gedor, Ahio, Zacharia, Mikloth.
Gedori, Ahiyo, Zekariya ndi Mikiloti.
38 Men Mikloth födde Simeam; de bodde också omkring deras bröder i Jerusalem, ibland sina bröder.
Mikiloti anabereka Simeamu. Iwonso ankakhala ndi abale awo ku Yerusalemu.
39 Ner födde Kis. Kis födde Saul. Saul födde Jonathan, MalchiSua, AbiNadab, Esbaal.
Neri anabereka Kisi, Kisi anabereka Sauli, ndipo Sauli anabereka Yonatani, Maliki-Suwa, Abinadabu ndi Esibaala.
40 Jonathans son var Meribaal; Meribaal födde Micha.
Mwana wa Yonatani anali Meri-Baala, amene anabereka Mika.
41 Micha barn voro: Pithon, Melech och Thahrea.
Ana a Mika anali: Pitoni, Meleki, Tahireya ndi Ahazi.
42 Ahas födde Jaera. Jaera födde Alemeth, Asmaveth och Simri. Simri födde Moza.
Ahazi anabereka Yara, Yara anabereka Alemeti, Azimaveti ndi Zimuri, ndipo Zimiri anabereka Moza.
43 Moza födde Binea. Hans son var Rephaja, Hans son var Eleasa. Hans son var Azel.
Moza anabereka Bineya. Ana ake anali Refaya, Eleasa ndi Azeli.
44 Azel hade sex söner; de heto: Asrikam, Bochru, Ismael, Searia, Obadja, Hanan. Desse äro Azels barn.
Azeli anali ndi ana asanu ndi mmodzi ndipo mayina awo anali awa: Azirikamu, Bokeru, Ismaeli, Seariya, Obadiya ndi Hanani. Awa anali ana a Azeli.

< 1 Krönikeboken 9 >