< Zaburi 87 >

1 Mji aliouanzisha umesimama juu ya mlima mtakatifu;
Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2 Yahwe anapenda zaidi malango ya Sayuni kuliko mahema yote ya Yakobo.
Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
3 Mambo matukufu yamesemwa kwako, mji wa Mungu. (Selah)
Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
4 Ninataja Rahabu na Babeli kwa wafuasi wangu. Tazama, Filisti, na Tiro, pamoja na Ethiopia nao watasema, 'Huyu alizaliwa humo.'”
“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
5 Itasemwa juu ya Sayuni, “Kila mmoja wa hawa alizaliwa katika yeye; na yeye Aliye Juu atamuimarisha.
Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
6 Yahwe anaandika katika kitabau cha sensa ya mataifa, “Huyu alizaliwa humo.” (Selah)
Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
7 Hivyo waimbaji na wachezaji kwa pamoja waseme, “chemchem zangu zimo kwako.”
Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”

< Zaburi 87 >