< Zaburi 120 >
1 Katika dhiki yangu nilimuita Yahwe, naye akanijibu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
2 Uiokoe nasfi yangu, yahwe, dhidi ya wale wadanganyao kwa midomo yao na wanenao hila kwa ndimi zao.
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
3 Yahwe atawaadhibu vipi, na atawafanyia kitu gani zaidi, ninyi mlio na ulimi mdanganyifu?
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
4 Atawaadhibu kwa mishale ya shujaa iliyo nolewa kwa makaa ya moto ya mretemu.
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
5 Ole wangu mimi kwa sababu ninaishi kwa muda Mesheki; huko nyuma niliishi kati ya maskani ya Kedari.
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
6 Kwa muda mrefu sana niliisha na wale waichukiao amani.
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
7 Nipo kwa ajili ya amani, lakini ninenapo, wao wako kwa ajili ya vita.
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.