< Zaburi 136 >

1 Mshukuruni Bwana, kwa kuwa ni mwema.
Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
2 Mshukuruni Mungu wa miungu.
Yamikani Mulungu wa milungu.
3 Mshukuruni Bwana wa mabwana:
Yamikani Ambuye wa ambuye,
4 Kwake yeye pekee atendaye maajabu makuu,
Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
5 Ambaye kwa ufahamu wake aliziumba mbingu,
Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
6 Ambaye aliitandaza dunia juu ya maji,
Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
7 Ambaye aliumba mianga mikubwa,
Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
8 Jua litawale mchana,
Dzuwa lilamulire usana,
9 Mwezi na nyota vitawale usiku,
Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
10 Kwake yeye aliyemuua mzaliwa wa kwanza wa Misri,
Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
11 Na kuwatoa Israeli katikati yao,
Natulutsa Israeli pakati pawo,
12 Kwa mkono wenye nguvu ulionyooshwa,
Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
13 Kwake yeye aliyeigawa Bahari ya Shamu,
Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
14 Na kuwapitisha Israeli katikati yake,
Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
15 Lakini alimfagia Farao na jeshi lake katika Bahari ya Shamu,
Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
16 Kwake yeye aliyewaongoza watu wake katika jangwa,
Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
17 Ambaye aliwapiga wafalme wenye nguvu,
Amene anakantha mafumu akuluakulu,
18 Naye aliwaua wafalme wenye nguvu,
Napha mafumu amphamvu,
19 Sihoni mfalme wa Waamori,
Siloni mfumu ya Aamori,
20 Ogu mfalme wa Bashani,
Ogi mfumu ya Basani,
21 Akatoa nchi yao kuwa urithi,
Napereka dziko lawo ngati cholowa,
22 Urithi kwa Israeli mtumishi wake,
Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
23 Aliyetukumbuka katika unyonge wetu,
Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
24 Alituweka huru toka adui zetu,
Amene anatimasula kwa adani athu,
25 Ambaye humpa chakula kila kiumbe.
Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
26 Mshukuruni Mungu wa mbinguni,
Yamikani Mulungu wakumwamba,

< Zaburi 136 >