< Zaburi 134 >

1 Wimbo wa kwenda juu. Msifuni Bwana, ninyi nyote watumishi wa Bwana, ninyi mnaotumika usiku ndani ya nyumba ya Bwana.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Bwerani, mutamande Yehova, inu atumiki onse a Yehova, amene mumatumikira usiku mʼnyumba ya Yehova.
2 Inueni mikono yenu katika pale patakatifu na kumsifu Bwana.
Kwezani manja anu mʼmalo opatulika ndipo mutamande Yehova.
3 Naye Bwana, Muumba wa mbingu na dunia, awabariki kutoka Sayuni.
Yehova wolenga kumwamba ndi dziko lapansi, akudalitseni kuchokera mʼZiyoni.

< Zaburi 134 >