< Salmos 98 >
1 Oh, haz una nueva canción al Señor, porque él ha hecho obras de maravilla; con su diestra, y con su brazo santo, él ha vencido.
Salimo. Imbirani Yehova nyimbo yatsopano, pakuti Iyeyo wachita zinthu zodabwitsa; dzanja lake lamanja ndi mkono wake woyera zamuchitira chipulumutso.
2 El Señor ha dado a todos el conocimiento de su salvación; él ha dejado en claro su justicia a los ojos de las naciones.
Yehova waonetsa chipulumutso chake ndipo waulula chilungamo chake kwa anthu a mitundu ina.
3 Ha tenido en cuenta su misericordia y su fe inmutable a la casa de Israel; todos los confines de la tierra han visto la salvación de nuestro Dios.
Iye wakumbukira chikondi chake ndi kukhulupirika kwake pa Aisraeli; malekezero onse a dziko lapansi aona chipulumutso cha Mulungu wathu.
4 Que toda la tierra envíe un clamor alegre al Señor; sonando con una voz fuerte, y alabándolo con canciones de alegría.
Fuwulani mwachimwemwe kwa Yehova, dziko lonse lapansi, muyimbireni nyimbo mofuwula ndi mokondwera.
5 Haz melodía al Señor con instrumentos de música; con arpa y la voz de la canción.
Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze, ndi zeze ndi mawu a kuyimba,
6 Con los instrumentos de viento y el sonido de trompeta, haz un alegre clamor ante el Señor, el Rey.
ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna fuwulani mwachimwemwe pamaso pa Yehova Mfumu.
7 Sea estruendo el mar, con todas sus aguas; el mundo y todos los que viven en él;
Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo, dziko lonse ndi onse amene amakhala mʼmenemo.
8 Que las corrientes hagan sonidos de alegría con sus manos; Que las montañas se alegren juntas,
Mitsinje iwombe mʼmanja mwawo, mapiri ayimbe pamodzi mwachimwemwe;
9 Delante del Señor, porque vino como juez de la tierra; juzgar al mundo con justicia y con rectitud e igualdad gobernará los pueblos.
izo ziyimbe pamaso pa Yehova, pakuti Iye akubwera kudzaweruza dziko lapansi. Adzaweruza dziko lonse mwachilungamo, ndi mitundu ya anthu mosakondera.