< Salmos 23 >
1 El Señor es mi Pastor; Nada me faltará.
Salimo la Davide. Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
2 Él me hace un lugar de descanso en los campos verdes: él es mi guía junto a las aguas tranquilas.
Amandigoneka pa msipu wobiriwira, amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
3 Él me da nuevas fuerzas: él es mi guía en los caminos de la justicia haciendo honor de su nombre.
amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo chifukwa cha dzina lake.
4 Sí, aunque atraviese el valle de la sombra de muerte. no temeré el mal; porque tú estás conmigo, tu vara y tu cayado me infundirán confianza.
Ngakhale ndiyende mʼchigwa cha mdima wakuda bii, sindidzaopa choyipa, pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu zimanditonthoza.
5 Tu preparas un banquete para mí frente a mis enemigos: unges con aceite mi cabeza; mi taza se está desbordando.
Mumandikonzera chakudya adani anga akuona. Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta; chikho changa chimasefukira.
6 Verdaderamente, la bendición y la misericordia estarán conmigo todos los días de mi vida; y moraré en la casa del Señor todos mis días.
Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova kwamuyaya.