< Salmos 13 >

1 ¿Me olvidarás para siempre de tu memoria, oh Señor? ¿Hasta cuando tu rostro se alejará para siempre de mí?
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale? Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
2 ¿Cuánto tiempo habrán de sufrir mi alma, y con tristeza en mi corazón todo el día? ¿Hasta cuándo tendrá poder sobre mí el que está en mi contra?
Ndidzalimbana ndi maganizo anga ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti? Mpaka liti adani anga adzandipambana?
3 Mírame y dame una respuesta, oh Señor mi Dios; deja que tu luz brille sobre mí, para que el sueño de la muerte no me alcance;
Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga. Walitsani maso anga kuti ndingafe;
4 Y el que está contra mí no puede decir: yo lo he vencido; y aquellos que me molestan pueden no estar contentos si yo resbalara.
mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,” ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.
5 Pero he tenido fe en tu misericordia; mi corazón se alegrará en tu salvación.
Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika; mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
6 Cantaré al Señor, por él bien que me ha hecho.
Ine ndidzayimbira Yehova pakuti wandichitira zokoma.

< Salmos 13 >